0% found this document useful (0 votes)
106 views108 pages

Nyimbo Za Mulungu.

Download as pdf or txt
Download as pdf or txt
Download as pdf or txt
You are on page 1/ 108

REFORMED CHURCH IN ZAMBIA

HYMN BOOK. (COMPLETE EDITION)


EDITED BY ELIAS MUTEYA, LILANDA CONGREGATION

Mwana wosatha wa Atate ndinu!


Simunanyoza mimba ya Namwali
1 Potipulumutsa.
1. NDINU wakuyera! Wamphamvu 7. Imfa mutagonjetsa ndi zoŵaŵa.
zonse. Njira munatsegula tikaloŵe
Nthaŵi ya m’mamaŵayi tiimba Momwe mukhala Inu ndi Atate
nyimboyi. Mwaulemerero
Mlengi wachifundo, tikuyamikani, 8. Kumva milandu yathu mudzabwera
E! Mlungu Mmodzi mwa Atatuwo. Mutithandize, atumiki anu;
2. Ndinu Wakuyera! Anthu ochuluka Mwatiwombola nawo mwazi wanu:
Akuimbirani, nakupempharanibe; Mutipulumutse.
Akumwamba omwe nagwadira Inu, 9. Mtiŵerengere m’Mwamba ndi oyera;
Wachikhalire ndi wosafa ’yi. Mutidalitse, ndife anthu anu;
3. Ndinu wakuyera! Ife akuchimwa Moyo wosatha, mutipatse tonse,
Zaulemerero zanu sitiona’yi; Mutilamule.
Mwayera nokha, wina saoneka 10. Tsiku ndi Tsiku timalemekeza:
Wangwiro m’mphamvu ndi Nanu tikukuzani osaleka;
m’kuyeramo. Mbuye, mtisunge tingachimwe lero;
4. Ndinu wakuyera! Zakumwamba zonse Mtichitire nsisi.
Ndi zapansi zitamabe dzina lanulo; 11. Mbuye, chifundo chanu chitigwere
Mlengi wachifundo, Mphambi, Monga tikhulupira inu nokha:
Ambuyathu, Ndakhulupira zedi mwanu, Mbuye
E! Mlungu Mmodzi mwa Atatuwo. Ndisagome konse!
2 3
1. INU Mulungu, tikuyamikani; 1. ATATE wa Kumwambako,
Tivomereza ndinu Ambuyathu; Munawombola ife ndi
Ponse, atate, akugwadirani, Chikondi chanu chijacho;
Ndinu wamuyaya! Tiyamikira Inutu.
2. Nanu akukuzani amithenga, 2. Ambuye Yesu Inutu
Nanu zam’mwamba ndi zamphamvu Munabadwira anthu ’fe;
zake, Munatifera tonsefe;
Nanu angelo a mitundu yonse Tiyamikira Inutu.
Akuimbirani: 3. Mzimu Woyera, m’mtimamo
3. Mbuye Woyera! E, Woyera nokha! Tiyeretsedwe ndinutu;
Mbuye Woyera! Mbuye wa makamu! Munatisunga bwinoli;
Ponse ulemu wanu ndi wodzaza Tiyamikira Inutu.
Pansi ndi Kumwamba.” 4. Atate, Mwana, Mzimunso,
4. Nanu Atumwi akumveka aja, Ndinu Atatu Mmodzitu,
Ndi Aneneri oyanjana omwe, Ochimwa tikupemphani:
Ndi aunyinji anakuferani Mutikhululukire ’fe
Akuyamikani.
5. Mpingo woyera wa kwa anthu onse 4
Ukumverani Mfumu ndi Atate, 1. LEMEKEZA Mulungu ’Tate,
Mwana woona wa ulemu wonse, Lemekeza Mulungu Mwana,
Mzimu Nkhoswe yemwe. Lemekeza Mulungu Mzimu,
6. Khristu Mfumuyo yaulemerero!
Mulungu Mmodzi ndi wamkulu, Yogunda mvula m’mlengalengamo,
Lemekeza, lemekeza Mawu akulu muzinenadi:
Mulungu wathu yemweyo. Aleluya.
2. Mlemekeze, anakonda 2 Paphiri paja papakulupo,
Natitsuka m’mtima mwathu; Pamwala ponse pakuŵala mbuu!
Anatiwombola ife Mumvomereze mawu omwewo:
Tikakhale ndi chifumu. Aleluya.
Lemekeza, lemekeza 3 Mphepo yay’kulu yakuwombayo,
Yesu Mbuye Nsembeyo. Chisanu chija chozizirachi,
3. Lemekeza Mfumu yathu, Ndi kabvumbulu muzinenadi;
Mfumu ya mipingo yonse, Aleluya.
Ipambana anthu onse 4 Mitengo yaitalitali ’nu
Akumwamba ndi apansi. Yachiimire mumaimabe,
Lemekeza, lemekeza Mubvomereze ndi kunenabe:
Mfumu ya mafumuyo. Aleluya.
5 Zam’madzi zonse zakuopsyazo,
Nyanja, matiti ndi mitsinjeyo,
5 Chigumula chakulindimacho,
1. Ndi aleluya imbirani Aleluya.
Tate wathu wakumwamba, 6 Zamoyo zili m’thengo zonsezo,
Analenga zones, Zodzuma, zina zobangulazo,
Chifundo chache chachikulu, Zimene ndi kulira konseko:
Nzeru mphamvu ndi unfumu, Aleluya.
Tayamike tonse. 7 Inu mumvere anyamatawo,
2. Ndi aleluya imbirani Okondedwa kuseŵerako,
Yesu Kristu Mpulumutsi, Mumtima mubvomere monsemo:
Anachoka kwawo, Aleluya.
Nakhala munthu pansi pano, 8 Ndi anamwali obvekedwa mbuu!
Nasauka, natifera, Ndi ana osakula msinkhu ’nu
……… mawu, Ana a Mulungu mubvomeretu:
3. Ndi aleluya imbirani Aleluya.
Mzimu wake wakuyera 9 Akulu nonse ndi mafumu ’nu
Amakhala nafe. Magulu nonse apadzikopa,
Atilangisa na Mulungu Mumlemekeze Mbuye yemweyo:
Nayeretsanso mitima Aleluya.
ya akristu ife. 10 Ndi amithenga akumwambako,
4. Mulungu wathu tiyamika, Ndi anthu ndi zamoyo zonsezo,
“Tate, Mwana, Mzimu yemwe,” Bvomerezani mau omwewo:
Aleluya inu. Aleluya.
Woyera inu ndi wamphamvu, 7
Muyenera anthhu onse
1. TAMANI Ambuye,
Agwadira inu.
Wamphamvu ndi Iye
Akhala m’ulemu
6 Kumwamba komweko:
Chikopa cholimba
1 MITAMBO inu yakumwambako
Ndi kothaŵiranso 2. Mulungu yemweyo
Kwa anthu akewo, Akhale m’fupi mwathu;
Kotero ndi Mlungu. Mtendere wakewo
2. Uzani zamphamvu, Ukhale m’mtima mwathu;
Imbani chisomo, Titsate Iyedi
Za Mwini ulemu, Ndi nsoni zakezo,
Ambuye wathuyo; Panjira yakeyi
Powomba chimphepo Masiku onsewo.
Mvulanso ndi bingu 3. Tilemekezetu
Padziko, pathambo, Atate wakumwamba,
Akhala ponsepo. Ndi Yesu Mbuyathu,
3. Zozizwa za m’dziko, Ndi Mzimu Wakuyera;
Za m’mwamba zonsezi, Mulungu Mmodziyu
Mulungu wamphamvu, Wanthaŵi zonsezo,
Munalenga zonse; Timlemekezetu
Muyendetsa mwezi Masiku onsewo.
Nyenyezi ndi dzuŵa:
Zolengedwa zonse
9
1. NDI mitima yokondwera
Zimvera Ambuye.
Mbuye wathu tiyamika.
4. Sitiha ifedi
E, chifundo chake chonse
Kukamba zokoma
Ndi chosatha nthaŵi zonse.
Za Inu Mulungu
2. Dzina Lake Tibukitsa,
Wolera anthuwa;
Mlungu ndiye yekhayekha.
Zifika ndi mphepo
3. Mphamvu yake inalenga
Ndi mvula ndi dzuŵa,
Dziko lonse ndi kumwamba.
Zigwera ponsepo
4. Anatsogolera kale
Pa anthu onsewa.
M’chipululu anthu ake.
5. Wamphamvu yosatha,
5. Ndi chifundo atipenya
Chikondi changwiro,
Ife anthu osauka.
Angelo akonda
6. Amaŵeta nyama zonse.
Kutama Mulungu;
Zingasoŵe kanthu konse.
Ndiponso ifetu
7. Tiimbire Mlungu wathu
Ananu tonsefe
Waulemu ndi wamkulu.
Tiyimba nyimboyi
8. Tithaŵire kwa Mulungu,
Yotama Ambuye.
Ndiko tikapeze moyo.
8 10
1. TSOPANO linoli
1. NDITAMATU Ambuyangayu,
Tiimbe nyimbo zathu;
Moyo wanga wonse ndidzamtamatu,
Tiimbe nyimbozi,
Ndiponso dziko lakumwambako;
Titame Mlungu wathu;
Masiku anga onse ndidzamlemekeza
Masiku onsewo
Iye;
Anatisungadi,
Sindizaleka konsekonse m’mene ndili
Anatipatsanso
m’moyotu,
Zabwino zonsezi.
Padziko pano pena m’Mwambamo.
2. Ndiye wokondwa, E, munthuyo
Wokhulupirira Mlungu yekhadi, 3. Okwaŵa pansi inu,
Wolenga dziko, nyanja, zonsezi; Oyenda m’madzi inu,
Choona chake chonse chingokhalatu Oyesa dziko nkwanu,
chosatha; Am’mlengalenga inu,
Apulumutsa onse namadyetsa anthu Nonsenu ntchito zake
akewo, Muona tsiku n’tsiku,
Wokonda ndiye Mbuye wathuyo. Saleka kusamala
3. Mlungu kuona athiratu Ndikudalitsa inu.
Inde m’maso awo osapenyawo. 4. Nditama mphamvu yake
Natuma akumvera mpumulo; Ya Mlungu yondizinga;
Amathandiza inde aulendo awo N’kafoka an’limbitsa,
ofokatu, N’kadwala andichiza
Akazi amasiye maka ndi anawo Pakundisiya bwenzi
onsewo, Mulungu ali paja;
Olira otonthoza mtimadi. N’kaloŵa imfa ine
4. Nditama Ambuyangayu, Alipo Mlungu wanga.
Moyo wanga wonse ndidzamtamatu
Ndiponso m’dziko lakumwambako;
12
1. Mtima wanga uyamike
Masiku anga onse ndidzamlemekeza
MfumuYakumwambako;
Iye:
Anandiwombola ine
Sindidzaleka konsekonse m’mene
Nanditsuka m’mtimamo
ndili m’moyotu,
Ife tonse, ife tonse,
Padziko pano pena m’Mwambamo.
Tiyamike Mlunguyo.
11 2. Tiyamike Mulungu wathu,
1. Paphiri ndi padambo Kaamba ka chifundocho;
Ponsepo pali Mlungu, Nthaŵi zonse sasanduka
Poyenda ife m’njira Mlungu wathu yemweyo
Mpoima pali Mlungu; 3. Nthaŵi zonse monga ‘Tate
Kokwera Maganizo, Atisamaliratu,
Komwe kuli Mlungu, Atisunga m’manja mwake,
Kumwamba ndi pansipo Atipulumutsatu.
Ponsepo pali Mlungu. 4. Anthu a mitundu yonse,
(Mulungu ali nane!) Ndipo a Kumwambako,
(Ali nane, ali nane, ali nane Yamikani Mungu wathu,
Ali nane, Aa! Ndiye wakukomatu.
Mulungu ali nane!) Anthu onse, anthu onse,
2. Ndi maso Ambuyathu Yamikani Mlunguyo.
Apenyetsetsa ife;
Amadalitsa onse
13
1. YEHOVA ndiye Mbusa wanga,
Okhulupira Iye;
sin’ngasoŵe konse:
Amamva timbalame,
Andigonetsa pali busa
Nabveka dziko lonse;
la misipu yonse.
Sataya tizirombo,
(Ndiye Mbusa wanga,
Asunga zina zonse.
Ndiye Mbusa wanga!
Yehova ndiye Mbusa wanga,
Sin’ngasoŵe konse.) Aleluya! Kondwerani!
2. Kumadzi kuli njiratu Mlungu wathu yamikani!
andiyendetsa bwino, 15
Nalimbikitsa moyo wanga
1. MULUNGU ndiye Mbusa wanga,
ndi chifundo chino.
sindisoŵa konse;
3. Pabande lolunjika
Amandiŵeta nandidyetsa
andilondolera njira;
nandipatsa zonse.
Chifukwacho cha dzina lake
(Ndiye Mbusa wanga,
anandisungira.
Ndiye Mbusa wanga!
4. Chigwa choopsacho cha imfa
Mulungu ndiye Mbusa wanga,
ndikachiloŵera,
Sindisoŵa konse)
Ndilibe mantha, muli ndine,
2. M’mitsinje yamtendere mtima
ndodo ndiigwira.
wanga aumwetsa;
5. Pamaso pa adaniwo
Mapazi omwe m’njira
mwayala gome langa;
Yolungama nayendetsa.
E, mutu mwaudzoza,
3. Za m’mdima, imfa, nkhondo ndi zoipa
chisefuka chikho changa.
sindiopa;
6. Zabwino ndi zokoma
Ndikakhumudwa ndi kutopa,
zinditsata chitsatire;
Andipulumutsa.
E, m’nyumba ya Yehova
4. Podwala ine pobvutidwa
ndidzakhala chikhalire.
Andisamalira;
14 Pondisauts’ adani anga
1. MTIMA wanga lemekeza nandithangatira.
Mlungu wako ndi Chimwemwe. 5. Chisomo ndi zokoma zake
Nthaŵi zonse ndimtamanda; sizileka konse;
Ndimwimbira nyimbo zanga. Ndi m’nyumba ya Mulungu
Moyo, mphamvu, nzeru zonse, Ndidzakhala nsiku zonse.
Zidzamlekeza konse.
2. Ndi wamwayi munthu uja
16
1. ZOBVUTA zoopsya ndi zosaukazi
Amthandiza Mbuye wake
Sitingathe ife kuzithaŵa tokha.
Akachita mantha iye
Koma Ambuyathu timtamande Iye,
Amchotsera nkhaŵa yake,
Uthenga Wabwino timveretu kokha.
Ndipo likamgwera tsoka
2. Amadyetsa iye mbalame
Amakhulupira kokha.
zam’mwamba,
3. Mbuye ndiye wachifundo,
Timtamande ndithu potisunga ife;
Achiritsa akudwala;
Timvere malembo a m’kalata mwake,
Anyamula akufoka
Ambuye yemweyo atisungirabe.
Naŵadyetsatu anjala.
3. Abramu kalelo anamvera bwino;
Wakusunga mlendo ndiye,
Timverenso ngatitu yemwe wakale.
Nathandiza amasiye.
Pokhala alendo atsogoza iwo,
4. Ndiye Mbuye wa ambuye;
Timkhulupirire Ambuye tonsefe.
Mphamvu yake ndi yokwana.
4. Timtamande Iye ndi moyo wathunso
Adzakhala chikhalire,
Pakutsatatsata malembedwe awo.
Mfumu yathu yopambana,
Tipezamo malembedwe awo.
Tipezamo malo okwanira ife Ndi Mlungu Iyeyo,
Ambuye wathu atipatsa kwawo. Anatifera anthu ’fe
17 Ndi Mulungu Iyenso.
6. Ndi m’munda muja chete, phee!
1. POKONDWA ndi poona bvuto
Pamtanda pati njo!
Ndi tsoka pena mwayi,
Anaphunzitsa ’bale ’fe
Ndikumbukira, ndiimbira
Titero ifenso.
Mulungu wangayo.
7. Kuuzani Mlungu m’Mwambamo
2. Kwezani nane Ambuyathu,
Mtamande m’kuyanso;
Timlemekeze yekha;
Nzozizwa nkhani zakezo,
Popsinja mtima ndinamtchula,
Njolimba ntchito njo!
Nandithangata ’ne
3. ANGELO amazinga nyumba 19
Za anthu olungama; 1. KALELO anthu onse
Mulungu ateteza omwe Nachimwa kwa Mulungu
Amkhulupirira. Mulungu anaona
4. Laŵani chikondano chake; Naona tchimo lawo,
Mudzadziŵitsa msanga Nafuna kwawononga,
Kudala kwawo kwa anake Nafuna kwawononga.
Omkonda Mbuyeyo. 2. Mulungu anatuma,
5. Opani iye, nimuleke Natuma mvula ija,
Kuopa kanthu kena; Nadzaza dziko lonse
Mumtumikire mokondwera, Anafa anthu onse,
Akusungani ’nu. Anafa m’mvula muja,
6. Mulungu wathu Mmodzi yekha Anafa m’mvula muja.
Atate, Mwana, Mzimu, 3. Mulungu anatuma,
Akhale ndi ulemerero Natuma Nowa uja,
Wachikhalirewo! Wamanga chombo chake,
18 Ndi chachitalitali,
Nowayo nayendamo,
1. KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
Nowayo nayendamo.
Mtamande m’kuyanso;
4. Nowayo anatuma,
Nzozizwa nkhani zakezo,
Natuma chikwangwala,
Njolimba ntchito njo!
Chatsika pansi pansi,
2. Pochimwa anthu onsewo
Chosabwerera konse,
Nja Mlungu nzeruyi;
Chithaŵa m’talitali,
Adamu wachiŵiriyo
Chithaŵa m’talitali.
Wathetsa tchimoli.
5. Kutuma wabwereza,
3. Thupi la mwazi wathu ’li
Natuma nkhunda ija,
Lochimwa kalelo,
Yatsika pamadzipo,
Labweranso ku nkhondoyi,
Yathyolatu mayani,
Laposa monsemo.
Yampatsa Nowa yemwe,
4. Choposa nalo thupilo
Yampatsa Nowa yemwe.
Chikhale momwemu,
6. Kalelo Mbuye Yesu
Chiyeretsetsa m’katimo,
’Nafera anthu onse,
Ndi Mulungu Iyeyu.
5. Anatikondakonda ’Ye,
Ndiyeyo chombo chathu, Kutifikitsa m’Mwambamo.
Tikabisala mommo 3. Pakuwoloka mtsinje wa imfa
Tipulumuka mommo, Dzanja Mbuyathu agwira;
Tipulumuka mommo. Tikadagwira ntchito zake
20 Atipatsatu korona;
Komwe kulibe masauko,
1. MULUNGU aŵakonda anthu
Pena misozi maliro;
Ali pansi pano;
Mulungu tidzamtamandira,
Afuna kuŵapulumutsa
Inde kosalekezanso.
Kumilandu yawo.
A! Chikondi chachikulu 22
Mulungu ali nacho, 1. NDIKONDA Mlungu pomva
Chimam’tengera Mpulumutsi, Mbuye wanga
Andifere pano Amva pemphero ndi kulira kwanga,
2. Ndikhulupira mwa Ambuye, Namachereza khutu nditapfuula,
Mulungu namukitsa, Andithandiza, nandipulumutsa.
Imfayo indipulumutsa, 2. Mulungu wanga ndiye wachifundo
Mwazi und’yeretsa. Ndi wolungama mtima ndi wabwino;
3. Chikondi chake chindidzera Apulumutsa anthu akufoka,
M’mtima mwanga muno, Akathandiza nkhaŵa imachoka.
Chipulumutsa nditalema 3. Mtimanga, bwera kuti upumule,
Ndi machimo anga. Wakuchitiranso zokoma Mbuye,
4. Mukondwe anthu a Mulungu, Wakuchotsera imfa ndi misozi,
Tere mulandira Ndingakhumudwe asungira phazi.
Chimwemwe chija chakumwamba, 4. Nditani ine kubwezera Mbuye
Chidzaloŵa m’mtima. Zokoma zonse anandichitira?
5. Mulungu atipatsa mphamvu Chipulumutso chake ndidzatama,
Yoletsetsa tchimo; Ndinalumbira zija ndidzapatsa.
Pofika tsikulo la imfa, 5. Imfa ya anthu ake imkomera,
Tidzakhala bwino. Aŵalandira m’nyumba zokonzeka.
21 Mbuye, kapolo wanu ndipereka
Nsembeyi yonga yanu, ndine ndekha.
1. TIIMBE nyimbo zotamanda
Mulungu wathu wabwino, 23
Pakuti akondana nawo 1. TITAME Mlungu Wakumwamba,
Anthu okhala padziko; Timwimbire nyimbo,
Tero natuma Mwana wake, Kukoma kwake kwatipatsa
Wakukondedwa kalelo, Zonse tili nazo.
Kutiphunzitsa ife tonse (Timwimbire nyimbo,
Za chikondano chakecho. Timwimbire nyimbo!
2. Mulungu ndiye wachifundo, Kukoma kwake kwatipatsa
Nadzalandira onsewa Zonse tili nazo)
Akuulula mphulupulu 2. Poyamba paja analenga
Ndi kukondana ndi Yesu Zonse dziko muno,
Tilondelonde njira yake Tsopano lomwe azisunga
Yopapatiza yaing’ono; Zonse zili moyo.
Adzatilondolera ndiye
3. Tinasokera ngati nkhosa, anandichitira zazikulu;
Moyo tinataya, Dzina la Ambuyanga
Tinakondwera ndi zoipa lili loyera kopambana.
Zonse tinatsata. 4. Ndiye amachitira
4. Komweko titasaukira, chifundo anthu a mibadwo,
Titafuna kufa, E! a mibadwo yonse
Atate anatilondola yakumuopa ndi kummvera.
Naitana ife. 5. Iye amazichita
5. Tiyeni tizipita kwathu, zamphamvu nawo mkono wake;
Tisasokerenso, Iye nabalalitsa
Tilape m’mtima kuti omwe anyada nadzitama
tikakhale ndi Mulungu. 6. Iye natsitsa kunsi
24 mafumu ku mipando yawo.
Iye nakweza konko
1. OONADI mtima,
omwe afatsa nasauka.
’Dzani mokondwera,
7. Ife amakhutitsa
Tiyeni, tiyeni ku Betlehemu;
anjala ndi zabwino zake,
Modyera ng’ombe
Ndi olemera onse
Muli Mfumu yathu.
naŵaingits’ opanda kanthu.
Tiyeni timgwadire
8. Monga anapangana
Khristuyo.
ponena kwa makolo athu,
2. Mulungu wamkulu
Ali kuthandizadi
Wakuyerayera
lero anake a Yakobo,
Kubadwa mwamkazi sanakana ’yi;
9. Poti akumbukira
Mwana wa ’Tate,
atate wathu Abrahamu;
Sanalengedwadi.
Inde chifundo chokha
3. Angelo kwezani
akuchitira ana ake.
Nyimbo zanu zonse,
M’wambamo mumveke zoyamikazo; 26
Lemekezani 1. AMITHENGA a Mulungu
Mulungu Wakumwamba. Anaimba nyimbo yomwe,
4. M’dzikomo Ambuye Posonkhana m’mlengalenga,
Mnabadwira ife, Natitu usiku womwe;
Ulemu wosatha muyeneradi. “Onse azilemekeza
Mawu a ’Tate, Mlungu Wakumwambamwamba;
Munaloŵa m’thupi. Akhalebe ndi mtendere
25 Anthu ali ponseponse.”
Amithenga anaimba
1. NDIKULEMEKEZA
Ndi usiku m’mlengalenga.
Ambuye Mpulumutsi wanga;
2. Anamva abusa omwe
Moyo ndi mtima wanga
Anaŵeta nkhosa zawo.
ndilikukondwa mwa Mulungu.
Mthenga nati: “Musaope;
2. Ndiye anayang’ana
Mumve ndikufotokoza:
umphaŵi wa mdzakazi wake;
Wabadwa usiku uno
Onse adzandiyesa
Yesu Kristu Ambuyathu
ine wodala nsiku zonse.
3. Ndiye wamphamvu zonse
Ndiye Mpulumutsi wathu; Ndiye kumwamba komwe
Anabadwa m’Betlehemu.” Ationetsa mbanda kucha,
Amithenga anaimba 9. Poŵalitsira omwe
Ndi usiku m’mlengalenga. ali mumdima ndi muimfa,
3. Yesu ndinu Mbuye wathu, Ndi potilunjikitsa
Munasiya za Kumwamba; tonse munjira yamtendere.
Munakhala mwana kuno; 28
Mnatifera mwaufulu.
1. AMBUYE tsopano lino,
Inu nonse amithenga,
monga mwa mawu anu aja,
Inu mumtamande Iye;
Lolani kapolo wanu
Anthu onse ali pansi
ndikachokere mumtendere;
Adza akondane naye.
2. Chifukwa chipulumutso
Zoonazi amithenga
chanu mwandionetsa zedi,
Anaimba m’mlengalenga.
Chimene munachikonza
27 akachione anthu onse;
1. AMBUYE ngwodalitsika, 3. Ndi nyali yakuŵalitsa
Mulungu wa Israyeli ndiye, omwe sadziŵa mawu anu;
Poti anayang’ana Ndiwo ulemerero
naŵawombola anthu ake, wa Israyeli mpingo wanu.
2. Napulumutsa tonse
mwapfuko la Davide mwana wake;
29
1. M’KATI mwa zobvuta zathu
Monga analankhula
Yesu aitana ife,
mwa aneneri ake, kuti
Tsiku lonse amanena:
3. Adzatipulumutsa
“Tsata Ine mkristu iwe.”
kudzanja la onse akutida,
2. Kale ophunzira ake
Ndipo adzachitira
Namvanso kunyanja kwawo,
akulu chifundo ndi chisoni.
Zinthu zonse anasiya
4. Ndiye akumbukira
Kukatsata Mbuye wawo.
pangani loyera lake lija,
3. Yesu aitana ife;
Ndi chilumbiro chake
Tikakonda chuma chokha,
cha kwa atate Abrahamu,
Ati Yesu; “Mwana wanga,
5. Choti timtumikire
Undikondetu koposa.”
osaŵaopa ’dani athu,
4. Mwachimwemwe, mwachisoni,
Ndi kuyeranso mtima
Pogwiritsa ntchito zonse,
mwa chilungamo nsiku zonse.
Aitana Mpulumutsi
6. Mwana, adzakuyesa
Kuti tizimkonda tonse.
mneneritu wa Wamkulukulu,
5. Yesu aitana ife;
Ndiwe udzakonzera
Mbuye, mutimvetse ndithu,
njira ya Mbuye Wakumwamba.
Tipereke mtima wathu,
7. Udzadziŵitsa anthu
Tikondane lero ndithu.
za Mpulumutsi wawo yemwe
Aŵakhululukira 30
Nafafaniza tchimo lawo, 1. IFE timakufunani
8. Poti Mulungu wathu Inu wotonthoza mtima.
ali ndi mtima wachifundo.
Yesu, nyimbo zathu zonse 4. “Senzani mtanda wanuwu.”
Ziyamika Inu nokha. Nawo muyende chetetu,
Munasiya zonse m’Mwamba,
Mutsogoledwe nawonso
Kudzakhala pansi pano
Kuwombola akapolo, Kwanu Kumwamba komweko.
Kumasula anthu anu. 5. “Senzani mtanda wanuwu.”
2. Yesu, ndi chifundo chanu Tsatani Yesu m’njiramu;
Chachikulu munadzera Iye wakusalemayo
Ife anthu osauka,
Ndiye alandiridwadi.
Tsoka lathu mnachotsera.
Mwazi ndi misozi yanu
Munakhetsa m’munda muja, 32
Kukonzera ife njira 1. MUNTHU wacisoniyo
Yonkako Kumwamba kuja.
… .....dzina lakelo,
3. Yesu munalaswa m’mtima,
Mpulumutsi linanso;
Ndi zonyoza munafoka,
Mnasenzera anthu mkwiyo Alleluia, ndiye Yesu.
Wa Atate, Inu nokha. 2. Anapeputaidwako,
Chikho chija ndi choopsa Nandifera m’mtandamo,
Munamwacho m’phiri lija Anandowombolayo;
M’mene munalola mtanda, Aleluya ndiye yesu
E! chifundo chanu chinja.
3. Ife tinacimwadi,
4. Yesu ndinu moyo wathu,
Chuma chathu choposetsa. Iye sanachimwa ayi,
E! tikondwerera mtanda, Anachotsa chimoli,
Apo moyo munapatsa. Aleluya, ndiye Yesu.
Mbuye tikondana nanu, 4. Anapachikidwathu
Yesu Mbuye Mwini zonse; Watha nchito yake……
Ndi mitima ndi milomo,
Tikuyamikani tonse.
Azakwera m’mwamba……
Aleluya, ndiye Yesu.
31 5. Azdabwera Iyenso
1. “SENZANI mtanda wanuwu.” Kudzatenga okhawo;
Atero Yesu Mbuyathu; Nyimbo tidzakaimbanso,
“Mukanditsata Inetu, Aleluya ndiye Yesu.
Mudzikanize nokhanu.”
2. “Senzani mtanda wanuwu.” 33
Musaopsedwe nawotu; 1. Unakhetsedwa mwazi dol
Mphamvu za Yesu nzanunso; Wa Yesu Mfumuyo,
Limba mtima wanuwo. Poweramira mutuwo
3. “Senzani mtanda wanuwu.” Pamtanda pakepo.
Bwanji manyazi mumva ’nu?
Yesu anapiriratu, Mbuye mthandiza inetu
Kuti mupulumuketu. Kukonda inidi,
Ndi kuli mpando wanuwo
Ndufuna kuzdako. Poona anthu amanyoza?
2. Zochimwa zanga zonsezo Onani umo apirira;
Wapachikidwa Ambuyathu.
Anaziferadi,
3. Anena mawu m’mtanda momwe
Chikondi chake chonsecho Mawu ochepa achifundo,
Sindingadziwe ayi. Apempherera ’dani ake;
3. Linadetsadi dzuwa bii, Wapachikidwa Ambuyathu.
Pakufa iyeyo 4. Mtima wangawe, uyenera
Kuduka ndi manyazi lero,
Pakumwalira indedi
Zamlasa ndi zoipa zako;
Wakundilengayo.
Wapachikidwa Ambuyathu.
4. Pokumbukira mtandawo 5. Ona chikondi cha Mulungu,
Wa mpulumutsiyu, Ona zoipazo za anthu,
Ndiphimba nkhope yangayi, Koma chakula ndi chikondi;
Ndi nsoni n’chitatu. Wapachikidwa Ambuyathu.
5. Zofuna zanga zosenzo 36
Za mutima wangawu 1. PAMTANDAPO Ambuyeyo
Ndipereka kwa inu, Anatifera ifetu,
Nakhetsa mwazi wakewo
Mundiweruzetu.
Kutiwombola tonsefe.
Pamtandapo, pamtandapo
34 Ambuye wanga ’nafatu;
1. KU Mzinda wakuyerawo Pamtandapo, pamtandapo
Wapachikidwa Mbuyeyo, Anandiwombolerapo.
Nasautsidwa Mbuyeyo, 2. Kwa munthu wosokerayo
Akatipulumutsa ’fe. Kudziko lakutaliko,
2. Padzanja lachifundolo Atero Yesu: “Bweratu
Linapenyetsetsa ’khunguwo, Ukhale nawo moyowo.”
Lachiza nalo nthendazo, 3. E! Yesu Mbuye wangadi,
Papyolatu msomaliwo. Ndipatsa Inu mtimawu;
3. Mapazi ake namvatu Ndithandizeni inedi
Zoŵaŵa zopambanazo, Ndisalekane nanu ’yi.
Napachikidwa kaamba ka 4. Zochimwa zanga zonsezo
Zoipa zathu zonsezi. Wandichotsera mwaziwo;
4. Ambuye, tikondweratu Mumtima mwanga muli mbee!
Kupulumutsa kwanuko; Mwayeretsedwa indetu.
Satana tisammvere ’yi
Komabe Mpulumutsiyo.
37
1. ZATHEDWA zonsetu
35 Za moyo wakewo,
1. TIYENI, dzalireni nane, Ambuye anatsikayo
Tidze ku mtanda wa Ambuye, Nafika pansipa.
Tionse tichitetu maliro; 2. Zintchito zakezi
Wapachikidwa Ambuyathu. Zofuna ’Tatewo
2. Kodi misozi itisoŵa, Anatsiriza zonsedi,
Sanazisiya ’yi.
3. Pa Iye padzapo E, mudzandimasula;
Chisoni m’mtimamo, Ndipenyetsetsa Yesu,
Mpweteko wonse wathuwo Ambuye Mfumu yanga,
Wa dziko lonseli. Ndikafa ndine wanu,
4. Pamutu minga kwe! Ndikhale nanu m’Mwamba.
Pamoyo wakewo 39
Zoipa zathu zonsezo,
1. POKUMBUKIRA mtandawo
Zinaikidwapo.
Ambuye ’nandiferapo,
5. Anandiferatu ’Ye,
Ndiyesa zingochepazo
Afera inedi;
Ndinazitama kalelo.
Athetsa nsembe zonsezi
2. Mndiletse ndisatame’yi
Ambuye Nsembeyi.
Zachabe, koma imfayi;
6. Pakugomedwapo Pa
Zijazo ndinakondazo
mlandu wangawo,
Ndazilekera mwaziwo.
Ndidzaitana Mbuyeyo
3. Onani m’mutu, m’manjawo
Andilanditsepo.
Mudzera nsoni m’mwazimo.
38 A! panalibe kalelo
1. A! MUTU wakuyera, Wondibvalira mingayo.
Wolaswa wachisoni, 4. Chinkana dziko lonselo
Abveka Inu anthu Lichepa ndithu mtulowo,
Ndi minga ya udani; Chikondicho chagwirabe
Ambuye mwafokatu Mtimanga, moyo, ndense ’ne.
Ndi masauko aja,
Mwatuŵa m’maso mwanu
40
1. LERO Kristu anauka, Aleluya.
Mumayerera kale.
Ndilo tsiku lokondwera. Aleluya.
2. Ambuye Mwini moyo,
Iye kale anafera, Aleluya.
Kokoma mnafumako;
Nawombola otaika Aleluya.
Ndizizwa pomva mawu
2. Timwimbire zomtamanda Aleluya.
Umo mwachitiramo.
Ndiye Kristu wa Kumwamba
Chisoni chija chanu
Aleluya.
Ncha pamachimo anga,
Natsikira kumanda, Aleluya.
Mwasaukira Inu
Nalanditsa akuipa. Aleluya
Kupalamula kwanga.
3. Koma masauko ake Aleluya.
3. Nditani! Bwezi langa
Anatiwombola ife. Aleluya.
Kulemekeza Inu
Ndiye Mfumu ya mafumu Aleluya.
Chifukwa cha chifundo
Mwana ndithu wa Mulungu.
Ndi imfa ija yanu?
Aleluya.
Mundikhalitse wanu,
4. Timwimbire Mulungu wathu,
Wokhulupira inu;
Aleluya.
Musandilole konse
Kuti atikonda ndithu: Aleluya.
Kufulatira Inu.
Mtamenso angelo inu, Aleluya.
4. Pakufa ine Mbuye
Ndiye ‘Tate, Mwana, Mzimu
Mukhaletu pafupi,
Aleluya.
Mundithandize ine,
41
1. NLA Mlungu dzuŵali: 43
Pa mbanda kuchapo
1. KONDWERANI dzuŵa lino,
Angelo ‘nadzatu
Aleluya.
Nachotsa mwalawo.
Yesu wanka m’Mwamba momwe:
Ndi mtima wonse mwimbedi,
Aleluya.
Wauka Mbuye leroli.
Wachokera m’dziko lino, Aleluya.
2. Akonda onsewo
Wabwerera kwawo komwe. Aleluya.
‘Nagwidwa manthadi
2. Zomkwezetsa zili m’Mwamba,
Poona zo’psyazo
Aleluya.
Zoonekerazi.
Zodikira Mbuye wathu; Aleluya.
3. Mulibe m’mandamu,
Mloŵetseni n’kumlambira, Aleluya.
Wadzuka Mbuyetu;
Mfumu yathu yaulemu. Aleluya.
Woposa imfayo
3. Yesu nkana saoneka, Aleluya
Ndi Mwini moyowu.
Atipempherera komwe: Aleluya.
4. Dzukani nayetu,
M’nyumba yake yokonzeka Aleluya.
Oyera inunso,
Atilinda ife tomwe Aleluya.
Lekani m’mandamo
4. Tiyamike Dzina lake, Aleluya.
Zakufa zanuzo.
Mfumu ya ulemu wonse. Aleluya.
5. Titama Yesuyo,
Tibukitse mbiri yake Aleluya.
Ambuye m’Mwambamo,
Pansipa padziko lonse. Aleluya.
Wofera anthu ’Ye,
Timkondakondako. 44
42 1. LAMBIRA, Mfumuyo,
Ndi Yesu Mbuyathu,
ALELUYA, Aleluya, Aleluya!
Tamvani nyimbo za ‘mithenga a
1. Nkhondoyo yatha, imfa yagonja,
Kumwambako;
Yesu wamoyo anaiposa,
Nafenso pansipa
Msampha woipa wonse nawonja,
Timyamikire ’Yo,
Aleluya!
Ndi Mpulumutsi wathu wotifera
2. Mphamvu za imfa ndi za Satana
kalelo.
Naye Ambuye zinalimbana,
2. Lambira Yesuyo
Komatu Yesu anapambana.
Wokonda tonsefe;
Aleluya!
Mabala ake achikondi aonekabe;
3. Atha masiku aja ansoni,
Tisaiwale ’yi
Mbuye wauka, ali ndi mboni;
Zoŵaŵa zakezo,
Lero chimwemwe, chatha chisoni,
Tileke kumchimwira, kumsautsa
Aleluya!
Yesuyo.
4. Nsinga za imfa Iye ’nadula,
3. Lambira Yesuyo,
Khomo la m’Mwamba, nalitsegula;
Uthenga wakewu
Yesu timtama tonse tipfuula,
Uyanjanitsa anthu onse m’dziko
Aleluya!
munomo:
5. Mbuye mabala anu olimba
Amaiŵala za
Atichotsera mantha a imfa;
Kudana kwawoko,
Tsono ndi mtima wonse tiiimba:
Nayamikira Mfumu yamtendere
Aleluya!
monsemo.
4. Lambira Mfumuyo
Wolenga zonsezi: Adzakudalitsa iwe,
Nyenyezi, dziko, dzuŵa, mwezi ndi Nadzaletsa tsoka lonse,
mitamboyi; Nadzakutsogoza kwawo,
Tikweze dzinalo Akondadi!
La Mbuye Yesuyo,
Timyamikire pansi pano ndi
Kumwambako. 46
45 1. Msandipitirire, Yesu,
1. YESU wakukoma mtima, Mundimvere ine;
Akondadi! Mukudalitsa ena,
Wakuposa mbale ndiye, Msandipitirire.
Akondadi!
Wina asautsa iwe, Yesu mbuye,
Pena adzasiya iwe, Khutu munditchere
Yesu sadzanyenga iwe, M’mene muitana ena
Akondadi! Msandipitirire.
2. Kumdziŵitsa ndiko moyo, 2. Ndigwadira inu, Yesu,
Akondadi! Musandikanize;
Akhumbira mtima wako, Ndizalapatu machismo
Akondadi Mbuye mndithandize
Mwazi wake ngwowombola, 3. Nkhope yanu ndifunitsa
M’chipululu akufuna, Sind’yenera konse;
M’khola mwake akusunga, M’mtima mwanga muchiritse
Akondadi! Nthenda zanga zones.
3. Akufuna kumdziŵitsa, 4. Yesu ndinutu chitsime cha
Akondadi! chimwemwe chokha,
Udzimpatsa moyo wako, Sindifuna wina konse,
Akondadi! Koma inu nokha.
Kodi umachita mantha?
Pena umadera nkhaŵa?
Yesu amasangalatsa, 47
Akondadi! 1. Idza wolema,
4. Bwenzi ndiye wakufera, Akupumitsa;
Akondadi! Womva chisoni,
Nthaŵi zonse sakusiya, Akutonthoza;
Akondadi! Mulendo limbika,
Anthu ena akunyenga, Mphamvu apatsa
Yesu sadzanyenga iwe, Amtisunga, yesu ambuye.
Zakubvuta adzachotsa, 2. Ndiye mtsamiro
Akondadi! Pogona ine;
5. Akhululukira iwe, Pofika kufa
Akondadi! Andidzutsanso;
Nadzainga mdani wako, Podzichepetsa;
Akondadi! Andikwedzanso;
Moyo wa moyo,
Yesu abuye.
3. Ndikakhumudwa Chikhala chosatha;
Andilimbitsa; Ndi mwaziwo
Ndikadzitama; Akhalatu Wansembe wanga Yesuyo.
Andichepetsa; 3. Mabala ajawo
Ndikasokera; A m’thupi mwakemo
Andilondola; Amukumbutsanso Za
E! wokondedwa ine pansipa;
Yesu Ambuye. Zoipazo
Achotsadi kotero sindingafe ’yi
4. Ndimachitira 4. Mulungu ali wokhulula
Inu umboni mtimatu,
Ndikukuzani Ndilibe mantha ’yi,
Moyamikira; Andisungiradi;
Mphamvu ndi nzeru Ndibwera kwa
Moyo, zonsezi, Atatewo, titayanjana leroli.
Si zanga, nzanu, 50
Yesu ambuye.
1. M’KHOLA mwa ng’ombe ku
Betlehemu
48 Anabadwamo Ambuyangayo;
1. MBUYE , mutsaganetu Etu, ndizizwa! natsikirako,
Nane ndingachimwenso; Kufuna inetu.
Nanu ndisungidwedi, Kufuna inetu, kufuna inetu,
Mwa chikondi chanucho. Etu ndizizwa! Natsikirako
Mbuye Yesu, Kufuna inetu.
Mundiperekeze inetu; 2. Popachikidwa pa Golgotapo
Ndine mlendo, Mbuye ‘Nu, Yesu anandiwombola ine,
Mutsagane nanetu Etu, ndidziŵa! Nakondetsadi
2. Inu mundibisadi Nafera inetu.
M’mene ndabvutidwamo, Nafera inetu, nafera inetu,
Ngati muli ndinedi Etu ndizizwa! Nakondetsadi
Bwino ndidzakhalamo. Nafera inetu.
3. Mbuye, mutsaganebe 3. Mbusa wokoma ndi Mbuyangayo,
Mpaka moyo watha zi! Nandiitana posokerapo,
Kwanu mundifitseko, Konse koipa nalondolako
Kwanu nsoni zathadi. Kubweza inetu.
49 Kubweza inetu, kubweza inetu,
Konse koipa nalondolako
1. E, MOYO wanga’we
Kubweza inetu.
Utsitsimuketu;
4. Uko kumwambako Mbuyangayo
Ambuye Yesuyo
Andikonzera mokhaliramo;
Akhala m’Mwambamo.
Tsiku linalo adzabweranso
Pampandopo
Kutenga inetu.
Akhalabe, natchula dzina langali.
Kutenga inetu, kutenga inetu,
2. Kwa Mlungu m’Mwambamo
Tsiku linalo adzabweranso
Amapempherako;
Chikondi chakenso
Kutenga inetu. 1. MBUYE Yesu adzabwera,
Asekere anthu onse;
51 Mawu awa achimwemwe
Azimveka m’dziko lonse.
1. Alinkuza wansoni munthu
Adzabwera, adzabwera;
Wakukhala kumwamba,
E! bwerani Mbuye wathu.
Alinkudza m’ulemelero
2. Dziko lino linaona
Ndi mwamuna wa mtanda.
Masauko a Mbuyathu,
Lidzaonanso ulemu,
Aleluya, aluluya
M’mene adzabwera Iye.
Alinkudza kwa ife;
Adzabwera, adzabwera;
Ndi chimwemwe ……………..
Timvomera, E! mubwere
Pakufika Ambuye.
3. Anthu anu amafoka,
2. Alinkudza Ambuye Yesu
Pa ulendo nasokera;
Wakuphedwa pa dziko,
Ha! Adzaonana nanu
Alinkudza kukhala mfumu
Atabvalanso zoyera.
Yoweruza maiko.
Mudzabwera, mudzabwera;
3. Pakufika asonkhanitsa
Inde Mbuyetu mubwere.
Anthu ake oyera;
4. Ndi chiyembekezo ichi
Adzafuna m’mitundu yonse
Sitikhala chete ife:
Omwe iye anafera.
Tiimbitsa nyimbo zathu
52 Zakulemekeza Mlungu.
1. PAKWITANA Mbuye wanga Adzabwera, adzabwera
Potsiriza dzikoli, E!! mubwere msanga YESU.
Pakufika tsiku la kuŵalalo, 54
Posonkhana akumvera,
1. YANG’ANANI, anthu onse,
Pakuona Yesuyo,
Yesu Mbuye wathuyo:
Ndidzakondwerera naye komweko.
Alinkudza ndi ulemu,
Pakwitana Mbuye wanga,
Kuoneka m’Mwambamo.
Pakwitana Mbuye wanga,
Anthu onse amlambire
Pakwitana Mbuye wanga,
Yesu Mwana wa Mulungu
Ndidzakondwerera naye komweko.
Alinkudza ndi ulemu
2. Potuluka m’manda mwawo
Wopambana, indetu.
Anthu ake onsewo,
2. Adzatenga anthu ake
Tidzasanganatu nawo nthaŵiyo.
Akumvera pansipo
Pakuuka osankhidwa,
Iwo adzakhala naye
Kunka naye Yesuyo,
M’dziko la Kumwambako.
Ndidzakondwerera naye komweko.
3. Koma anthu onse omwe
3. Tisaleke kugwirabe
Anamnyoza pansipo,
Ntchito ya Mulunguyo,
Nthaŵi Yesu alinkudza
Tibukitse mbiri yake m’dzikoli,
Adzaopa m’mtimamo.
Ndi podzatha moyo wathu
4. Ife tonse tikumbuke
Ndi zintchito zathuzo,
Mawu ake onsewo;
Tidzakondwerera naye komweko.
Timuyang’anire Iye,
53
Yesu Mbuye wathuyo. Nakweradi Kumwambako,
55 Nakhala Mfumu monsemo,
1. A MULUNGU, Ambuye wathu Mlunguyo.
Munatuma Yesuyo, 4. Adzadza indetu
Mwana wanu Yekhayo. Kudziko linoli;
2. Anabadwa, Tidzanka nayeyu
Anabadwa motere, M’ufumu wakedi.
Monga mmphaŵi m’kholamo. Momwemo tidzampenya ’Ye,
3. Anakonda Momwemo tidzakhala ‘fe
Anakonda anthuwo, M’kuŵala kwake koti mbee!
Naŵapulumutsanso. 57
4. Anafera, 1. Yesu, dzina lakukonda,
Anafera m’mtandamo, Lopambana onse ena,
Anafera ifenso. Tonse tidzaligwadira
5. Anadzuka Ndi mitima yochepetsa.
Anadzuka m’mandamo, 2. Yesu, dzina lokondwetsa
Anatenga moyowo. Akuipa a padziko,
6. Anakwera, Kale linatidziŵitsa
Anakwera m’Mwambamo Mpulumutsi ndiye Yesu.
Kwa Mulungu ’Tatewo. 3. Yesu dzina lakufatsa,
7. Adzabwera, Anamutcha ’kali Mwana,
Adzabwera Iyeyo M’mene analoŵa kale
Tsiku lomalizalo. M’dziko lino lakudana.
8. Aleluya, 4. Yesu, dzina ndi lomweli
Aleluya Yesuyo, La pa dziko lino lonse,
Tizitama dzinalo. Ndi lamphamvu yolanditsa
56 Anthu mu masoka onse.
1. IDZANI nonse ’nu 5. Yesu, dzina lakukonda
Okonda Yesuyo; La Mwanayo wa Mulungu,
Libuke Dzinali, Ife anthu osauka
Tithaŵira nalo kwanu.
Timtame konseko.
Uzani onse m’Mwambamo, 58
Uzani onse pansipa, 1. Inde ndifuna kumvatu
Wafera Iye anthuwo. Za chikondano chakecho
2. Waleka kronayo, Cha Yesu mbuye wangayo
Nasiya ’Tatewo, Zomwe anmva kalelo.
Natsika m’Mwambamo,
Nalira, nafatu. E! zina za Yesu
Zoŵaŵa zake zonsezo E! zina za Yesu
Nazimva, zinaposatu Inde, ndirira m’mtima
Kuti tipulumukedi. Chipulumutso chakecho
3. Nadzuka m’mandamo
Moopsya m’mdimamo, 2. Zina za Yesu Ndimvetu,
Nigonja imfayo Kuti ndichite zakezo;
Ndi mdani waketu;
Mzimu woyera, mudzetu 2. Ndinasokera kalelo,
Ndiphunzitseni zonsezo. Ndamkana Iye Yesuyo,
3. M’mawu a Yesu mbuyeyo, Koma ndiimba leroli:
Inde, acheza nanemo; Wandiwombola inedi.
Liu ndimamva m’bukumo 3. M’mtima ndimakondweramo
Ndilo la Yesu Mbuyeyo. Popenyetsetsa Yesuyo
4. Zina za Yesu m’mwambamo Pamtanda pake pomwepo,
Ali pampando pakepo; Pakundifera inenso.
Udze ufumu wakewo, 4. Sizitha ntchito zangazo
Ndiyetu Mfumu ponsepo Kundiyeretsa m’mtimamo;
59 Anandiyesa inetu
Wakulungama Yesuyo.
1. Wina atikonda ife,
5. Tsono mubwere inunso;
Bwenzi lathu ndiyeyu,
Mtetezi wanu ndiyedi.
Atifunafuna ife,
Apulumusa onsewo
Inde nthawi zonsetu.
Akumkhulupiriradi.
Chikondano chakechi
Nchachikulukuludi 61
1. Konda dzinalo la Yesu,
2. Ndani mwa abale athu Mwana wosauka iwe;
Angatifere ife? Ndilo lothandiza anthu;
Koma yesu m’malo mwathu Khala nalo ponse phee.
Anapachikidwatu
3. Anamnyoza pansi pano, Dzina la Yesuyo
Bwenzi la ochimwawo; Nlokondetsa onsewo,
Mu’ulemerero wake M’mwambamo, ponsepo
Alizonda Dzinali. Litonthoza m’mtimamo.
4. Timchimwira kopambana,
Ndi kumsautsa iye, 2. Konda dzinalo la Yesu
Koma Bwenzi lathu Yesu M’moyo mwakomo
Atikondakondabe. M’mene ulikuyesedwa,
5. Mtiphunzitse, mbuye Yesu, Tchula Dzina lakelo.
Tikondane nanutu; 3. Dzina ili ndi lokoma
Tisaiwalire konse La mtetezi wathuwo;
Bwenzi lathu ndinutu. M’mene adzatilandira
M’mwamba, tidzakondwa.
60 4. Mbuye Yesu timtamanda
Ndi nyimbo zathuzo;
1. NDITAME Mlungu m’mtimamo,
Mfumu ya ma mfumu onse
Wakundifera pansipo,
Yesu timavesadi.
Nafafaniza tchimolo,
Nanditengera dipolo
Wandiwombola inetu 62
Pokhetsa nwazi wakewo; 1. KHAMULO liliko
Timlemekeza Iyetu Kumwambako mbuu!
Wotilipira dipolo. Pakukhala ndi Yesu
Aimbirako: Mbveke Mbuyeyo!
“Kwa Iye atikonda 64
Natsuka ’fe mbuu!
1. MUBWERE Mzimu Wakuyera,
E! kukhale ulemu
Kuyatsa moto m’mtima mwathu;
Kwa Mbuyathuyu.”
Ntchito ndi yanu kudzozera
2. Onsewa ’nachimwa
Ndi kutininkha mphatsozo.
Nadetsedwa bii,
2. Kudzodza kwanu kutipatsa
Nthaŵi yino ayera
Chimwemwe, moyo ndi mtendere;
Naimbiradi:
Kuŵala kwanu kupenyetsa
3. Akhala mafumu
A m’mdima ndi a m’ndendemo.
Kwa Mbuyathuyo,
3. Mtima wodetsa mukonzere,
Anawombola onse
Chisomo chanu chakwanira;
Ndi mwaziwo pyu!
Adani athu muthaŵitse
4. Akadakhalabe
4. Mutidziŵitse ‘Tate wathu, Ndi
Osaukako
mwana wake ndinu Mmodzi.
Ngati Yesu sakana-
Mnafuma kwa aŵiri onse,
Wombolatuwo.
Koma Mulungu Mmodziyo.
5. Ndi nyimbo yabwino
Tidzamtamako, 65
Kuti ena pakumva 1. MZIMU Woyera, mudze mumitima
Amwimbirenso: mwathumo,
“Kwa Iye atikonda Mufike nazo mphamvu zanu zazikuluzo.
Natsuka ’fe mbuu! 2. Mufike monga nyali younika
E! kukhale ulemu m’mtimamo.
Kwa Mbuyathuyu.” Mutidziŵitse zakuipa zakukhalamo.
63 3. Mufike monga moto wakuotcha
zomwezo.
1. TAMANI mphamvu ya Yesu,
Mutiyeretse ifetu m’mitima mwathumo.
Angelo agwade;
4. Mufike monga ngati njiŵa
Tulutsanitu korona,
yamtenderewo.
Mumbveke, mbveke, mbveke,
Kutitu anthu anu onse akondanetu.
Mbveke Mbuyeyo!
5. Mufike monga ngati mphepo
2. Inu osankhidwa ake,
yokokomayo,
Owomboledwa ’nu,
Tikhale tonse nazo mphamvu zanu
Tamani Mpulumutsiyo,
zonsezo.
Mumbveke, Mbveke, Mbveke,
Mbveke Mbuyeyo! 66
3. Anthu onse ndi mitundu 1. MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine
Pa dziko linotu, E, ngati mvula m’dziko lakuuma,
Amlemekeze Mfumuyo. Ndikhale munda wanu wakupatsa
Mumbveke, mbveke, mbveke, Zipatso zoyenera Mbuyeyo.
Mbveke Mbuyeyo! 2. Mphunzitsi, ndinu mudziŵitse ine
4. Tifuna kuti komweko Chikondi chanu chija chachikulu;
Tikamgwadire ’Ye; Lembani mawu anu pamtimanga,
Tidzaimba kosaleka: Kuti ndikhumbukire zanuzo.
Mumbveke, mbveke, mbveke,
3. Wosangalatsa, ine ndikalira A Mbuyathu Yesu.
Muchotse nsoni, m’mtimamo mudikhe; 3. Mtitsitsimutse ife
Mundigoneke pachifuwa chake Kuchotsa nkhaŵa zathu,
Cha Yesu kuti ndikakondwepo. Muyatse moto wachikondi
4. Wotsogolera, munditsogolere Mu mitima yathu.
Kuti n’kafike kwawo kwa Atate, 4. Mtitsutse titachimwa
Nditsate Yesu ndikuyendayenda kutilapitsa m’mtima,
M’njira yomweyo anapondamo. Mwonetsenso chikondi chokhululukira
5. Mthandizi ndinu, mndithangate ine tchimo.
Kupempha bwino izo zindisoŵa. 5. Kutiyeretsa m’mtima
Kupempha monga Mlungu amafuna Ndi ntchito yanu yokha,
Kulingalira zake zokhazo. Kupatsa moyo watsopano
6. Mzimu Woyera, n’dzipereke ndense, M’mene timafoka.
Mundichitire ntchito yaikulu; 6. Mukhale m’kati mwathu,
Mtima woyera ndi womvera mpatse, Mutichotsere mantha,
Wodzala ndi chikondi chanucho. Tidzayamika ’Tate wathu,
Mwana wawo ndi ’Nu.
67
1. MPUME pa inetu, Mpweya wa 69
Mulungu, 1. IDZANI, Mzimu Inu,
Ndi kundidzaza moyo wanuwo, Mundidalitse kuno;
Kuti ndikonde zomwe mukondanso, Ndafoka mtima ine
Ndichite chomwe mumachitanso. Polendo wanga uno;
2. Mpume pa inetu, Mpweya wa Kwambiri ndakhumudwa
Mulungu, Panjirayo ya moyo;
Mpaka mtimanga ukayeretu, Mkaleka kutsogola
Ndipo zokhumba zanga zilingane Ndiwonongeka pompo.
Nazo zanuzo zakuyera mbuu! 2. Wakunga mwana ine,
3. Mpume pa inetu, Mpweya wa Sindidziŵitsa konse;
Mulungu, Mundilangize Mzimu
Mpaka ndikhale wanu nokhatu; Panjira yanga yonse;
Ayeretsedwe makhalidwe anga Mundiyendetse bwino
Ndi mphamvu yanu yondisunga nji! Ndifike ine ndemwe
4. Mpume pa inetu, Mpweya wa Panjira yolungama,
Mulungu, Kudziko lachimwemwe.
Kuti inedi ndisafe ’yitu, 3. Mundilimbitse m’mtima
Koma ndikhale nanu m’moyo womwe Pogwira ntchito izi;
Wangwiro ndi wa nthaŵi zonsetu. Ndikapumula pena
Mukhale ndithu ndine;
68 Zolingirira zanga
1. MUBWERE Mzimu Inu
Ziyere zonse m’mtima
Woyera wakufatsa,
Zoipa muzichotse,
Muchotse mdima m’mtima mwathu
Sindidzazichitanso.
Tikapenye m’maso.
2. Mtisangalatse m’zonse, 70
Ndi wachifundo Inu, 1. MZIMU Woyera, mudzetu,
Tiyembekeze kumapazi
Tiyeretsedwe m’mtimamu; Atipatsa ife makhalidwe
Mupatse anthu anuwa Ofanana naye Yesu,
Mitulo yanu yonseyo. Anatsika kumwambako.
2. Kudzoza kwa Kumwambako
Kutitonthoza m’mtimamo, 2. Naye mzimu mndiphunzitsekuko
Ndi kutidzutsa m’moyomu, Kukondwera nsiku zones
Tikhale okondanatu. Ndi kukhara ndi mtendere
3. Pankhope pathu mthirepo Osadaratu nkhawa ayi!
Chisomo chanu chijacho; 3. Mndithandize kukondana
Mtendere mutininkhebe, Ndi kuthangatira onse
Mutiyendetse ponse phee! Ndi kukhululukirabe
4. Tionetseni tonsetu Akundichimwirawo.
Umodzi wanu wonsemo, 4. Mndirimbitse ndipirire
Atate, Mwana, Mzimu ’Nu Osadandaura konse,
Tiimbe Nthaŵi zonsezo: Ndi kulamulira thupi
Titamire Nthaŵi zonse Ndi zofuna zakezo.
’Tate, Mwana, Mzimu, Nonse. 5. Kudzirala ndi kufatsa,
Amen. Inde, zonse muzikonda,
Mndiphunzitse pondipatsa
71 Mzimu wanu woyerawo.
1. MUBWERE kuno Mzimu ’Nu
Chitsime cha chikondicho; 73
Mudziŵa ndimaliratu, 1. MBUYE, Mawu anu
Mukhale m’mtima mwangamo; Atikondweretsa,
Ndipatsa inu mtimawu, Atitsogolera,
Masiku onse mkhalemu. Salephera konse.
2. Mukonze mtima wangawu, 2. Poyesedwa ife
Muyere ndithu m’katimo; Atipambanitsa,
Ndilinda tere, Mzimu ’Nu, Natonthoza mtima
Mupatsetu chikondicho; Natipulumutsa.
Lichepa dontho lokhali, 3. Tikaona bvuto
Ndipempha mundidzazedi. Tikaloŵa m’dima,
3. Ndilira Mzimu leroli, Kuunika kwake
Mutsimikize Mawuwo; Kusonyeza njira.
Ya Mbuye Yesu mphamvuyi, 4. Atisangalatsa,
Ikhale yathu, yanganso; Atilemeretsa
Muloŵe m’mtima, mdzazetu Poŵerenga mommo
Ndi mphamvu, nzeru, moyowu. Nawo mtima wonse.
5. Ndiwo alimbitsa
72 Omwe akufooka,
1. Mbuye wondipulumutsa Naŵapatsa moyo
Akufuna kufa.
Mulandire mtima wanga,
6. Mbuye, mtiphunzitse
Mwandipatsa mzimu wanu
Womeretsa zipatsomo. Nzeru zake zonse,
Tikayenderane
Ndiye mzimu wakuyera
N’tiyanjane nanu. 2. Mkate wamoyowo
Ndinu Ambuye;
74 Mawu oyera anu n’khumbanso,
Mun’dyetse onsewo
1. Cholimbitsa mtima ndi
Ndikhale moyo,
Chonditsogolera
Ndikonde zakuona zanuzo.
M’njira ya Mulunguyo,
3. Mtume tsopanoli
Ine ndili nacho.
Mzimu Woyera,
Kuti andikonzere m’masomo;
M’Bukuli ine ndi
Abvumbulutse zinsinsi za m’Mawu,
Onse owerenga
Kuti ndionemo Ambuyeyo.
Mawu a Mulunguwo,
4. Mndidalitsire ’ne
Timapeza moyo
Mawu amoyo,
Monga munadalitsa mkatewo;
Ndikhale mfuludi,
2. Dzinthu zakumundazo
Wosamangika,
Zilimbitsa thupi
Mukhale moyo wanga wonsewo.
Zolembedwa m’Bukumo
Zimadyetsa mtima.
3. Ndikachimwa, Bukuli 76
Lindiyambotsutsa 1. MBIRI yakalelomwe
Limanditonthoza ndi Mundisimbiretu
Mau a mtendere. Ya Yesu Mbuye yemwe
4. Pakudera nkhawa ine, Anandiferatu.
Pakuchita mantha, 2. Simbani bwinobwino -
N’kawerenga m’Bukuli Ndilibe nzeru ’yi -
Lindipatsa mphamvu. Ndimve tsopano lino
5. Lindionetsela ‘ne Mbiri ya moyowo.
Chifuniro chake Mbiri yakalelomwe,
Cha mbuynga Yesuyo, Mbiri yakalelomwe,
Ndikamvera bwino. Mbiri yakalelomwe
6. Zonse mwazilembamo, Mundisimbiretu.
Mzimu wakuyera, 3. Mawu amveke bwino,
Kuzimvera zonsezo Aloŵe m’mtimamo,
Mundithangatire. Ndizindikire tsono
7. M’Buku lakuyerali Chipulumutsocho.
Powerenga ife, 4. Simbani mobwereza,
Mbuye mutipatsemo Ndisaiŵale ‘yi
Moyo, moyo, moyo. Koma ndisunge bwino
Mumtima Mbiriyi.
75 5. Simbani Mbiri yonse
1. MUNDINYEMERE ’ne
Ya Mbuye wangayo;
Mkate wamoyo
Zochimwa zanga ndizo
Monga kunyanja kuja kalelo;
Zinapha Yesuyo.
Ndipyola Mawuwo,
6. Simbanitu mwachete
Ndifuna Inu,
Mbiri ya Yesuyi,
Ndikhumba Inu mwini moyowo.
Pakubvutidwa ine 2. Musachitenso nthantha ’yi,
Inditonthozepo. Mufulumire inutu;
7. Simbani Mbiri yomwe, Tsiku labwino nleroli,
Ndikhulupiredi, Mulandirenso moyowu.
Kuti pakuyesedwa 3. Zokondweretsa m’dzikomu
Ndipulumukepo. Nzosakhutitsa m’mtimamu,
8. Inde, pakufa panga Koma za Yesu zonsezo
M’maso mukhale mbee! Zikwaniritsa inudi.
Mbiri ya Mbuye wanga 4. Sakukanani Yesudi,
Mundisimbirebe. E, mukalapa m’mtimamo;
77 Lolani kuti Mzimuyo
Agwire ntchito zakezo.
1. Kodi ulikulemedwa
Ndi zoipazo? 79
Idza kuno, ati Yesu, 1. PAKUPEMPHA ife pano,
Pumako. Pakwitana ’Tatewo,
2. Ndikamzindikira ninji Pakudziŵa tsoka lako,
Mbuye wangayo? Bweratu kwa Mbuyeyo.
Ali ndi mabala m’manja Idzatu, idzatu
Mwakemo. Kwa Mbuyathu Yesudi
3. Kodi ali ndi chilemba Idzatu, idzatu,
M’phumi mwakemo? Iwe bwera leroli.
E, chilembacho chaminga 2. Unachimwachimwa ndithu,
Chilimo. Wasokera m’talimo
4. Ndikampeza, ndikamtsata Unachedweranji kudza
Ninji pansipa? Pakulinda Yesuyo?
Masauko ndi misozi 3. M’dziko lino pansi pano
Zilipo. Sungapeze kanthumo
5. Ndikamfunafuna Iye, Kokwanitsa mtima wako;
Ndipezenjiko? Bweratu kwa Mbuyeyo.
Kumaliza kwa chisoni 4. Bvumbulutsa zonse zako
Chonsecho. Zobisika m’mtimamo;
6. Ndikampempha anditenge, Ayeretse moyo wako
Akataniko? Nawo mwazi wakewo.
Ati Yesu, “Idza msanga, 80
Idzatu.”
1. MIPINGO iyo idzatu,
78 Yoyenda mangu pajapo,
1. MUSAŴALOLE mawuwo Afuma kuti anthuwo?
Apite ngati mphepozi, Afika bwanji komweko?
Musaumitse mtimatu, Anena anthu onsewo,
Polira Yesu Mbuyedi. “Yesu Sing’anga apitapo.”
Idzanitu, idzanitu, Anena anthu onsewo,
Idzani kwa Ambuyeyo. “Yesu Sing’anga apitapo”
Idzanitu, idzanitu 2. Azizwa anthu ajawo,
Apulumutse inunso. Nafunsa, “Ndani mlendoyo?
Wanzeru monga Iyeyo
Kulibe wina konseko.” 4. Anathera pamtanda zintchito
3. Ndi Yesu yemwe kalelo zonsezi
’Nakhala munthu pansipa; Zowombola mizimu yathuyi,
Anthenda onse nthaŵiyo Ndipo yense akadza
Nachira yake mphamvuyo. mokondwakondwadi
4. Afika Yesu leroli, Moyo apeza kwa Yesuko.
Chifundo m’mtima mwakemo,
Timfitse msanga kwathuko
82
1. AMBUYE wathu Yesu
Akhale nafe ponsepo.
Akhala Mfumunso;
5. Timsankhe Yesu Mbuyeyo,
Zoipa zazikulu
Timyese Mfumu yathuyo,
Azigonjetsa ’Ye;
Chifukwa tikamkanatu
Anena mawu ake
Tikhala otayikawo.
Ochotsa zonsezo,
Tsopano inu ’dzanitu,
Kalelo nalamula:
Asanapitirirepo.
Pakhala bata duu!
Tsopano inu ’dzanitu,
2. M’ulemerero mwake
Asanapitirirepo.
Anenanenabe:
Munkhondo apambana
81 Ndi mawu akewo.
1. Ukapenya kwa yesu uliko Akristu akondwera
moyobe, Poona mphamvuyo
Inde, moyo tsopanopanotu; Ya Mbuye wathu Yesu
Olakwira upenye kwa Yesu Wotiwombolayo.
mbuyeyo, 3. Zobvala zake zonse
Kuwombola naferatu ‘we. Nza mwazi woti pyu!
Pamphumi pake pomwe
Ona! Ona! Anatu! Korona waketu.
Kuli moyo kwa yense apenya Unyolo wa Satana
yesuyo Umasulidwako;
Wakuferatu pamtandapo. Kumwamba amithenga
Atama Mbuyeyo.
2. Anasenza pa bwanji uchimo 4. M’kufatsa kwake komwe
wonsewo Anena nafenso,
Ngati wanu pa Yesu sulipo? Tonsefe omangidwa
Bwanji mwazi wakhetsa kutsuka Ndi zakuipazi;
ifetu, Ambuye amanena
Ngati uwu sutikwanako. Zotichenjezazi:
3. Zilepheradi zonse kugula Ananu, msiye zonse,
moyowu, Mupulumuketu.
Koma mwazi wa Yesu mbuyeyo. 5. Chikondi cha Mbuyathu
Khulupira mwa phamvu ya Chiposa zonsetu;
mlungu wathuyu. Chisomo chake chomwe
Nuyeretsa ‘we m’timakoma Chikondweretsabe;
Ulemu wake wonse
Umapambanadi;
Tiyeni, tikondwere Akuti anthu akumvera
Popita m’Mwambamo. Yesu aŵapulumutsa,
Inde, aŵapulumutsa, indetu.
83 85
1. SING’ANGA ‘mkulu ndiye Yesu, 1. OKOMA ndiwo mawu
Mwana wa Mulungu; A Yesu Mbuyeyo,
Asangalatsa achisoni, Wopatsa ife anthu
Ali wachifundo. Mtendere wakewo.
Kwa ife akumvera
Dzina la Yesu ndi lokoma, Kulibe mantha ’yi;
Dzina la Yesu lipambana, Timamva liu lake
Dzina lake lakukonda, Lingoti, “Mudze ’nu.”
Yesu, inde Yesu. Inu akutopawo
2. Zoipa zakhululukidwa, Yesu aitana ’nu;
Yesu amatero; Mudze kwa Ambuyeyo,
Tiyende bwino mnjira yake, Mudze msangatu.
Tilowemo lero. 2. Mukana Iye bwanji,
3. Nditama nsembe ya mulungu, Wokoma Bwezilo?
Ndilandira Yesu; Mutsate Yesu yekha,
Ndikonda dzinalo labwino, E, mpaka imfayo.
Dzina lanu Yesu. Mwafoka osokera,
4. Akulu inu mbwere nonse, Mwadetswa nazozi
Ana inu nomwe, Zoipa mwazichita;
Ambuye akuitanani; Mumvere Mbuyedi.
Bvomerani nonse. 3. Ambuye, musendeze
Pafupi nafedi,
84 Timvetse Inu msanga,
1. UTHENGA wa Mulungu
Poyenda m’dzikoli.
Waloŵa m’mtimamu,
M’ulendo m’moyo uno
Wochotsa zakuipa
Titsate Inutu;
Zakundidetsazo.
Kumwamba mutifitse,
Pakuti anthu akumvera
Tidzamve: “Idzani.”
Yesu aŵapulumutsa,
Ine, aŵapulumutsa, indetu.
2. Ndidziŵa kuti Yesu 86
Anafa kalelo, 1. Inu nonse obutidwa,
Nafafaniza zonse Mbuye alipanopa;
Tinazichimwazo. M’maso mwanu muli msozi;
3. Satana ndi unyolo Dzani kwa Mbuye wathuyo.
Anandimanga nji!
Ambuye Yesu yekha
Nandimasuladi. Yesu ngwachifundodi
4. Ambuye muloŵetse K! wafera inutu,
Mtendere m’mtimamo, K! wafera inutu.
Ndimvetse mawu anu
Masiku onsewo.
2. Yesu ndiye bwenzi lanu, Idza msanga ’we,
Ali wachikondicho; Adikira iwenso;
Kodi inu mumkanabe? Wachedwatu.
Mlape msanga m’mtimamo. 2. Iwe afuna,
3. Pena imfa idza mawa, Inde, kalelo;
Manda ali mfupimo; Leronso adika
Nthawi yino niyabwino, Mbuye wathuyo.
Mlole Yesu m’mtimamo. Uza Iye zonse
4. Ndi angelo akumwamba Za uchimowo;
Anke ndi uthengawo Yesu ati leroli:
Kuti wina adza lero “Wachedwa ’we.”
Kwa mbuyathu yesuyo. 3. Yesu alindira,
87 Inde, iwetu;
Idza ndi kukhala
1. Wochimwa iwe bweratu
Ndi chimwemwenso
Kwa Yesu mbuyeyo;
Ndi mikono yake
Atero iye; pumatu;
Yachikondiyo;
Umvere mawuwo.
Sankha Iwe msangatu;
Wachedwatu.
Khulupira mawu onse
A mbuyeyo;
Ulinawo pakumvera 89
Inde, moyowo. 1. Lero lino mbale wanga,
Ndilo dzuwalakukoma;
2. Ambuye Yesu anatsira Talandira mpulumutsi
Mwazi wake pyu! M’mene ali kuitana.
Ubire m’mwazi omwewo, 2. Lero lino mbale wanga,
Uyereyere mbuu! Usazengereze ayi;
3. Wamoyo ndiye Yesudi, Ngati ulindira Yesu
Nzoona zakezo; Lero udzachita mwayi.
Akhala iye njiratu 3. Lero lino ndi la bwino;
Yofika m’mwambamo. Moyo wako ulinawo;
4. Tiyeni tonse, tinkeko Pena mawa umwalira,
Ulendo wakewo Uzdatani mlandu wako?
Mudziko lake m’mwambamo, 4. Lero lino mbale wanga,
Tikhale nayeko. Lapa mtima, lapa tchimo,
88 Yesu adzakulandira,
Ukapempha lero lino. 5.
1. YESU ndi wokonda;
Ndiwe mlendo lero lino,
Ati “Idzatu,
Mvera ndikupepha iwe;
Yense wakufuna,
Yesu mwana wa Mulungu
Bwera msangatu.”
Akufuna ndithu iwe.
Ali wachifundo
6. Inde, lero lino Yesu
Ndi wamphamvunso
Aitana inu nonse.
Nthaŵi zonse Yesuyo
Landirani Mpulumutsi,
Alindatu.
Musazengereze nonse.
Yesu akukonda,
90 Ungamvetu Kumwambako,
“Akusowanso malo.”
1. PENYETSETSA Yesu,
2. Wina panalibe
Mtima wosauka;
Kumlandira Iye,
Anafera iwe,
Wakumsangalatsa,
Idza, nupumule.
Wamkonda nasowa.
Iye anachotsa
Anthu sanafuna
Nsoni ndi zoipa;
Chuma chosatha,
Penyetsetsa Yesu,
Sanamkondweresa,
Ndi kukhulupira.
Malo unalibe.
2. Penyetsetsa Yesu
Likatentha dzuŵa; 92
Yachuluka ntchito, 1. ATATE,’nu, atate ’nu,
Mphamvu idzakula. Mverani Ambuye.
Akonzera kwawo Khulupirani kuti mukaloŵe
Nyumba zokhalamo; m’Mwambamo,
Penyetsetsa Yesu, Khulupirani kuti mukaloŵe
Mtsatetu tsopano. M’Mwambamo.
3. Penyetsetsa Yesu 2. Amayi ’nu, amayi ’nu
Pogwirana nawo; Tsatani Ambuye.
Nkhondo ikabvuta 3. Abale ’nu, abale ’nu,
Tamva Mbuye wako. Kondani Ambuye.
Achuluka ’dani, 4. Alongo ’nu, alongo ’nu
Iwe ungofoka; Kondani Ambuye.
Penyetsetsa Yesu, 5. Abwezi ’nu, abwenzi ’nu,
Mantha adzachoka. Tamani Ambuye.
4. Ndipo pakuloŵa 6. Oipa inu nonsetu,
M’dziko la Kumwamba, Mverani Ambuye.
Udzapeza komwe 93
Onse adzatama.
1. NDICHITENJI kukapeza
Mwa zoŵala zija
Moyo? thandizeni!
Za Kumwamba kwawo,
Ndili wakutopa; Mzimu,
Udzapenya maso
Muthandize ine.
Yesu Mbuye wako.
Zonse zinathedwadi;
91 Yesu watha zonsezo;
1. MALO anachepa, Sutha ntchito, ungomvera
Nyumba anammana, Mawu ake omwewo.
Agona m’modyera, 2. Iye anatsika m’Mwamba,
Mutu paudzuwo. Anachoka kwawo,
Anthu sanamtama, Anafera anthu, nati:
Nyimbo panalibe, “Ndatha zonse zawo.”
M’nyumba ya alendo 3. Mbuye wanga ndilikumva,
Malo munalibe. Ndikondana nanu;
Apempha malo Ambuye; Umapuma mzimu wanga,
E, mlandiretu m’mtimamo, Kwathu ndiko kwanu.
94 1. YESU ponong’oneza, idzanitu;
Mupempherera ife, idzanitu;
1. KODI mwalandira Yesu?
Njabwino nthaŵi yino, idzanitu,
Iye anakuferani.
Yodziŵa Mpulumutsi, idzanitu.
Afunitsa inu nonse;
2. Tulani zoipazo, idzanitu;
Kodi mumufunanso?
Yesu adzatha zonse idzanitu;
Kodi mufunatu Yesu?
Olema ndi ochimwa, idzanitu;
Bvomerani msangatu:
Sakambukira izo, idzanitu.
“Inde Yesu ndifunadi,
3. Imvani mawu ake, idzanitu;
Ndinu Mbuye wangatu.”
Mudzalandira dalo, idzanitu;
2. Nthaŵi zonse mufunabe
Nacho chisomo chake, idzanitu,
Zinthuzo za pansi pano;
Yesu alinda inu, idzanitu.
Koma munyozabe Yesu
4. Mverani Iye ati: Idzanitu
Wopachikidwa kalelo.
Tiyeni mudzamwone, idzanitu;
3. Yesu akuitanani
E! akuitanani, idzanitu;
Kwanja kwake kwakukulu;
Ife tibvomereza, Tibweratu.
‘Mvani mawu ake lero,
Musachite nthantha ’yi 97
4. Imfa idzafika msanga; 1. IWE tiye, iwe tiye,
Ndipo mdzaikidwa m’manda; Tiye tsopanoli;
Nthaŵi yomwe simudzamva Pano tiye kuti Yesu,
Kutitana kwakeko. Tiye tsopanoli.
95 (Ndaima pano, ndaima pakhomo!
Loŵa, loŵa, loŵa, loŵa!
1. ’MVANI liu lomwe
Ndaima pano, ndaima pakhomo!)
M’khutu mwakomo,
2. Akukonda, akukonda,
Alikuitana
Tiye tsopanoli:
Mpulumutsiyo:
Pano akukonda iwe,
“Undipatsetu
Tiye tsopanoli.
Mtima wakowo;
3. Akupeza, akupeza,
Ndinakuferau
Tiye tsopanoli;
Kalekalelo.”
Pano akupeza iwe,
2. Ati: “Undiuze
Tiye tsopanoli.
Nsoni zakozo;
4. Salephera, salephera,
Ine ndidzachotsa
Tiye tsopanoli;
Zonse zomwezo.”
Pano salephera Iye,
3. Kodi ukafuna
Tiye tsopanoli.
Kupumulatu?
5. Mvera Yesu, mvera Yesu,
Yesu aitana:
Tiye tsopanoli;
“Udze kunoku.”
Pano mvera Yesu iwe,
4. Tula mtolo wako
Tiye tsopanoli.
Pali mtandapo,
6. Aleluya, aleluya,
Akaunyamula
Aleluya, Amen;
Mpulumutsiyo.
Aleluya, Aleluya,
96 Aleluya, Amen.
98
1. Tadza kukudyaku, Wotifera kalelo.
Kwakonzedwatu; 100
Mkate wamoyodi, idyatu ’we;
1. YESU wathu Mbuyeyo
Bwera wochimwanso,
Alandira onsewo
Yesu adikatu,
Akuipa omwewo,
Akuitanaku; mvetsatu ’we
Osokera m’talimo.
2. Tadza kumtsinjeku
Imba kaŵiri ndi kaŵirinso,
Wa moyo weni,
Yesu Ambuye sakanatu,
Chiza zoŵaŵazo za m’mtimamo;
Mvetsa Uthenga Wabwinowo,
Mtsinje wodzalawo,
Wakukchimwa adzatu.
Wokwaniratuwo
2. Idzatu kwa Yesuyo,
Yesa sakana ’yi; idzatu ’we.
Apumitsa inunso,
3. M’dzina la Yesuyo
Inde m’mtima mwanumo
Pemphatu iwe,
Ndi mtendere wakewo.
Iye adzamvatu, dikirapo.
3. Walandira inetu
Wamphamvu Mlunguyo,
Tsiku lija kalelo,
Ndiye apatsatu,
Wanditsuka ine mbuu
Dalo labwinolo; idzatu ’we
M’mtima mwanga momwemo.
4. Yamba ulendowo
4. Wandifera Yesuyo
Wonka Kumwamba;
Pansi pano kalelo,
Pano mpoipatu padzikoli;
Sindiopa mlanduwo
Komwe tikondwako,
Pakubwera Iyeyo.
Tidzasekeranso;
Tinke Kumwambako; idzatu ’we. 101
99 1. A! MBUSA wathu amvatu
Uko kuchipululuko
1. MWAMVA Mawu a Mulungu;
Zilira nkhosa zakezo,
Mukabvomeranjiko?
Zili kuthengo kunjako.
Kodi musandula mtima
Bwezatu, bwezatu,
Ndi kumvera Yesuyo?
Bwezatu zonse m’moopsyamo;
Bvomerani, Bvomerani
Bwezatu, bwezatu
Bvomerani msangatu,
Bweza zakezo kwa Yesu
Musazengereze ayi,
2. Ndani afuna kunkako
Landirani Yesuyo.
Kukazipeza nkhosazo?
2. Munachita nthantha kale,
Ndani adzathandizako
Musazengereze ’yi;
Kuti zifunde m’kholamo?
Yesu akulindirani,
3. M’tali mutali m’phirimo
Sadzakana inu ’yi.
Mvetsa, zilira nkhosazo; A!
3. Musaope pokumbuka
Mbusa wathu atitu;
Zakuipa anuzo;
“Bweza zothodwa m’kholamo.”
Khulupilirani Yesu,
4. Etu, zilira konseko
Adzachotsa zonsezo
Zili m’phiri moopsyamo.
4. Perekani mtima wanu
Imva, anena Mwiniyo:
Kwa Mulungu wathuyo;
“Kweye, upeze nkhosazo.”
Khulupirirani Yesu,
102 Laleka ndithu ludzulo,
Tsopano moyo wadza
1. Thanthwe long’ambikatu,
5. Ambuye naitana ’ne;
Ndibisale momwemu!
“La dziko ndine Dzuŵa,
Madzi ndipo mwaziwo
Yang’ana Ine, kwacha ’we,
Zotuluka mthitimo
Wachoka mdima uja.”
Zinditsuke m’mtima mbuu!
6. Ndayang’anira Mbuyeyo
Zindilimbikitsetu.
Ndzapeza Dzuŵa langa
2. Ntchito zanga zonsezo
Londiyendetsa bwinoli
Sindikondweretsa ‘Nu;
Pa njira yonse yanga.
Ndikazigwiritsadi,
Ndikalira nsonizi, 104
Zonse sizikwanazi, 1. YESU wondikondadi,
Koma Yesu yekhayo. Ndithaŵire mwanumo
3. M’manja mopanda kanthu, Pakugunda mvulazi.
Mtanda ndingogwiradi; Pakubvuta madziwo,
Maliseche mbveke ‘ne; Yesu mundibise ’ne!
Ndili ndekha, msunge ‘ne; Ikaleka mphepoyo
Ndithawira m’mtsinjewo, Tsidya lija chete phee!
Munditsuke m’mtimamo. Mundilandire momwemo
4. M’moyo uno kunsiku 2. Pothaŵira pena ’yi
Pena ndinawaliratu, Ndikhulupirira ’Nu;
M’mene ndidzakwerako Musasiye inedi,
Tionane masowo; Mundigwirizizetu.
Thanthwe long’ambikatu Ndinu wothandiza ‘ne
Ndibisale momwemu. Wolimbitsa mtimawu;
Pansi pamapiko phee!
(maiwe! Thanthwe Mundifungatiretu.
long’ambikatu ndibisale 3. Wina sindifuna ’yi,
momwemu) Zokhutitsa nzanuzo;
M’utsetu akugwawo,
Mchizetu odwalawo.
103 Ndine wakuipa bii,
1. AMBUYE ’naitan ’ne;
Ndinu wakuyera mbuu!
“Dzapumulire kuno,
Ndimadzala tchimoli
Tsamira mutu, mwana ’we
Wolungama ndinutu.
M’chifuwa mwanga muno.”
4. Zindichulukirazi
2. Ndabwera kwa Ambuyeyo;
Nsoni zanu m’mtimamu;
Wolema, wachisoni;
Zindichiza nthendazo,
Anandipulumutsako,
Zindiyeretsetsa mbuu!
Nakondweretsa ine.
Pachitsime panupo
3. Ambuye naitana ’ne;
Moyo ndimwe ndimwebe;
“Ndipatsa anthu madzi,
Mubukatu m’mtimamo,
Wotopa ndi waludzu ’we
Mundilanditsetu ’ne
Dzamwere moyo kuno.”
(Mulungu ali nane!)
4. Ndabwera kwa Ambuyeyo.
Ndamwera madzi awa;
(Ali nane, ali nane, ali nane, ali nane, 2. Mzimu mndipatseko,
Aa! Wondilimbitsayo
Mulungu ali nane!) Mumtimamu.
105 Munandiferadi;
Ndiyambe leroli
1. NDI inetu sinditha ’yi
Kukonda Inu ndi
Kunenako milanduyi
Mtimangawu.
Kupempha zachisonizi;
3. Poyenda m’mdima bii,
Ndagonjatu Mbuyanga ’Nu.
M’mtimamo nsonizi
(Aa! Mulungu wanga,
Mndigwirepo;
Mundilembe pamphumipo:
Mdima uchoke zi,
Chidzakhala chizindikiro
Msozi ulekedi,
Cha mpumulo ulinkudza ndi Yesu.)
Ndisasokere ’yi
2. Ndi ine sizitheka ’yi
Kwa Inuko.
Kuchoka zakuipazi;
4. Moyo ukatha zi,
Ndisambe m’mwazi wanuwo;
Pofika imfadi,
Ndagonjatu Mbuyanga ’Nu.
Mndisungepo:
3. Ndi ine pondibvutapo
Yesu Mbuyanga ’Nu
Kugwira nazo m’mtimamo,
Mantha mthaŵitsetu
Mundithandize monsemo;
Ndifike m’Mwambamo,
Ndagonjatu Mbuyanga ’Nu.
E, wanuyu.
4. Ndi ine ndasaukadi,
Zabwino m’mtima zonsezi 107
Mwa Inu ndingapezezi; 1. CHITSIMECHO cha mwaziwo
Ndagonjatu Mbuyanga ’Nu. Udzera mwa Mbuyanga;
5. Ndi ine simufuna ’yi Wochimwa ndikasambamo,
Ndingatayike m’mdima bii, Nditaya tchimo langa.
Ndimvere mwandiuzazi 2. Wakuba uja nachiona,
Ndagonjatu Mbuyanga ’Nu Nangokhulupira,
6. Ndi ine, m’mtima Mwanu mbee! Ambuye namva pempholo,
Mokoma ndingakhalebe, M’Mwambamo namlandira.
Ndikhale wanu wanudi; 3. Ambuye, mwazi wanuwo
Ndagonjatu Mbuyanga ’Nu. Siitha mphamvu yake,
7. Ndi inetu ndidziŵedi E, Mpingo wonsewo
Chikondi chodabwitsachi Wayera m’kati mwake.
Pansipa ndi Kumwambako; 4. Chionerere mwaziwo
Ndagonjatu Mbuyanga ’Nu Wofuma m’bala lanu,
Sindinaleke ineyo
106 Kutama mtima wanu.
1. NDIKHULUPIRA ’Nu,
5. Kumwamba komwe n’dzaimbira
Mwana wa Mlungutu,
Mpulumutsi wanga,
Mbuyangayo;
Chifukwa ayeneratu,
Mumve popempha ’ne,
Wakonza m’mtima mwanga.
Tchimo muchotsebe,
Lero ndikhale ’ne Wa
Mlunguyo. 108
1. Yesu mundimve ndikuliratu,
‘Dzani kwa inetu; Thupi lonse, mtima womwe,
Mtimangawu ufuna unidi, Mwini wake ndinu nokha.
Bwerani, Yesudi. 4. E, ndikukhurupirirani,
Ndauona mwazi wanu;
Ndinasokeratu kutaliko, Tere ndikugwadirani,
Ndalekana naye Mulungudi; Tere ndapachikwa nanu.
Tsopano koma mndirandirenso,
5. Wadza Yesu wandidzoza,
Bwerani Yesudi.
Ndakonzeka mwa iyeyu;
2. Ndilibe malo mokhaliramo, Ndine wake, tokondana,
‘Dzani kwa inetu; Ndiyamika mbuye Yesu.
Khalani nane m’mtima
mwangamo, 110
Bwerani Yesudi. 1. NDIKHULUPIRIRA, Yesu,
3. Njobvuta njira ndimayendamo, Inu nokhadi
Dzani kwa inetu; Mundipulumutsa konse
Adetsa m’maso Leroli.
ndimapunthwamo, 2. Kuti mukhululukira
Bwerani Yesudi. Tchimo langalo
4. Wolap mtima simunyozadi, Ndi chifundo chachikulu
Dzani kwa inetu; Chanucho
Pemphero mumve langa lonseli, 3. Kuti muyeretsa mtima
Bwerani Yesudi. Ndibvomeratu;
Mwazi wanu unditsuka
M’mtimamu.
109 4. Kuti munditsogolera
1. Ndilinkudza kwa ambuye Paulendopo;
Ndasauka ,ndinachimwa; Mukwanitsadi zosoŵa
zonse zanga ndizisiya, Zangazo.
kudzapeza moyo wina. 5. Kuti mundipatsa mphamvu
Yopambanayo;
Mau mundilonga m’kamwa
Yesu ndikhulupirira
Mwangamo.
Munafera ine nemwe! 6. Ndikhulupira, Yesu,
Mwa umphawi ndipemphera Mndibvomereko;
2. Kale ndinalira inu, Ndine wanu lero, maŵa,
Kale lomwe ndangochimwa; Konseko.
Mund’itana, “idza bwino, 111
Kuti nkuchotsere tchimo”. 1. NDASIYA zonse ndi Yesu kalelo,
3. Yesu n’kupatsani zonse, Inde zakuipa zangazo;
Zili nanu zokhazokha, Anafera ine m’phirimo:
Pomva Mawu ake n’kondwako;
Mumachoka m’mtima
Mwangamo nsonizo,
Mumachoka m’tima
Mwangamo nsonizo. “Mwana, gonja, ndikupatsa
2. Chisoni andichotsera Mbuyeyu, Chimwemwe.”
An’thandiza ine teretu; 2. Kale ndinakana Inu,
Ndikhulupirira Iyeyu Ndinathaŵatu:
Andisunga m’manja mwakemu; Ndinazengereza, ndati:
Alimbitsa mtima “Maŵatu.”
Wangawu teretu, 3. Lero mtima ungolema,
Alimbitsa mtima Usaukadi;
Wangawu teretu. Wina wakundimasula
3. Mtima ’we siya ndi Yesu nsonizi, Ndilibe.
Usabisa tchimo lakoli 4. Mbuye, ndingogonja tere,
Zichuluka mphamvu zakezi, Ndibvomerapo;
Likusunga dzanja lakeli; Mundithyole, mundikonze
Bwera kwa Mbuyathu M’mtimamo.
leroli mwana ’we, 5. Chifuniro changa, Mbuye,
Bwera kwa Mbuyathu Ndiperekachi;
leroli mwana’we. Mutsogole, ndidzatsata
112 Inudi.
6. Tere moyo wanga wonse,
1. KWA Inu Yesu ndilira,
Mawu, ntchitonso
Wopanda Inu ndidzafa;
Zidzakondweretsa Inu
Mupulumutse ined,
Zonsezo.
Mundilandiretu.
7. E, chimwemwe chachikulu,
Mundilandiretu,
N’taperekadi
Ndiipa m’mtimamo
Mtima wanga, ndimapeza
Kotero mnandiferatu
Mtendere.
Mundilandiretu.
2. Ndifoka ndi zoipazo,
Ndidzalatu ndi machimo, 114
Sinditha kuzitayazo; 1. Chitha nchianikudyeretsa;
Mundilandiretu. Mwazi wa Ambuye Yesu;
3. Ndayesa kudzikonzadi, Nchiani chindipulumutsa?
Ndapeza mphamvu ndilibe, Mwazi wa Ambuye yesu.
Zoipa zakanikadi;
Mundilandiretu. Chitsime ndi chokoma
4. Onani Mbuye ndigonja, Chindiyeretsa bwino,
Kuyesa kwanga ndaleka; Chinanso sindifuna,
Chitani Inu mumtima; Mwazi wa Abuye ndiwo.
Mundilandiretu.
5. Muyambe ntchito yanuyi, 2. Mtanda m’mtima ndiyangana,
Musalekenso, chitani Mwazi wa Abuye yesu;
Ndidzipereka leroli; Ndikhululukidwa nawo
Mundilandiretu. Mwazi wa Abuye Yesu.
113 3. Zonse zina sizikwana,
Mwazi wa Ambuye ndiwo;
1. YESU, mulikundipempha
Ntchito zanga sinditama,
Munaterodi;
Mwazi wa Ambuye ndiwo. Yakulenganso ife;
4. Ndikhulupirira bwino Idzakhalatu yangwiro,
Mwazi wa Abuye Yesu; Ndiyo yoyenera ’Nu
Chilungamo change ndicho Usinthika ’lemu wathu,
Mwazi wa Ambuye Yesu. Udzakhala momwemo,
115 Mpakatu Kumwamba komwe
Tidzalemekeza ’Nu.
1. MNDILANDIRE ine Mbuye
Yesu wondifera ‘ne; 117
M’mtima mwanga muzikhala 1. NDILIKUMVA m’mtima mwanga
Mawu anu okhawa. Mau ake a MbuyAnga,
2. Ndasokera m’tali ndithu Ati, “Ndakukonda iwe,
M’njira zopwetekazo; Kodi undikonda Ine?”
Wolemedwa ndingopempha, 2. Ati; “Mwana, kumbukira
Mndilandire inetu. Zonse ndinakuchitira;
3. Pakukumbukira zanga Ndakukonda, ndakufera,
Ndili ndi manyazitu; Ndakufuna posokera.
Ndingogwera pansi, ’Tate, 3. “Ku zoipa zonse zako,
Mlapo wandigwiratu. Goli la pakhosi pako,
4. Ndingopatsa Inu Mbuye Ndi kunthenda zosautsa
M’manja mwanu mtimawu, Ndine ndakupulumutsa
Moyo, mzimu, zonse zanga, 4. “Kodi mayi wobereka
Mzilandire Mbuyetu. Mwana wake adzamleka
5. Mukhululukire ine, Pena adzamwiŵalira,
’Tate mundikondadi; Koma ndikukumbukira.
Mundisunge nthaŵi zonse 5. “Nthaŵi ilikudza yonse
Ndi chikondi chomwechi. Sindisinthanika konse;
116 Imfa sindiletsa Ine
Ndisakondekonde iwe.
1. A CHIKONDI chopambana,
6. “Ine ndidzakuonetsa
E, chinadza ndi Mbuye;
Zonse zakukondweretsa
Chinasangalatsa m’Mwamba,
Za Kumwamba zanga izo,
Chinaloŵanso mwa ’fe
Mwana, sundikonda ine?”
Yesu ndinu wachifundo, Wa
7. Ambuyanga, ndalephera,
chikondi changwiro, Ee,
Mwachisoni ndipemphera
muloŵetu m’mtimanga,
Mundipatse ine ndithu
Mumuyese mwanutu.
Mtima wakukonda Inu.
2. ’Dzanitu Wamphamvuyonse,
Mtilanditse konseko; 118
Musachedwe, thandizeni 1. ATI Yesu Mbuyeyo:
Musachoke mwangamu; “Ofoka ndinutu,
Inu nokha timakuza Mudikire, m’pemphedi,
Nditumikirabe; Ndidzapatsa mphamvutu.”
Tinyadira chikondicho, Yesu wathadi
Tichitame konseko. Za mangaŵatu,
3. Tsirizani ntchito yanu Inde ndinaipa bii!
Watsuka ine mbuu!
2. Mbuye ndimva leroli Zakukondakwakeko,
Za mphamvu zanuzi Anatuma mwana wake
Zomwe zisandutsadi Kundifera kalelo
Mtima wanga woti bii!
3. Ine kanthu ndilibe Inde ndidzaimba nyimbo
Kogula moyowu; Za kukonda kwakeko,
Ndingotsuka m’mtimamo Ndidzaimba ndi Angelo
M’mwazi wa Ambuye ’Nu Akukhala m’mwambamo.
4. M’mene ndifa inedi,
Kumwamba mzimuwu 2. Ndinachita mphulupulu,
Udzakwera komweko Waiwala zonsezo;
Kuonana Mbuyeyo. Ndinakhala ndi zoipa,
5. Ndipo pakuima phe! Wazichotsa zonsezo!
Pokhala Yesuyo, 3. Wandipatsa moyo wake,
Ndidzamama Mlunguyo Moyo wakuyera mbuu!
Kosaleka konseko. Ine ndili mwana wake,
Wandilera inetu.
4. Ndiyamika mbuye wanga
119 Ndidzamulemekezabe.
1. LINDIKOMERA dzina la Ambuye
Yesu wanga, 121
Lisangalatsa, lichiritsa, lin’chotsera 1. BWENZI ndinamkomanayo
mantha. Anandikonda kale;
Dzinalo la Yesu, Kukonda kwandigwirako,
Dzinalo la Yesu1 M’kukondamo nditsale.
Lindikomera dzina la Ambuye Yesu Kumtima kundimangako
wanga. Kosamasuka konse;
2. Lichiza mzimu wophwetekwa Ambuye ndine wanutu
ukakhale Kunthaŵi nthaŵi zonse.
bata, 2. Bwenzi ndinakomanayo
Lidyetsa mtima wonse, lipumitsa Anandifera yekha,
thupi langa. Anandipatsa moyowo,
3. Nlokoma dzinalo la Yesu, ndilo Ndatenga ine ndekha.
thanthwe langa, Zimene ndili nazozi
Chikopa changa, linga langa m’mene Nza Yesu mwini zonse, Ndi
ndibisala. moyo wanga wonse ndi
4. Ambuye ndinu Mbusa, Bwenzi, ndi Wakenso nthaŵi zonse.
Wansembe wanga, 3. Bwenzi ndinamkomanayo,
Ndi Mfumu, Moyo, Njira yomwe, Ndapeza mphamvu zanga,
Inde ndimatama, Zakundisunga inemo,
5. Tsopano ndibukitsabe chikondi chanu Ndiyende m’njira mwanga.
chija, Zolemera zoti mbee!
Pakufa ine Dzina lanu lindilimbikitsa. Zindilimbitsa monse;
Ndalema kuno, komweko
N’kupuma nthaŵi zonse.
120 4. Bwenzi ndinamkomanayo
1. Ndidzaimba za Mulungu,
Wokoma mtima wake, Zidzatu zinanso.
Wotsogolera nzeruzo Mlungu wachisomocho
Zisunga m’njira mwake. Mbuye wathu ndiye,
Palibe wondichotsa ‘ne Ati zinthu zonsezo
Kwa Iye wondikonda; Nzathu mwa Iyeyo.
Pamoyo, imfa, nayeyo (Zina ndi zinanzo
Ndilipo nthaŵi zonse. Zidza kwa ifedi,
122 Inde mtima wakewo
Uli wokomadi.)
1. NDIMKONDE Kristuyo,
2. Mwamva Yesu m’mtimamo,
Ndimkondebe;
Adzanso kaŵiri,
Pemphero langali
M’mene ali nanutu
Mlandiretu;
Muli ndi Chimwemwe.
Ndipempha Inutu,
Ntchito zachifundozi
Ndimkonde Kristuyo,
Iye watha izi,
Ndimkondebe,
Kuti mwawo m’Mwambamo
Ndimkondebe.
Naye tikhalebe.
2. Ndatsatatsatabe
3. Mwamva Mzimu wakewo,
Za pansipa;
Zake zimvekanso
Ndisiye zonsezi,
Kugwa ngati mvulayo
Nditate ’Nu.
Yachisomo chake.
M’mtimanga wonsewu
Mzimu ndiye mphamvudi
Ndimkonde Kristuyo,
M’moyo mwathu muno,
Ndimkondebe,
Mpaka tidzafikako
Ndimkondebe.
Komwe kuli Yesu.
3. Chisoni chonsecho
Chidzatha phe!
Angelo anuwo 24
Afiketu; 1. Poyambapo ndakondwadi,
Nawo, ndiimbetu, N’tapeza inu Mbuyetu,
Ndimkonde Kristuyo, Ndiimba nyimbo yomweti,
Ndimkondebe, Kukondwa sindikhala duu!
Ndimkondebe.
4. Pakufa pangapo Kalelo! Kalelo!
Ndinenebe; Wandisambitsa m’mtimamo,
Myamiko wangawu Wandiweruza lomwelo,
Ndikwezebe, Kupempha ndi kukondwako,
Ndidzapempheradi, Kalelo! Kalelo!
Ndimkonde Kristuyo, Wandisambitsa m’mtimamo.
Ndimkondebe,
Ndimkondebe. 2. Mnyamata wake ndinetu,
123 Ndimvera mawu akewo;
Ndimpatsa mtima wonsewu
1. MWAKHULUPIRIRADI
Ndimtumikira pansipa.
Yesu Ambuyathu;
3. Kumwamba ndidza……….
Muli nazo zakezo,
Za chipangano chathucho,
Wamoyo sindimsiya ‘yi,
Nditafa ndinka kwawoko.
125 Wofatsa ndithu,
1. AMBUYANGA Yesu, Kuti ndiyambe ’ne
N’kukondani Inu; Ntchito zanuzi;
Ndisiya zoipa Akusokerawo,
Chifukwa cha Inu. Abwere kwawoko,
Ambuye wabwino Inde,kwanutu.
Mundipulumutse konse; 4. Zambiri zangazo
Ndikonda tsopano Mnandipatsa kale,
Koposa kale lonse. Ndibweza zonsezi
2. Ndikonda chifukwa Kwa Mbuyanga ’Nu;
Mnayamba kukonda; Ndikadzaona ’Nu,
Mnafera pamtengo, Mbuye wabwinotu,
Munandiwombola. Nsembe yokomatu
Mukhululukira Ndidzakhalabe.
Zoipa zanga zonse;
Ndikonda tsopano 127
Koposa kale lonse. 1. WAFUNAFUNA ine
3. Ndidzakukondani Ambuye Yesuyo;
Mwa moyo ndi m’imfa; Wapeza ine ndithu
Ndidzakutamani; Wodwala m’mtimamo:
Chikondi n’dzaimba. Zochimwa zanga zonsezo
Mpakatu ndidzafa, Wachotsa izo zomwezo.
N’dzanena nthaŵi zonse; E! chikondi ndithu,
“Ndikonda tsopano E! chikondi ndithu,
Koposa kale lonse.” Ndi chisomo chake chonsecho,
Ndi zozizwa zake zonsezo.
126 2. Ndafoka ine kale
1. AMBUYE, m’imfamo Ndafuna kufaku;
Munandikonda ine; Zinthenda zangazo;
Sindikaniza ’Nu Ndi mwazi wake woti pyu!
Kanthu konse ’yi. Ndayera nawo m’mtimamu.
Ndimagwadira ’nu. 3. Mabala ake m’manja
Ndikonda m’mtimamu, Ndaona indetu,
Ndidzaperekatu Ndi minga ya pamutu
Nsembe yangayi. Yolasa Mbuyeyu;
2. Kumwamba kwanuko Etu, wakonda inedi,
Mundipempherere; Pamtandapo kufera ’ne.
Ndikhulupirako, 4. Ndikhumba ine ndithu
N’dzalandiradi; Madalo akewo;
Ndisenze mtandawo, Ndifuna kumyamika
Ndikhale mboniyo, Masiku onsewo;
Ndiperekeko Ndikafa ine pansipa,
Mitoloyi. Kumwamba ndizamtamanso.
3. Ndikhumba mtimawo
128
1. AMBUYE Mulungu,
Ndikondwera maka, 4. Akumangidwa ndi mzimuwo,
Ndapeza chimwemwe Mudze ndi ife kwa Yesuko,
Ndi moyo wosatha. Akuchotsereni magoli,
Aleluya, mlemekeze, Nadzakupatsani moyo,
Aleluya, ndiye Mfumu; Mlandu walipa ndi moyo,
Aleluya, mumpembedze Moyo ndi moyo ndi moyo,
Ambuye Mulungu. Tambirana za moyowo.
2. Ambuyanga Yesu 130
Nandikhetsera mwazi,
1. ADALITSIKA munthuyo
Nakonza ine
Wopeza dalo lomwelo,
Milandu yangayi.
Chisomocho cha Mlunguyo
3. Pamtanda woopsya
Chogwera m’Mpingo wakewo.
Adakandifera,
2. Chikhulupiro chomwenso
Natsika m’mtimanga
Chogweratu m’chikondicho;
Mukhale moyera.
Akhala nazo nzeruzi
4. Tsopano Mulungu
Zofumatu mwa Mbuyedi.
Alandira ine,
3. Adalitsika, indetu,
Popeza Mbuyanga
Wodziŵa wadza Yesuyu
Nawombola ine.
Nafera iye kalelo
5. Padziko lapansi
Ampatse moyo wosatha.
Ndikumva chisoni,
4. Akondwerera nthaŵiyi
Komatu kumwamba
Pomvera mwini Mlungudi;
Ndikhala ndi Mboni.
Mtendere ngwake panotu,
129 Nakhala nawo m’Mwambanso.
1. IMFA ndi mfumu ya mdimawo,
Anthu oipa imangawo,
131
1. NDIDZIŴITSITSA Yesu ndi wanga,
Akhristu amapulumuka.
Tsiku ndi tsiku ndimakondwera.
Omwe aimbira moyo,
Anandigula ndi mwazi wake,
Moyo ndi moyo ndi moyo,
Anandipatsa Mzimu woyera.
Wosalekana ndi moyo
Mawu omwewo, nyimbo yomweyi,
Wosamaliza Mulunguyo.
Yesu ndimtama tsiku lonseli;
2. Yesu anafa pamtandapo,
Mawu omwewo, nyimbo yomweyi,
Mzimu woipa nugomapo,
Yesu ndimtama tsiku lonseli.
Ndi ife titame Mulungu.
2. N’kamvera Yesu ndikakondwera,
Ndife tamasudwa m’moyo
Ndiyang’anitsa nkhopeyo yake;
Imfa ithedwa ndi moyo,
Ndipo angelo anditengera
Tsiku lomaliza moyo
Ine chisomo ndi chuma chake.
Wosamaliza Kumwambako.
3. Ndine kapolo wa Mbuye wanga;
3. M’mitima mwathu mwakhala mbee!
Andigwiritsa zintchito zake.
Mtambo wamdima wang’ambwa ke!
Ndimyembekeza adzabweranso,
Panyanjapo pagawanika.
Adzanditenga kwawo ndikhale
Ndife tipita ku moyo,
Mtima wabwino ndi moyo; 132
Kumbanda kucha kwa moyo 1. SINDINANYENGEDWA konse
Kumatiuza za dzuŵalo.
Pakutsata Yesuyo; Aleluya, Amen.
Yesu apambana zonse Aleluya, ndidzamtama
Ndinalingalirazo. Mulungu wanga.
Pakuyenderana naye 2. Mwazi wa Yesu
Ndimamdziŵa ndi woona; Unditsukatu,
Ndifunitsa anthu onse Ndiye Mbuye wanga
Adziŵenso Yesuyo! Ndi Mpulumutsi.
Ndifunitsa anthu onse 3. Pamtanda wake
Adziŵenso Yesuyo! ’Nafera ine,
2. Sindinanyengedwa konse: Ndi zoipa zanga
Yesu wachotsera phe! ’Nazichotsadi.
Zakuchimwa zanga zonse 4. Mulungu wanga
Zakupsinja mtimazo. Andilandira,
Yesu potsagana nane Chifukwa cha Yesu
Wandidzaza ndi mtendere; Mwana wakeyo.
Kundisunga, kundikonda 5. Adzabweranso
Sadzaleka konse ’yi! Kundilandira
Kundisunga, kundikonda, Ndikhale ndi Iye
Sadzaleka konse ’yi! Masiku onse.
3. Sindinanyengedwa konse, 134
Yesu adzabwerabe;
1. TILI ndi mtendere
Mtima wanga undiuza
Wopambanatu,
Akuyandikiradi
Monga ngati mtsinje
Omwe sangamzindikire
Mumitimamo;
Andinyoza nandijeda,
Koma mtsinje uno
Koma Yesu ati zedi;
Umayenda phee,
“Ine ndidzabweradi.”
Nthaŵi zonse mtima
Koma Yesu ati zedi;
Nutonthozabe.
“Ine ndidzabweradi.”
Tikakhulupira
4. Sandinyenga, salephera;
Mlungu wathuyo,
Yesu wadalitse ’ne
Tidzaona mwayi
Mpulumutsi ndi Myeretsi
Ndi mtenderewo.
Ndi Mchiritsi yemweyo
2. Dzanja la Mulungu
Wandiyanjanitsa naye,
Litisunga nji!
Mtima wanga nakhutitsa;
Nkhondo ya Satana
Sindinanyengedwa konse,
Sitiopa ’yi.
Yesu akwaniradi!
Zaphokoso zonse
Sindinanyengedwa konse,
Ndi zoopsyazo
Yesu akwaniradi!
Sizibvuta mtima,
133 Siziloŵamo.
1. MULUNGU wanga, 3. Masauko athu
Ndapeza moyo; Ndi zokondwazo,
Ndili wokondwera Azilola zonse
Masiku onse. Ndi Atatewo.
Aleluya, muyenera!
Pokhulupirira Chete! Chete!
Tidzapezabe M’tima mtendere ‘phee!
Kuti mtima wake Udzera kwa Yesu wokonda
Utikonda ’fe. Mtendere mumtimamu.
135
1. YESU ndiye Mbuye wanga,
2. Pamtanda mbuyanga ‘nafera,
Ndamva Mawu akewo
Akandichotsera zochimwa;
Andilandira ine,
Anandigulira mtendere;
Nandipulumutsatu.
Anditonthoza ‘ne phee!
Mwalembedwa mukalata
3. Pomlambira Yesu Mbuyanga,
Mawu ake omwewo,
Mumtima mtendere walowa;
Kuti iwo akumvera
Mdaliso woposa ndapeza,
Akalandiridwatu.
Anditonthoza ‘ne phee!
2. Ndinakahala wakuipa,
4. Pokonda Yesuyo, mtendere!
Ndinamkana kalelo;
Kanthawi kosatha, mtendere!
Koma Yesu waiŵala
Potsata Mbuyanga apatsa
Mphulupulu zangazo.
Mtendere mumtimamu.
3. Wapumitsa mtima wanga,
Kaamba ndaphunziratu 138
Mau ake olembedwa 1. KHALANI duu! Ambuye adzatu;
Mukalata mwakemo. Senzani chete mtanda wanuwu;
4. Mumvetu abwenzi athu, Mulungu adzakonza zanuzo,
Musakanirire ’yi; Sangasinthike mtima Iyeyu.
Yesu aitana inu, Khalani duu! Bwenzilo Yesuyo
Zalembedwa zomwezi. Atsogolera m’njira mwathumu.
136 2. Khalani duu! Mulungu wanuyu
Akonzeratu nthaŵi zonsedi;
1. MTENDERE uli m’mtima
Musakayike mtima; zo’psyazo
mwathumu,
Zimasulidwa pomalizapo.
Chifukwa mwazi watitsuka mbuu!
Khalani duu! A Yesu Mawuwo
2. Zakutsogolo sitidziŵa ’yi;
Ngamphamvu lero monga kalelo.
Adziŵa Yesu wathu zonsezi.
3. Khalani duu! pakufa mnzathuyo,
3. Abale angakhale m’talimo
Pakumlirira ndi misoziyo;
Mbuyethu asungira onsewo.
Pa nthaŵizo abwera Yesutu,
4. Imfa ndi manda sitiopa ’yi,
Mitima yathu natonthozadi.
Chifukwa Yesu wazithetsadi.
Khalani duu! Ambuye athadi
5. Mtendere wopambana m’Mwambamo
Kutibwezera zochotsedwazi.
Pakufa ife tidzaonanso.
4. Khaladi duu! pakufa ifetu,
Ndi Yesu tidzakhala indetu
137 Popanda mantha ndi zoŵaŵazi,
1. Ndiimba mumtima mokondwa Chikondi chokha koma m’mtimamo.
Ndi nyimbo yokoma, yoyera; Khalani duu! pakutha zonse phe
Ndiimba na Yesu Mbuyanga, Tidzasonkhana tonse kuli ’Ye.
Anditonthora ‘na………… 139
1. NAMONDWE akawombabe, Andifere kalelo.
Mafunde akakulanso, 2. Ngatitu abwenzi anga
Palipo pobisala ’fe. Sandikonda ine ’yi,
Ndi popemphera Yesuyo. Ndikhulupirire Mlungu,
2. Paja athira Yesutu, Iye sandikana ’yi.
Chimwemwe muli m’manthamo, 3. Pansi pano ndili mlendo,
Paja pokometsetsatu, Kwathu ndi Kumwambako;
Mwazi wa Yesu nukhapo. M’mene ndimalira ine
3. Pakulekana ifetu Ndidzapita komweko.
Mitima ikomanapo; 142
Tikumbukana ’bwenzi ’fe,
1. MBUYANGA Yesu, mundigwire
Popempherana komweko.
Dzanja.
4. Tidzathaŵira kuti ’fe
Kuyenda ndekha sindikwana ’yi;
Pochita mantha nkhaŵanso?
Mukandigwira dzanja langa, Mbuye
Pakuyesedwa, tinke ku?
Sindikaopa kanthu kena ’yi.
Tipemphe Yesu mphamvuyo.
2. Mbuyanga Yesu, mundisunge ine
5. Tikhale ndithu pomwepo;
Pafupi ndi ’Nu nthaŵi yonseyo;
Zapansi zisaloŵe ’yi.
Ndikasoŵatu Inu, Mpulumutsi,
Sitidzapempha m’Mwambamo;
Ndingosekera m’talimo.
Tidzayamika Mlungudi.
3. Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
140 Ukadza mdima m’mtima mwangamu;
1. MULUNGU anditsogolera, Koma ndinutu dzuŵa langa ndithu
Ndapumula m’mtimamo; Lakuwalitsa m’mtima momwemu.
Ayang’anira njira zanga 4. Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja
Nsiku zanga zonsezo. Pamene ine ndimwalirapo.
Mulungu anditsogolera Mkhaletu m’fupi nthaŵi yomwe Mbuye,
Nsiku zanga zonsezo; Mundiloŵetse ine m’Mwambamo.
Ndidzatsatira Mbuye wanga 143
M’njira mwake momwemo.
1. NDIFUNA Inu, Yesu
2. Masiku ena pali mdima,
Ndadzala ndi machimo,
Ndivutidwa m’mtimamo;
Mumzimu muli mdima,
Masiku ena ndikondwera
Ndikufatu m’katimo.
Ndi zabwino zangazo.
Ndifuna kutsukika
3. Masiku onse m’mtima mwanga
M’chitsimecho cha mwazi
Ndili ndi mtenderewo,
Wa Inu wokondedwa,
Chifukwa ndimakhulupira
Munandifera kale.
Mtsogoleri wangayo.
2. Ndifuna Inu, Yesu,
141 Lisoŵa bwenzi lina
1. M’MENE ine ndisauka Losungiritsa ine,
Ndi zoipa zangazo, Londithandiza mwina.
Ndidzapita kwa Mulungu, Ndifuna mtima wanu
Adzandilandiratu. Wodziŵa nkhaŵa zanga,
Mlungu adzandilandira, Wondisezera mtolo
Iye ndiye ’Tate wanga; Wa tchimo lonse langa.
Watumiza Mwana wake
3. Ndifuna Inu, Yesu, Ukukonda ‘we;
Ndimasauka ndithu, Ndiye mukaona
M’ulendo andisoŵa Wopirirabe;
Kambayo wa padziko. Ukasowa bwenzi,
Ndifunanso chikondi Usaope ‘yi;
Cha Inu chondisunga, Chikondano chake,
Chakundisangalatsa Chikwaniradi.
Panjira ponse panga. 2. Akukumbukira
4. Ndifuna Inu, Yesu, Yesu yemweyo;
Ndidzaonana nanu, Mkuyanjana naye
Mudzadza pamitambo Muli moyomo.
Ikhale mpando wanu; Uderanji nkhawa!
Pamodzi ndi ananu Mpulumutsiyo
Ndidzakondwera kuti; Atisamalira,
Ndilemekeze Inu, Atisungatu.
Ambuye, Mpulumutsi. 3. M’munda mwa Mbuyako
144 Muli ntchitomo;
Amithenga ake
1. Ndifuna yesuyo
Aigwirayo.
Ambuyanga,
Usaime chabe,
Mtendere ndinkemo
Usakhale duu!
Mwa iyeyu.
Yesu akufuna
Umthandizetu
Ndifuna inu Yesu,
4. Kwawo kwa Mbuyeko
Nthawiyi ndifuna!
Udzafikako;
Kwa Yesu Mbuyathu
Mwa ulemerero
Ndifunako.
Udzapuma ‘phee!
Usalowerere,
2. Ndifuna Yesuyo
Mvera Yesuyo,
Mobvutamo,
Ati: “mwana wanga,
Ndipulumukemo
Bwera kwathuko.”
Mwa iyeyu.
3. Ndifuna Yesuyo 146
Mokondwa ndi 1. PAMENE ndisauka,
Mowawa, adzemo Pamene ndivutidwa,
Ndi moyodi. Mizimu yakuipa
4. Ndifuna Yesuyo, Ikadza nindiyesa,
Ndichite ‘ne Mulungu wanga,
Zofuna zakezo, Mwini mphamvu,
Ndidzazabe. Mkandikumbukire ’ne.
5. Ndifuna Yesuyo 2. Pamene ndilemedwa
Woyeratu, Ndi zakuipa zanga,
Ndikhale wakeyo Poloŵa mdima m’mtima,
Wa iyeyu. Pochita ine mantha,
145 3. Masiku anga onse
Mulungu mundisunge;
1. Mtima wa mbuyako
Pamene ndimwalira, Mbuye, ndithaŵire kwanu
Ndi tsiku lomaliza, Poti mundikonda.
147 3. Sindidziŵatu zamaŵa,
Koma sindiopa;
1. KHALA chete mtima wanga
Ndidzakhulupira Inu
Mlungu wako ndiye Mfumu;
Kuti mundikonda.
Zinthu zonse zisinthika,
4. Inde wakukonda ndinu;
Mlungu ndi wachikhalire.
Mawuwo oona
(Khala chete,
Andidzaza ndi chimwemwe:
Chidzakupinga ninji?
Mlungu andikonda.
Usaope,
Mulungu ali nawe.) 150
2. Anthu onse pansi pano 1. Odala ndi onsewo
Sakhutitsa mtima wawo; Oyera m’mtima mwawo;
Amadera zinthu zawo, Adzaonana ndi Mulungu,
Namakhumba zakutali. Yesu ndiye wawo.
3. Khala chete mtima wanga, 2. Ambuye anachoka
Zikwanire zinthu zako; Mumwamba, mwini moyo,
Usakhumbe zapansipa Wofatsa anakhala nafe,
Koma Mlungu wako yekha. Mfumu yachisomo.
148 3. Mumtima wakufatsa
Anaconda kukhalabe
1. NGATI mtima sumakonda
Asankha mtima wakuyera,
Yesu supumula bwino;
Ndiwo nyumba yake.
Mbuye, suwu mtima wanga,
4. Tifuna inu mbuye,
Ndiwo wanu, mulandire.
Mtininkhe mtima uwu
2. Dziko lonse ndilitaya;
Wodzichepetsa, wakuyera,
Ndikondetsa Yesu Mbuye;
Woyenera inu.
An’komera kopambana
Andikondweretsa ndiye. 151
3. Ndakudani, mnandikonda 1. MNDIYANDIKITSE nanu.
Ndi kukhetsa mwazi wanu. Yesu,
Simuleka kundikonda; Ndiyenderane nanu;
Ine sindidzalekanso. E, nditsamire panu, Yesu,
4. Mndisungire mtima wanga, Panjira yonseyi.
Uzikhulupira Inu, 2. Ndionetsere kuunika
Kuti moyo wanga wonse Kokoma kwanu, Yesu!
Ubisaletu mwa Yesu. Yabwino mbiri ndibukitse
149 Yokondweretsayo.
3. Chitsime chakuyera ine
1. NJIRA yanga sindiziŵa,
Ndifanefane nacho;
’Tate muikonza;
Mundigwiritse ntchito zanu
Komatu muzindikira
E! zanu zokhazo.
Kuti mundikonda.
4. Mulamulire mtima, Yesu,
2. M’mene mantha andigwira,
Ndi chifuniro changa;
Andidetsa m’mtima,
Muloŵe mwanga ngati Mfumu;
Mundimveretsedi.
152 Kumwamba n’dzaimbira
Kukoma kwanuku;
1. “KHALA mwa Ine,” Yesu anatero;
N’dzatama nthaŵi zonse
Mawu abwino, koma Mbuye wanga
Chikondi chanucho.
Sin’ngathe ndekha, mukhalitse ine
Mwa ’Nu ndikhale nawo moyotu. 154
2. “Khale mwa Ine,” munachotsa tsoka, 1. KHALATU woyera, pempheratu
Mletse Satana anganyenge ine: m’tseri;
Mibvi yamoto yake muizime Werengani Mawu masiku onsewo.
M’mtimamo, ndikhulupirire ’Nu. Uthenga omwe ali akufoka,
3. “Khala mwa Ine,” ndinu mwini Madalitso ake ufunefunebe.
mphamvu, 2. Khalani woyera, dziko laipadi;
Mundithandize ine ndikafoka; Pemphera kolimba kwa Yesu
Mzimu Woyera andiululire Mbuyathu.
Zoona zanu m’mtima mwangamu. Yang’anitsa Yesu ndi kumutsatira,
4. “Khala mwa Ine,” ndinu mwini moyo. Kuti anthu ena aonenso Iye.
Nthambi zouma zidulidwa m’mtengo: Ine 3. Khalatu woyera, akutsogozetu;
wopanda Inu ndifokanso, Usamtsogolere munjira zakozo.
Zipatso zikasoŵa msadze ’ne. Pokondwa ndi m’nsoni tsata Ambuyako
5. “Khala mwa Ine,” Mbuye, ndifunitsa; Khulupira Yesu ndi Mawu akewo.
Mzimu Woyera mlonge m’mtima 4. Khalatu woyera, khalatu wofatsa;
mwanga, Alilamulire ganizo lakolo.
Akagonjetsetu machimo anga, Utatsogozedwa ndi Mzimu wakeyo,
Mtima woyera andipatsenso. Msanga udzagwira m’Mwamba
153 ntchito yake.
1. AMBUYE mundisunge 155
Pafupi ndinutu; 1. MUDZAZE Yesu mtima wanga ndi
Palibe malo pena chikondicho,
Popuma pansipa. Ukhazikike pa Mulungu wosachokapo.
Adani andizinga, 2. Mwa ine myatse moto wanu waku
Zoipa m’katimo; yera mbuu,
Chifundo chanu Yesu Utenthemo zoipa zonse zidakhalamo.
Chikonze m’mtimamo. 3. Mubweretu nomwe ’Nu munatsika
2. Ndikabisala mwanu kalelo;
Ndilibe mantha ’yi; Ndilira Inu mundidzaze mphamvu
Ndikasungidwa kwanu yanuyo.
Mumtima muti phee! 4. Ndikhazikike inetu, mumtima muli
Ndi mphamvu yanu yokha mwai,
Ndiposa ’daniwo; Ndi Yesu ndikondanetu, si kanthu
Chifundo chanu Mbuye kena ai.
Chitchinjirize ’ne 156
3. Ndidzaonana nanu
1. MBUYE ndamva mwawazira
Mokondwakondwadi.
Anthu ena madalitso;
Oyera mtima onse
Mvula yanu yawagwera;
Apenya Mbuyeyo.
Mbuye, ine mudalitse.
Etu ine, etu ine, Moyo wangawu ngwabwinotu.
Mbuye, ine mudalitse. Moyowo
2. ’Tate, msandipitirire, Ngwabwino,
Ndimaipa mtima ine; Moyo wanga ulitu bwino.
Ndiyenera munditaye, 2. Ngakhale Satana andizunza ’ne,
Koma mukhululukire. Chilipo chitonthozacho;
3. Yesu, msandipitirire Chifundo cha Kristu anafera ’ne,
Kuti ndinu ndikondane; Kundipatsa ’ne moyo wake.
Ndinalira Inu Mbuye, 3. Uchimo unapachikidwa pomwe
Msandileke poitana. Pamtanda wa Yesu Mbuye;
4. Mzimu, msandipitirire, Machimo angawo anatherapo;
Mupenyetsatu akhungu Mbuye wanga, ndiyamika ’Nu.
Mboniyo ya Mbuye Yesu, 4. Ambuyathu, ndikhumba tsiku lija
Mundipatse ine mphamvu. Limene ndidzaona ’Nu;
5. Ndinagona mwa zoipa, Lipenga limveke, ndidzakondwatu
Ndinakunyozani ine, Pakukomana ndi Yesuyo.
Dziko lino ndinakonda, 159
Mbuye, mukhululukire.
1. NDILIRA ine kukayenda
6. Ha! chikondi cha Mulungu,
M’njira ndi Mulungu;
Mwazi wa Mbuyathu Yesu,
Ndilira nyali ndikaone
Chiyanjano cha Mzimuyo
Njira Ya kwa Yesu.
Zonse zidzalemekeza.
2. Chimwemwe chija chamumtima
157 Ndinalaŵa kale
1. AMBUYE, thandizenitu Poyambutsata ine Yesu,
Ndi mphamvu zanuzo; Chili kuti tere?
Pantchito zathu zonsezi 3. Kalelo m’mtima ndinakondwa,
Mthandize Mbuyathu. Tere ndingolira,
2. Zochimwa zathu m’mtimamo Zokoma zonse zapadziko
Tilira nazotu; Sizindikwanira.
Mumtima mwathu muti zii; 4. Mubwere, Mzimu wa mpumulo,
Mthandize Mbuyathu. Mundileze m’kati;
3. Mthandize Mbuye, timvetu, Ndidana nazo zoipazo
Tikalandiredi Zinakuchotsani.
Zimene muperekazo 5. Mundichotsere tchimo lonse
Zakudalitsa ’fe. Ndinakonda kale,
4. Kumwamba Yesu mthandize, E, muligwetse kuti ndinu
Tilibe wina ’yi: Mfumu mukakhale.
M’moyo, muimfa mthandize, 6. Mkatero ndidzayenda m’njira
Tikhale kwanuko. Ndi Mulungu wanga,
158 Idzandiunikira nyali
Njira ya Kumwamba.
1. POKHALA mtendere mu
mtimangamu, 160
Pamene ndisaukanso, 1. NDILIRA mtima wotamanda
Pamene mabvuto ndi akuludi, Mlungu, ndi woyera,
E, mtima woyamika mwazi
Munandikhetsera. Musambitse ine, ndiyeretu mbuu!
2. Mtimatu wopirira ndi 4. Chifukwa cha ichi ndipempheratu,
Wofatsa mkati mwake, Ndidikira Inu Ambuyangayu;
Mumveka Mbuye Yesu yekha, Ndikhulupirira pa mwaziwo pyu!
Ndiye Mfumu yake. Musambitse ine, ndiyeretu mbuu!
3. Ndilira mtima wakulapa 163
Ndi womvera Yesu,
1. USAFUNE, chuma chokha,
Wosasiyana ndi Ambuye
Pena maseŵera okha,
Wakukhala m’mwemo.
Koma za Mulungu zokha
4. E, mtima watsopano ndi
Zipambana zinazo.
Wodzala ndi chikondi,
2. Ukafuna kulemera,
Wangwiro ndi wokoma, Mbuye,
Pempha chuma chosathera,
Wonga wanu wonse.
Ndiwo mtima wakuyera
5. Mkhalidwe wanu mundipatse
Ndi wokonda Yesuyo.
Ndifanane nanu
3. Zosauka ubvomere,
Mulembe m’mtima mwanga Dzina
Ndipo Yesu chaulere
La chikondi chanu.
Chikondano ndi mtendere
161 Aloŵetsa m’mtimamo.
1. Zoipa zangazi 4. Zonse umazinyadira
Zidetsa m’mtimamu; Udzaleka kusirira;
Mnditsuke, Yesutu, Uli nazo zokwanira
Kutsuka koti mbuu! Pakupeza Yesuyo.
2. Ndafoka inetu, 5. Mbiri yake ubukitse,
Ndalema m’mtimamu; Anthu onse nuphuzitse,
Andilimbitsa ’Ye, Kwa Mulungu nufikitse
Kulimba koti njo! Osokera onsewo.
3. Zin’soŵa indedi 6. Yesu sakusiya konse;
Zabwino m’mtimamu; Mphamvu, nzeru, chuma chonse
Ambuye, mdzazebe, Akupatsa nsiku zonse;
Kudzaza koti tho! Tsata Yesu yekhayo.
162 164
1. AMBUYE, ndifuna nditsukenitu; 1. MKRISTU, ulimbike
Mukhalire ndine mumtimangamu; M’ntchito yakeyo;
Muthyole zonsezo zodetsa ’netu; Yesu anafera
Musambitse ine, ndiyeretu mbuu! Anthu akewo.
Ndiyere mbuu! E, ndiyere mbuu! 2. Mphamvu zathu zonse
Musambitse ine, ndiyeretu mbuu! Tionetsenso,
2. Ambuye, chotsani zonse zomwezo Kuti kudziŵike
Zakundisautsa mumtimangamu; Tili akewo.
Ndileke zangazo zoipsa ’netu 3. Mtima wakufatsa
Musambitse ine, ndiyeretu mbuu! Amakondako;
3. Kumwamba ndiona Ambuyangayo, Ndipo anthu onse
Mudzandithandiza, nditsate ’nemo; Angatengero.
Mudzandichotsera zoletsa ’netu; 4. Mapemphero athu
Tikakwezebe,
Dzina lake lomwe 4. Tioperanji ifetu?
Tiyamike ’fe. Ali pafupi Mbuyeyu;
5. Limbikani nonse Sangasinthike mtima ’yi;
Mpaka imfayo. Kristu akonda ifetu.
Ndipo Mfumu yathu 167
Idzakondwako.
1. MBUYE, nditsate bwanjiko?
165 Ine ndikonde bwanjinso?
1. GWIRA zintchito zako, Bwanji kuyenda m’njiramo
Pomva usiku udza; Yonka Kumwamba kwawoko?
Yamba mamaŵa ndithu 2. Kodi m’njiramo ndimvadi
Potuluka dzuŵa. Nsoni zoŵaŵa, nkhaŵazi
Gwiranso m’msana monse Ndi masauko, mingayi?
Dzuŵalo likatentha; E, nkana izi n’tsatabe.
Gwira tsopano ntchito; 3. Anasauka Mbuyeyo,
Msanga udzaleka. Mwini nalola zonsezo;
2. Ntchito za Yesu gwira Anatsiriza ntchitozo,
Pomva usiku udza; Osabwerera imfayo.
Lero lonseli gwira, 4. Ndikamayenda m’dimamo,
Bwino udzapuma. Mletse zodandaulazo;
Gwiratu tsiku lonse Mundikumbutse mtandawo;
Ntchito zakuyenera; Zanga zichepa zonsezo.
Gwira tsopano ntchito, 5. Ine nditaya chumacho,
Tere udzaleka. Ndikondweretse Mbuyeyo,
3. Mkristu gwiratu ntchito Thupi liopa mingayo,
Pomva usiku udza; Koma mlimbitse mtimawo.
Dzuŵalo lopendeka 168
Tere lidzaloŵa.
1. YESU, afuna iwe unke kwawoko,
Gwiranso ’dzulodzulo
Loŵa m’njira yake yakuyerayeratu;
Kutada mdima bii!
Anadzera m’Mwamba kutiperekezako;
Tsono zintchito zonse
Yamba msanga iwe kunka kwanuko.
Zatha zonsezi.
Tsata, tsata, nditsatadi Yesu;
166 Iwetu, iwetu, ukatsatanso.
1. TITHAŴIRENJI ifetu Tsata, tsata, nditsatadi Yesu;
Mphamvu za Yesu nzathunso. Inu nonse mukatsate Mbuyeyo
Kristu atithangatatu. 2. Ngati umtsata Mpulumutsi wakoyo,
M’nkhondo ya moyo wathuyo. Udzakhaliranso kuli Mbuye wakoyo;
2. Yendani bwino m’njiramo Adzapulumutsa thupi, mzimu wakonso,
Ya kwa Mulungu wathuyo; M’mphamvu ndi chilango cha zoipazo.
Kwezani maso kuli ’Ye; 3. Kunsi kudambo, pena m’mwamba
Kristu ndi njira yomweyo m’phirimo,
3. Nkhaŵa tilbe; Yesuyo Pomwe pali Yesu ndidzayenda
Atsogolera m’njiramo; yendapo:
Tikhulupire Iyeyo, Andiperekeza bwino m’njira yakeyo,
Kristu ndi moyo wathuwo. Kuli Mzinda wa Mulungu wangayo.
169 Tidzabwera tonse
Ndi zipatsozo.
1. MBUYE, mwatiuza ’fe
3. Tingolira kaya,
Tizikhala mchere
Koma tidzafesa
Wokometsa onsewo
Mbewu za Ambuye;
Akumanga kwathu.
Ntchitoyo nja Yesu.
Mcherewu ndi ifetu;
Adzachotsa msozi,
Mtifanize nanu,
Adzatilandira,
Tikakope ndi chitsanzo
Tidzabwera tonse
Onse akuchimwa.
Ndi zipatsozo.
2. Mbuye, mwatiuza ’f
Tizikhala nyali 171
Yoonetsa onsewo 1. M’MENE umauka m’maŵa,
Njira yonka kwanu. Sunagwire ntchitozo,
Nyali ndi ifetu; Sunayambe kukayenda,
Kuunika kwanu Ugwadire Mlunguyo.
Mutipatse tiŵalire Pena uli kusekera,
Osokera onse. Pena nkhaŵa m’mtimamo,
3. Tisasungaluke ’yi, Wachimwemwe, wachisoni,
Tisasiye Yesu. Uza Yesu zonsezo.
Tisabise nyaliyi 2. Wakuchezacheza naye
Pakuchita mantha. Ukagwira ntchitozo;
Mcheretu ndi nyaliyi Pakukumbukira Yesu,
Tizikhala tonse; Nkhaŵa zidzachokanso
Mbuye, mtiyeretse m’mtima Ndi zapansi zikafuna
Tikatero ndithu. Kukudzaza m’mtimamo,
170 Utsogole kopemphera,
Uza Yesu zonsezo.
1. M’MAŴA tizifesa
3. Ndi m’kutero udzadziŵa
Mbewu zakukoma,
Chifuniro chakecho;
Msana ndi usiku
Iye adzakuthandiza
Tizifesa momwe.
Uthangate enanso:
Nyengo yamasika
Ndi ofoka ulimbitse,
Tidzatema m’munda,
Akulapa bwezatu;
Tidzabwera tonse
Ndi za ntchito zake izi
Ndi zipatsozo.
Uza Yesu zonsezo.
Ndi zipatsozo
4. Ndipo ngati ungolema,
Ndi zipatsozo
Ulefuka m’dzulomo,
Tidzabwera tonse
Ndi Satana akayesa
Ndi zipatsozo.
Kukukola m’mtimamo:
2. Tizifesa m’dzuŵa
Wakufoka, wakuopa,
Tizifesa m’mthunzi,
Penyetsetsa Iyeyo;
Sitiopa ife
Udzakhazikika m’mtima
Mtambo ndi chisanu.
Pakumuza zonsezo.
Athatu masika
Ntchitozi zidzatha; 172
1. HAYA! ’nzanga taonani
Yoonekayo Tiyeni, tiŵauze za Mbuyathu
Yakumwamba iti: “Yesu Mpulumutsi
Alikudzako.” Nitiŵanditse mbiri yake
Kanganani nkhondo yanu M’dziko lonse lathu.
Ndi mbendera mbuu! 174
Tibvomere: ‘Inde Mbuye
1. LIMBA mtima mbale wanga
Mtithangatetu.”
Usapunthwe m’njirayi;
2. A! mizimu yakuipa
Onatu nyenyezi ija
Isautsabe,
Ikutsogoleradi.
Tikaniza zakuipa
Tamveratu Mlungu yekha,
Zotizinga ’fe.
Chita zolungama ’we,
3. Mdani adza nazo mphamvu,
Yenda bwino, khulupirira
Koma ifetu
Mbuyeyo, Mbuyeyo,
Tidzamthetsa nkhondo yake
Ndikuchita zakezi.
Timwingitsetu.
2. Taya zako zochenjera,
4. Yesu ati, “Ndidza msanga!”
Taya zamumdimanso;
Thangateni phee!
Nthaŵi zonse khulupira,
Mbweze mawu akulimba:
Chita zolungamazo.
Tikanganabe.
Usayang’anire wina
173 M’khondo yake yomweyi,
1. ANATILEMBA Yesu tikagwire Koma m’zonse khulupirira
nkhondo yake, Mbuyeyo, Mbuyeyo,
Natilimbitsa tipirire osaopa kanthu. Ndi kuchita zakezi.
Kwa Satana n’ziwembu zake 3. Leka zakuipa zako,
Sitigonja konse; Myambi yonse yoti bii,
Tiyenderana naye Mfumu Usakhulupire mommo:
yathu yopambana. Tamveradi Mbuyedi.
2. Amaliwongo ochuluka amaloŵa Adzadana nawe ena,
m’mtima Ena adzakonda ’we;
Nafuna kuipitsa usana ndi usiku; Kweza maso, khulupirira
Tikatsatabe Mfumu yathu Mbuyeyo, Mbuyeyo
Sitidzagwa konse, Ndikuchita zakezi.
Pakuti atipatsa mphamvu 4. Mawu ake atipatsa
tipambane nazo. Mphamvu ndi mtenderenso,
3. Amatininkha zida zoteteza mtima, Bwino atitsogolera,
Ndizo; Tikhulupirira ’wo
Kupempherabe, kukhulupirira ndi Limba mtima, usapunthwe
kufatsa; M’njira yamumdimayi;
Mtheradi, ndi lupanga ndilo Yenda bwino, khulupirira
Mawu a Mulungu; Mbuyeyo, Mbuyeyo,
Pogwira zida zakezi sitilephera Ndi kuchita zakezi.
konse.
4. Mafumu atiuza tikaletse ukapolo,
175
1. POYESEDWA ine
Ndi kumasula goli la anzathu akuopa
Yesu mudzetu,
Mundipempherere
Ndisachimwetu. Kumwamba kuli Inu,
Mukaona kuti Ambuye wangayo.
Ndilefukatu, 3. Yochita ndi yodikha
Mbuye mndilimbitse Mupatse mphamvuyo,
Nazo mphamvutu. Ndikhale wochenjera,
2. Ndi zapansi pano Wogwira ntchitozo.
Ndikokedwadi, Zoipa zanga zonse
Koma ndi chisoni Mufafanizezo,
Mndiphunzitsedi; Ndiyende nanu nokha
Ndisaiŵalire Masiku onsewo.
Za Getsemane, 177
Pena mtanda wanu
1. TIYENI Akhristu,
Yesu Mbuye ’Nu.
Nkhondo tigwire;
3. Mukandipweteka,
Yesu Mbuye wathu
Ndipirirapo:
Atitsogolera.
Nsembe yanga ndiyo,
Mfumu yathu mwini
Landirani ’yo.
Atipatsa moyo;
Ndikachita mantha
Taonanitu mbendera
Sindithaŵa ’yi:
Yailoŵa nkhondo!
Mtima udzalimba,
Tiyeni Akristu,
Ndidzaima nji!
Nkhondo tiigwire;
4. Pakumalizidwa
Yesu Mbuye wathu
Moyo wangawu,
Atitsogolera
Pomwalira ine,
2. Nkhondo ya Satana
Mudze Mbuyetu.
Idzakuthaŵani;
Ndidzadzipereka
Tiyeni Akristu,
M’manja mwanumo:
Kaipambaneni.
Mpulumutsi Yesu
Idzanjenjemera
Mndilandireko.
Mukapfu’litsatu;
176 Imbitsanitu anzathu,
1. AMBUYE wa Kumwamba, Mau mukwezetse.
Mundithangatetu 3. Mpingo wa Mulungu
Kuyenda bwino lomwe Uli ngati nkhondo;
M’ulendo unowu. Titsagane nawo
Kaŵiri ndi kaŵiri Ana a Mulungu.
Ndipunthwa m’njiramo Sitipatukana,
Mlimbitse mtima wanga, Ndifetu amodzi;
Ndingatayikeko. Ch’yembekezo, chikondano,
2. Ndikhumba Mzimu wanu Chonse ndi chimodzi.
Kundiyeretsa mbuu! 4. Zonse zapadziko
Pang’ono ndi pang’ono Zidzamalizira,
Mundiphunzitsetu; Koma mpingo wake
Ndifuna nzeru zanu Uli chikhalire;
Zakundifitsako Udzakhala ndithu
Mphamvu za Satana,
Yesu analonjezetsa, Ya Mbuye wathuyo;
Mawuwo sakana. Tileke zakuipa
5. Tiyeni anzathu Zokhala m’mtimamo.
Tizithandizana; Sitikwanira tokha
Imbirani nafe Kuleka zathu zomwe,
Nyimbo zopambana Koma Mbuyathu Yesu
Kristu ayenera Atithangatatu.
Mphamvu ndi ulemu; 3. Tsopano timenyana
Komwe kuli Yesu. Ndi zakuipazi;
46 Pamene nkhondo yatha
Tidzanka kwathuko.
178 Yesu adzalandira
1. TIYENI, Akristu inu, Ankhondo ake onse;
Mumenyane nkhondo iyi, Adzakhalika naye
Mukafoka nonse, koma Kumwamba komweko.
Yesu akulimbitsani.
2. Muyendanso kunka komwe, 180
Mugonjetse mdani wanu; 1. MBUYE, ndapangana
Musafoke, musaleme, M’njira yanuyi,
Musagone konse inu. Kuti ndidzayenda
3. Musagonje, anthu inu, Osaleka ’yi.
Mtamiretu Yekha Mbuye; Mundipatse mtima
Ipambana mphamvu yake, Wopiriramo,
Ya Mtsogoli wanu yemwe. Wakukana zonse
4. Mtima wanu wonse ndithu Zondipingazo.
Udzakhala ndi chimwemwe. 2. Mzimu wakuipa
Zida zanu mbvale bwino Undiyesa ’ne;
Zakudzera m’Mwamba momwe. Mundithangatire
5. Limbikani inu nonse, Ku’thaŵitsabe.
Msangalalo ngwanu nokha; Akandisautsa
Musaope kanthu kena Kum’dzi kunoku,
Mumtamire Mbuye Yekha. Muloŵetse mphamvu
6. Tiyeni ku nkhondo iyi, M’mtima mwangamu.
Mugonjetse zonse konko; 3. Akathira nsembe
Muingitse mdani uja, Ku mizimuyo,
Muyendetse m’njira momwe. Ndipenyera kwanu,
E, Kumwambako.
179 Tsoka ndi zonyenga
1. AKRISTU limbikani, Za ufitizo,
Imani mtima nji! Yesu mndilimbitse
Mbendera nyamulani, Ndisaopezo.
Msatenthemere ’yi. 4. Pena kumwa nawo,
Wotsogolera wathu Ndisateroko,
Ndi Mwana wa Mulungu; Pena kukaona
Adzagonjetsa onse Gule woipa,
Adani athuwo. Pena kuwombeza
2. Tigwire nkhondo yomwe
Sindifuna ’yi; Inde, mudze inu nonse,
Yesu mundithandize Mudze nafe paulendo.
Kuzikanazi. Inde, mutiperekeze,
5. Ndinu mbusa wanga; Yesu atilinda ife.
Mndithandizetu; Yesu atilinda ife
Ndisaipse nazo Kuli dzikolo labwino,
Mtima wangawu. Yesu atilinda ife
Osaopa konse, Kuli dzikolo labwino.
Osachimwa ’yi.
Mundiyendetse Yesu
182
1. ANA akumwamba ndife,
M’njira yanuyi.
Paulendo timaimba;
181 Timatama Mbuye wathu
1. AULENDO, munka kuti Ndi Wa ulemerero wonse.
zindodo m’manja mwanu? Tilikupita kwathu kuja
Paulendo tizipita; Munjira ya atate athu,
Aitana Mbuye wathu; Amakondwera lero lomwe;
Pamapiri, pamadambo Tinka kuonana nawo.
Tizipita komwe kwawo. 2. Mbuye anatiitana
Tizipita komwe kwawo Kukagwira ntchito yake,
Kuli dzikolo labwino, Kuitana anthu onse
Tizipita komwe kwawo Atsatenso njira yino.
Kuli dzikolo labwino. 3. Inde Mbuye, tibweradi,
2. Kodi simuopa njira, Zathu zonse tizisiya,
Inu anthu akufoka? Mtsogoleri wathu ndinu
Ayi, atiperekeza Titsatabe inu nokha.
Mbuye wathu wotikonda. 183
Iye amakhala nafe,
1. MBUYE munditsogolere,
Natitsogolera ife.
Ndine mlendo m’dziko muno;
Atitsogolera ife
Ndikafoka mundikweze,
Kuli dzikolo labwino.
Mundisunge m’manja mwanu;
Atitsogolera ife
Mundidyetse, mundidyetse,
Kuli dzikolo labwino.
Sindingamve njalayo.
3. Mundiuze, aulendo,
2. Mundimwetse madzi anu,
Muli chiani m’Mwamba muja?
Andichize nthenda zanga;
Atibvekako zoyera
Utsogole mtambo wanu,
Akorona natininkha;
Ndikadziŵe njira yanga;
Moyo, moyo atipatsa,
Mpulumutsi, Mpulumutsi,
Kwa Mulungu tidzakhala.
Munditchinjirizetu.
Kwa Mulungu tidzakhala
3. Ndikaloŵa m’mtsinje muja,
Kuli dzikolo labwino,
Mndichotsere mantha osne;
Kwa Mulungu tidzakhala
Mndiwolotse tsidya lija,
Kuli dzikolo labwino.
Ndikondwere nthaŵi zonse;
4. Kodi inu, aulendo,
Nyimbo zanga, nyimbo zanga
Ife titsagane nanu?
Zidzalemekeza ’Nu.
184 Nditsatatu.
Ndidadzikuza osaopa ’yi;
1. NDIMAYENDA paulendo
Ambuye, msakumbuke zomwezi.
Ndi yaminga njira yake;
3. Ndi kale lonse mnandisunga ’ne;
Tsoka ndikapeza, koma
Tsopanonso.
Ndinka kwa Atate;
M’khwaŵa, paphiri, mundisungebe
Pena m’mtima mwanga mwada,
M’tsogolomo.
Pena andibvuta ‘dani,
Ndipo mamaŵa n’dzaonana ndi
Ndikatenga nkhaŵa, mantha,
Abale anga adafikadi.
Amadziŵako.
2. Ichi chindisangalatsa 186
M’mene nkhondo indigwira, 1. TIYENI nonsenu okonda YESUYO,
M’mene nsoni zazikulu Tiimbe nyimbo yabwino,
Zimanditsatira; Tiimbe nyimbo yabwino,
Mtima ukhazika m’mene Ku mpando wakewo,
Kwathu kuja ndikumbuka Kumpando wakewo.
Kuti Mlungu ali ndine, Tiyeni pamodzi
Andisungako. Tilikupita Kumwamba;
3. Mbuye andipeza lero, Akristu tilikupita
Andikonda, andisunga; Ku mzinda wa Mlungu.
Adzapitikitsa mdani 2. Ngakhale enawo aleke kwimbako,
Akamandibvuta. Akristu ’fe tidzaimba,
E, ulendo wanga utha, Akristu ’fe tidzaimba,
Tsono ine ndimwalira; Kumlemekeza ’Ye,
M’mene ndidzafika kwawo Kumlemekeza ’Ye.
And’landirako. 3. Akristu tonsefe, tikondwe m’Dzikoli
4. Komwe ndi chimwemwe ine Koposa anthu enawo,
N’dzaonana ndi Atate, Koposa anthu enawo,
N’dzagwadira ndi kumtama, Tisanafikeko,
Amandikondabe. Tisanafikeko.
Sakandisautsa kanthu 4. Tiimbe mokondwa, misozi iume;
M’dziko lija lakukoma; Poyenda kunka kwathuko,
Adzandidalitsa Yesu, Poyenda kunka kwathuko,
Ndidzakondwako. Kwa Mlungu wathuyo,
185 Kwa Mlungu wathuyo.
1. MUNDIŴALIRE m’njira 187
mwangamo, 1. NDAMVATU kuti tifika komweko
Mbuyanga ’Nu. Kuli Ambuye, Mtetezi wathuyo.
Kwada usiku, ndasokerako, Ine, pakutha zobvuta zathuzo
Mtsogoletu. Iye tidzamwona maso ndi maso.
Phazi langali mndisungirenso, Ndi Mbuyeyo tikhalamo,
Ndilonde Inu m’njira monsemo. Kupenyanso wokondatu;
2. Sindidapempha kale Mbuye ’yi, Tidzakondwera, E, nthaŵi zonsezo
Mtsogole ’Nu; Ndicho chimwemwe ndi ulemutu.
Ndisankha ndine, koma leroli 2. Kaamba chisomo cha Mbuyathu
uyu,
Malo okoma tipeza m’Mwambamo; Poliriratu abale,
Kumva mtetezi amene ndi Yesu, Yesu mutimveretu.
Ndicho chimwemwe ndi chachikulutu. 2. Munabvala thupi lathu,
3. Onse aliko takonda kalelo, Munadziŵa masauko,
Kale napita kwa Yesu Mbuyawo; Mnalirira bwenzi lanu;
Koma kumwona Mtetezi wathuyo Yesu mutimveretu.
Ndicho chimwemwe choposa, 3. M’mene imfa yathu idza,
nchathucho. Mweya wathu ukaleka,
188 M’mene ife timwalira,
Yesu mutimveretu.
1. UKATHA moyo wanga
4. Mnamwalira Inu paja,
Kumwamba kundichera;
Mwazi wanu munakhetsa,
Dzuŵalo ndimalira
Koma Inu munadzuka;
Lafika lokomera.
Yesu mutimveretu.
Usiku m’nali mdima,
5. Mtima ukachita nkhaŵa
Tsopano mbanda kucha;
Ndi zoipa zotimanga,
Kudzaŵalitsa ndithu
M’mene tikachita mantha,
Ku Dziko la Mulungu.
Yesu mutimveretu.
2. Chitsime chachikondi
Ndi Yesu Mbuye wanga; 190
Ndalaŵa mtsinje pano 1. KODI uli ndi chisoni
Ndzamwetsa ine m’Mwamba. Choliritsa mtima wako?
Komweko zidzakula Kweza maso, ndi Atate
Chisomo ndi chifundo, Akumvetsa zonsezi.
Pondiŵalira kuja 2. Kodi umadandaula;
Ku Dziko la Mulungu. “Mbale wanga waferanji?”
3. A! Yesu Bwenzi langa Kumbukira Wakumtenga
Inenso bwenzi lake, Saphophonya konse ’yi.
Woipa ’ne alola 3. Mbale wako unamkonda,
Ndiloŵe m’nyumba mwake; Koma Yesu amkondetsa;
Ndikhulupira Iye Anamfuna nagomtenga;
Achotsa mphulupulu; Usammane Yesu’yi
Kudzandiŵalitsira 4. Pakutsazikana nanu
Ku Dziko la Mulungu. Ndi potseka maso ake,
4. Ambuye andisunga Imfa, bii! Anangogona
M’chifundo chachikulu; Koma adzadzukanso.
Zisoni zisanduka 5. Usalire; Mpulumutsi
Chimwemwe cha Mulungu. Analaŵa imfa Yekha;
Dzanjalo ndilitama Imfa yomwe nagonjetsa
Ndi mtima wachifundo, Potuluka m’mandamo.
Mpakatu kwaŵalitsa 6. Chikondano sichifera;
Ku Dziko la Mulungu. Mbale wako udzamwona
189 Kwathu komwe; zipirira
1. TIKAGWIDWA ndi chisoni, 50
Ikayendanso misozi, Mpaka ukafikako.
7. Leroli chisoni chokha,
Tsiku lija kungokondwa; 3. Ndi nkhondo ikaleka
Kweza maso osalira, Kwa Mlungu komweko,
Yesu akukondadi. Ndi ukapolo watha,
191 Udani wathanso;
Ndi zakuopsa zonse
1. NTCHITO yonse yakeyo
Ndi zosauka zii!
Yatha m’dzikoli linoli
Ndi mwayi wa kwa Mlungu
Mlendo wafikatuko
Udzoza mutu tho!
Pokocheza leroli.
’Tate, mwa kusunga kwanu
Timusiya mwana wanu.
’Tate, mwa kusunga kwanu
Timusiya mwana wanu. 193
2. Yathatu misoziyo 1. Nlokoma dziko langa!
Zobisika zonse mbee! Ndiyang’anirapo,
Aweruza bwinoko Ndilira ndi chikondi
Ndiye Wolungamayo. Poona dzinalo;
3. Komwe Mbusa kwawoko Pakumva mbiri yanu
Atengera nkhosa zonse, Mumtima muti duu!
Zake asungiramo Ndi moyo ndi mtendere
Zosaopa kanthu konse. Imalowetsamo.
4. Onse akulapawo 2. Mokhala mokhamokha
Ayang’ana mtanda wake; Mokondwa momwemo;
Aphunzira komweko Misozi yatha yonse,
Zonse za kukonda kwake. Angosekeramo;
5. Dothili kudothilo, Panyezimira ponse,
Pfumbili kupfumbi tere; Panyumba pati mbee!
Mpaka adzadzukanso Pamyala pakongola
Timusiya mumtendere. Yoyala ponsepo.
192 3. Makomo afanana
Ndi myala yoti mbuu!
1. MUMZINDA wa Mulungu
Ndi kristu wopambana
Moyera mulimo,
Aonekeramo;
Ndiye amathu omwe
Ndi mtanda woyeretsa
Olera ifewo;
Wopachikidwapo,
Mitima yathu yomwe
Amamlambira Mfumu
Ikondwereratu,
Namlemekezanso.
Nikhala nawo Mzinda
4. Kulibe gombe, Nyanja,
Wakukongolawu.
Kulibe nthawi ‘yi,
2. Akondwerera anthu
Alendo alandira
Zokoma zonsezi
Zoziziritsazi;
Za midzi ya padziko
Pa mwala wa muyaya
Lapansi lonseli;
Amanga nyumbayo,
Mtendere wake koma
Ndi omwe opambana
Wa Mzinda wathuwo
Adzakondweramo.
Upambanditsa zonse
5. Nlokoma dziko langa!
Zapansi pomwepo.
Kopita onsewo Iwo adatichimwira.
Mulungu awasankha, 3. Musatifikitsemo
Tifuna kunkako. Muli mayeserowo,
Ambuye, mutsogole Koma mutipulumutse.
Ku dziko komweko; Wanu ndi ufumuwo,
Tidzakuimbirani Mphamvu ndi ulemunso
M’ulemerero. Kufikira nthaŵi zonse.
194 196
1. NDIKONDWA kuganizirabe 1. Mtima wanga ndikonzera,
Za Dziko la Mulungu; Mbuye Yesu aitana;
Momwemo muli abwezitu Ati: “Mwana, tapemphera,
Okhala mumtendere. Ine sindidzakukana.”
Iwo salekana, iwo salekana, 2. Mbuye ndinu Mfumu yanga
Ayi salekana abwenzi omwewo. Yolemera ndi yamphamvu;
2. Komweko akhala Yesuyo Ndikapemphatu zambiri,
Mtetezi wa inedi Simundimanira kanthu.
Pakati pa ’womboledwawo; 3. Ndikabwera nd katundu
Sadzamva kuŵaŵanso. Wa zoipa zanga zonse;
Iwo asekera, iwo asekera, Mwazi wake wa Ambuye,
Inde asekera kumwona Yesuyo. Udzandiyeretsa konse.
3. Mulibe zoipa m’Dzikolo, 4. Mbuye ndinalema ine,
Nzokomazo zabwino; Mloŵe Inu m’mtima mwanga;
Ndi nthenda, imfa, misoziyi Mkhale m’mwemo mwini wake,
Kumwamba kulibenso. Mantha mwandichotsera ’ne.
Dziko labwinotu, Dziko labwinotu, 5. Ndine mlendo pansi pano,
Nawo mtenderewo, tikhumba ilotu. Mndilimbitse ndi chikondi;
4. Ndikonda kuganizirabe Bwenzi mundilondolere
Za Dziko la Mulungu, Njira pa ulendo wonse.
Za zonse zotikondweretsamo, 6. Mndidziŵitse ntchito yanga,
Nzosathanso chikondi. Mphamvu yake mundipatse;
Ife tikondwera, ife tikondwera, Mundilimbikitse m’mtima
M’mene tidzampenya Ambuye wathuyo. Ndikhale kwa Atate.
195 197
1. ’TATE wa Kumwambako, 1. PEMPHERA m’mbanda kucha,
Likayere Dzinalo, Pempheranso usana;
Udzetu Ufumu wanu; Pemphera m’dzulo momwe,
Chifuniro chanucho Pemphera ndi usiku.
Chichitike pansipa Ndi mtima wonse idza,
Monga chachitika kwanu. Tulutsanso zachabe;
2. Mutipatse leroli M’nyumbamo ugwadire
E, chakudya chathuchi Ndi kukapempherabe.
Tsiku n’tsiku tichilira. 2. Kumbuka ’bale ako
Mukhululukiredi Ndi onse uŵakonda;
Tchimo lathu, monga ’fe Pemphera ’dani ako
Amene akutonza.
Dzipempherere wekha M’wapulumutse ndi k’ŵachitira
Mulungu akusunge; Zomwe mufuna k’ŵapatsawo.
Tchulanso popemphera 6. Poloŵa ndi Inu
Dzinalo la Ambuye. M’chipinda cham’tseri,
3. Akakusoŵa malo Posonkhananso pamodzi,
Opempheramo m’tseri, Muyandikire nafe, Atate,
Komatu m’mtima mwako Mtibvomere, mtidalitsepo,
Mwaloŵatu zoyera;
Anazilonga m’mwemo
Ndi Mzimu Wakuyera;
199
Zolingirira zija 1. Bwenzi lathu ndiye Yesu
Kwa Mlungu zidzakwera. Atikonda ifetu;
4. Tilibe madalitso Zifunsiro zathu zonse
Akulingana n’lino Tipemphere mbuyathu.
Atate atipatsa, Mtima phee tisowa tonse,
Kupempherabe bwino. Zitibvuta chabeko,
Ukamvatu chisoni, Kaamba sitimanka konse
Kwa Mbuye kapemphera. Kupemphera Mlunguyo.
Adzakusangalatsa, 2. Tili nazo zotiyesa,
Pemphero adzamvera. Zitidetsa nkhawamu;
Tisadandaule chabe,
198 Timpemphere Mbuyathu.
1. POKUPEMPHERANI Kodi tikaona wina
Mundiphunzitse ’ne Timkhulupiriremo?
Ndi Mzimu wanu Woyera, Yesu adziwa bwino,
Ndikayanjane nanu, Atate, Timpemphere yekhayo.
Ndi kukulemekezani ’Nu
2. Mdikumbutse zomwe 3. Kodi tikulema nazo
Munandichitira Zotiwawa m’mtimamo?
Ndikakuyamikireni, Atipulumutsa Yesu,
Ndikweze Dzina lomwe angelo Timpemphere iyeyu.
Aliimbira Kumwambako. Kodi adathawa ‘balo?
3. Mndimvetse chisoni Pempheratu Bwenzilo;
Pakuululira Akusunga m’mkono mwake,
Zochimwa zanga zambiri; Udzapumuliramo.
Mumtima ndi kupatsa mtendere
Mutachotsera zoipazo
200
4. Chikondi, chimwemwe, 1. ZOKOMA ndithu nthaŵizi
Chifatso, chiletso, Kwa Mlungu zondifitsadi;
Zipatso zonse za Mzimu Kumpando wachifumuwo
Mundibalitse, ndikafanane Ndiuza zanga zonsezo.
Ndi Mbuyathu popempherapo. Pobvuta ine mtimamo
5. Pakupempherera Nditulapo pa Yesuyo;
Anzanga ndi onse Pakuyesedwa ndinkatu
Akusokera mumdima, Kwa Mbuye, sindikhala duu.
Pakuyesedwa ndinkatu
Kwa Mbuye, sindikhala duu.
2. Zokoma inde nthaŵizi Ambuye yemwe,
Zotama Dzina lomweli Chitsime chomwe, njira yomwe
La Yesu, ndiwoonayo yokhulupirira;
Wopatsa dalo lonseli Tiyeni tonse, m’Mpingo ’modzi
Ndilakalaka Iyeyu tiziyenderana.
Wofera ine pansitu; 2. Atate yemwe anatuma Mpulumutsi
Pakuda nkhaŵa ine bii mmodzi
Nditchula Dzina lomweli, Kudzatifera kuti atiyanjanitse tonse,
Pakuda nkhaŵa ine bii Ndi Mzimu yemwe ayeretsa akumvera
Nditchula Dzina lomweli. onse;
3. Zokoma etu nthaŵizi Tiyeni tonse, m’Mpingo ’modzi
Ndicheza naye Mlungudi; tiziyenderana.
Koma kwathu m’Mwambamo 3. Anatipatsa Mawu omwe olimbitsa
Kumwona ndi koposako. mtima;
Pobvula ine thupili, Kumwamba komwe tinka ndi kulonda
Ndiloŵa Dziko lakedi; njira yomwe.
Ndidzati nthaŵi yomweyo; Tibalalikiranji ife akutsata Yesu?
“Tsalani bwino pansipo.” Tiyeni tonse, mMpingo ’modzi
Ndidzati nthaŵi yomweyo; tiziyenderana.
“Tsalani bwino pansipo.” 4. Satana apambana tikayamba kusiyana;
201 Tikayanjana, yemwe adzagonja ndi
kuthaŵa;
1. MTIDZUTSE, Mbuyetu,
Mbuyathu adzamthyola konse ndi
Mtionekeremu:
kumlamulira.
Munene zakukmvekazi,
Tiyeni tonse, m’Mpingo ’modzi
Timvere ifetu.
tiziyenderana.
Mtidzutse, Mbuyetu,
5. Tiphatikane tonsefe okonda Yesu
Mtipatse moyonso;
Kristu;
Mudzetu Mbuye, mudzetu,
Tisalekane pakugwira ntchito za
Tidalitseni ’fe.
Mbuyathu;
2. Mtidzutse, Mbuyetu,
Tilimbitsane pakuyenda m’njira yonka
Tikweze Dzinali:
kwathu.
Tiuzireni Mpweyawo
Tiyeni tonse, m’Mpingo ’modzi
M’mitima yathuyi.
tiziyenderana.
3. Mtidzutse, Mbuyetu,
Timvere Mawudi; 203
Zoona zanu tonsefe 1. MBUYE, Mpingo wanu usauka
Tikhulupire ’zi. kwakukuludi;
4. Mtidzutse, Mbuyetu, Kale lija munatsitsa Mzimu wanu
Mthirenso moyowo; Wakuyera;
Ulemu ngwanu nokha ’Nu, Lero linonso muchite, ulimbike
Dalitso nlathulo. Mpingo wanu.
2. Tidza kwa Mulungu Inu, ndinu
202 wachifundodi;
1. AKRISTU ndi abale, tiziyenderana
Mutipatse Mzimu wanu tsopanoli,
tonse,
Mulungu mmodzi tili naye, ndi
tere lino; 5. Pakufika tsidya lija,
Tikakhale ndi chimwemwe kuti tili Zotibvuta zonse phe!
mbike ndithu. Mfumu yathu yopambana
3. A! maliro m’Mpingo mwanu kulirira Idzatikondwetsadi.
’balewo 6. Nthaŵi yina adzadzuka
Adasokerera kale ndi zoipa zapa Ogonera m’mandamo,
dziko. Kuthaŵatu mphamvu zonse
Muwabwezerenso kwanu kuti akakhale Zotibvuta pansipa.
mommo. 205
4. Ndi chikondi mtithandize kuigwira
1. TADZUKA mzimu wanga’we
nkhondoyi;
Ugwire ntchito zakozi;
Mwa kulema ndi kulimba
Kukondwa ukutengedi,
mutipempherere
Pemphero ulikwezedi.
ife,
Pemphero, pemphero,
Kuti tilimbane naye Satanayo,
Pemphero ulikwezedi
osamwopa.
Pemphero, pemphero,
5. Pakubweradi Woyesa tidzamlaka
Pemphero ulikwezedi.
ifetu;
2. E, nthaŵi ya mamaŵayi
Angelonso adzabwera kutithandizira ife,
Umtamandire Mbuyeyo,
Kuti tilimbike ife ndi kumchotsa
Nuyese lero ngatitu
m’mtima mwathu.
Tsiku lakumalizalo.
6. Pa la Mulungu tibwera kulandira
3. Munkhani zako zonsetu
zidazo;
Unene molungamadi,
Mphamvu yanu ndi chikondi
Nudziŵe kuti Mbuyako
zititsogolere
Adziŵa zachinsinsizi.
ife;
4. Pa tsikuli, Mbuyanga ’Nu,
Machitidwe ndi mkhalidwe zikokere ena
Munditsogolere m’njiramo;
kwanu.
Ulemerero wanuwo
204 Undilimbitse monsetu.
1. AULENDO amayenda 5. Timlemekeze Mlunguyu
Muusiku wo’psyawo, Wa madalitso onsewo;
Namaimba nyimbo zawo Timlemekeze tonsefe,
Kunka kwawo m’Mwambamo. Atate, Mwana, Mzimunso.
2. Kuunika kuoneka 206
Koingitsa mdimawu;
1. KRISTU wakuyeratu,
Mbale amakondwerera,
Kristu wakuŵalayo,
Osaopa konse ’yi.
Wolungama mdzuketu,
3. Mlugu amaunikira
Muingitse mdimawo.
Anthu ake onsewo,
Dzuŵa lathu m’Mwambamo
Namachotsa mantha omwe,
M’wale m’kati m’mtimamo.
Nayeretsa m’njira mbee!
2. Konse kuli mdima bii
4. Anthu osaŵerengeka
Kosakhala Inutu;
Amtamira onsewa,
Nlosakondwa tsikuli
Nagonjetsa zosautsa
Mosaŵala Inu ’mu.
Pomtamira Mbuyeyo.
Ndionetu m’katimo Komatu mukhalitse ndinetu.
Mwakuŵala kwanuko. 4. E, tsiku lonse Inu ndifunitsa;
3. Mudze, mloŵe m’mtimamu, Ndi mphamvu yanu yokha ndisungika;
Mchotse monse mdima bii; Mukatsogola ndidzadikha m’mtima;
Mdzaze ndi kuyeraku, Usiku, msana, mkhale ndinetu.
Mchotse zosamverazi; 5. Adani sindiopa mukalipo
Ndi kuyera kwanuku Muletse tsoka ndi chisoni chino;
Ndikaone bwinotu. Ikadza imfa n’dzalimbika m’mtima;
M’moyo ndi m’imfa mkhale ndinetu.
207
1. AMBUYE munapatsa tsiku 209
Limene langopitali, 1. ATATE ndiyamika, mwandisamalira
M’mamaŵa nyimbo zathu zomwezo leroli;
Mukhale nafe nthaŵiyi Mulungu wandikonda, mndisungenso
Mukhale, mukhale, m’mdima muno bii.
Mukhale nafe nthaŵiyi; 2. Mundikumbutse, ndikapanda tulo, za
Mukhale, mukhale, Kumwambako;
Mukhale nafe nthaŵiyi. Zoganizira zoipitsa m’mtima
2. Tipempha kuti Mpingo wanu muchotseremo.
Ukhale ponse m’dzikoli; 3. Zochimwa za usana uno
Mumdima monse muŵaletu, mndikhululukire
Kuŵala kwanu kudzedi. ’ne;
3. M’maiko monse, zisi zomwezo, Mtendere wanu muloŵetse m’mtima
Kuŵala kumafikanso; ndikagone phee.
Kupempha sikuleka konse 4. Mundilimbitse ndikayese manda
Kuyamikira Yesuyo. ngati mphasayi,
4. Pogona ife, amadzuka Nditagonamo ndikadzuke tsiku
Abale akutaliwo; lomalizalo.
Panthaŵi yonse anthu ena 5. Tiyamike Mlungu wotipatsa
Alemekeza Mbuyeyo. zachifundozi,
5. Ufumu wanu, Mbuye Yesu, Amyamikire onse a Kumwamba ndi
Ukhale nthaŵi zonsedi; apansipa.
Magulu onse adzagonje, 210
Naloŵe m’njira mwanumu.
1. DZUŴA lapitira,
208 Wadza mdimawo,
1. MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa, Mthunzi wamadzulo
Wagwa usiku, bwenzi lindisoŵa; Wagwa m’mwambamo.
Ndilibe wina wakundithandiza, 2. M’mwambamo nyenyezi
Wamphamvu ndinu, mkhale ndinetu. Zithwanima mbee;
2. Kamoyo kanga katha lero lino, Zonse zili m’tulo
Zidzachokanso zinthuzo za dziko; Pansi pali duu.
Zimasinthika zonse zooneka, 3. Yesu mutipatse
Simusinthika, mkhale ndinutu. Tulo toti phee;
3. Koma kalelo mnakhalitsa pano, Ndi mdalitso wanu
Mukhale ndine, msandichokerenso, Mndigonetse ’ne
Sin’pempha kuti Mbuye mungotsotse,
4. Mpatse ana ’ng’ono Odwala anagona duu;
Alotemo mbee; Opwetekedwa nthendazo
Anthu aulendo Munachiritsa Inutu.
Msungesungebe. 2. Tsopano lino kwada bii,
5. Mutonthoze mtima Nafenso timva m’mtimamo;
Wopwetekawo; Simuoneka, komatu
Akutsata tchimo Tidziŵa muli nafedi.
Mletse onsewo. 3. Wopulumutsa mudzetu;
6. Wonsewu usiku Adwala ena m’mtima bii,
Andisunge ’ne Ena sakukondani ’Nu,
Amithenga anu Ena sasamalira ’yi.
Akuyera mbee. 4. Ndi ena sanamvera ’yi
7. Ndidzukanso m’maŵa, Enanso alemedwatu,
Kucha koti mbuu, Zoopsya nazo tifadi;
Ndiyeretu mtima Mukadza tidzaposatu.
M’maso mwanumo. 5. Wopulumutsa, Inunso
8. Titamadi ’Tate, Munasauka kalelo;
Mwana wakeyo, Muona zoda m’mtimamo
Mzimu Woyeranso, Tibisa ndi manyaziwo.
Nthaŵinthaŵizo. 6. Mutichiritse ifenso,
211 Mutiphunzitse zanuzi;
Timve tsopano mawuwo
1. DZUŴA lapita,
Ochiza nthenda yathuyi.
Dzuŵa lapita,
Mlungu, mutigonetse phee. 213
2. Mdima wafika, 1. MPULUMUTSI, tikagona
Mdima wafika Mtidalitse m’mtimamo;
Mutisunge tonse bwino. Tingolapa zakuipa,
3. Tibvomereze, Muzichotse zonsezo.
Tibvomereze Kukadetsa bii usiku,
Zakuchimwa zathu zonse. Inu mutipenya ’fe;
4. Mkhululukire, Simulema, simugona;
Mkhululukire Anthu anu msungabe.
Zoipa zathu zonse. 2. Atipsinjadi masoka,
5. Lero tigone, Mibvi iponyekatu;
Lero tigone, Atisungadi angelo,
Tigonemo mumtendere. Moyo mutipatsa ’Nu.
6. Ndife ananu, Ngatitu usiku uno
Ndife ananu, Ikabwera imfayo,
’Tate Mlungu wotikonda. Mtiukitse m’maŵa kwanu,
7. Aleluya! Mpatsenso zoyerazo.
Aleluya! 214
Aleluya, Aleluya!
1. MULUNGU wanga, Dzuŵatu
212 La mtima wanga ndinudi;
1. MADZULO aja kalelo Palibe mdima ngatitu
Mukaŵalira inedi.
2. Muchotse zonse zoti bii Munapuma tsikulo;
Zobisa nkhope yanuyo; Tipumadi ifenso.
Mudzazetu mtimangawo Mommo tilandiratu
Ndi kuunika kwanuko. Zopumitsa mtimawu.
3. Madzulo ano mkhaletu 4. Yesu munadzukanso
Pafupi ndine, Yesudi; M’manda lero lomwetu;
Ndisanagone tuloto, Ntchito munayambayo
Ndilingalira Inudi. Yakudzutsa anthu ’fe,
4. Kapena wina leroli Kuti ndi mitimayi
Wasokerera m’njirayi Tigwirebe ntchitozi.
Ya Inu Mbuye, mbwezetu, 217
Mumpulumutse iyedi.
1. AMBUYE, tasonkhana
215 Tsiku lino lopatula,
1. LERO mwatipatsa moyo, Tidzapembedza Inu
Wadza mdima, kwada bii; Tsiku lino lopatula.
Mtigonetsetu usiku, Bwenzilo lakufatsa,
Mchotse zakuipazi. Mbweretu kutipatsa
Yesu mutisunga ife; Mtima wakumvesetsa
Tidzakhulupirabe. Tsiku lino lopatula.
Yesu mutisunga ife; 2. Sitinanyalanyaza
Tidzakhulupirabe. Tsiku lino lopatula.
2. Ndife anthu aulendo, Tigwadirira m’mantha
Tili ndi adaniwo; Tsiku lino lopatula.
M’manja mwanu mtigonetse, Mbwezetu maganizo,
Mtichotsere manthawo. Mtimvetse malangizo;
Ndipo pakumuka ife, Tchimo mufafanize
Kwanu tidzapumabe. Tsiku lino lopatula.
Ndipo pakumuka ife, 3. Timvere Mawu anu
Kwanu tidzapumabe. Tsiku lino lopatula
216 Muŵadalitse ndithu
Tsiku lino lopatula.
1. KWACHA lero kwati mbee,
Mtiperekeze kwathu,
Tsiku la Mulunguli;
Msunge mitima yathu;
Dzuŵa liŵaliradi
Mpatse chisomo chanu
Thambo ndi zapansipa
Tsiku lino lopatula.
Upumira mpweyawu
Wa Mulungu konseku. 218
2. M’nyumba yanu, Mlungu, ’yi 1. DZUŴA la Mulungu
Tisonkhana teretu, Ladzatu labwino;
Ndi mitundu yonseyi Ndi chimwemwe ife
Tikulambireni ’Nu: Tiliona lero.
Yesu Mbuye wathuyo Lithaŵitsa nkhaŵa,
Ndiye Mfumu ponsepo. Lichotsanso mantha
3. Inu Mlungu kalelo Ndimo m’mtima mwathu
Mutalenga zonsezi Likhalitsa bata.
2. Tikondwera kuti
Tipumula lero; Timdikirabe.
Tazileka ntchito 221
Kuti tipemphere.
1. ANTCHITO a Mulungu ’nu
Koma ntchito zathu
Olinda m’nyumba mwakemo.
Za palero lino
Myamike, muimbiretu
Nzakumvera Yesu,
Mlungu Mbuye wathuyo.
Kumlandira bwino.
2. Mugwade pansi m’nyumbayo
219 Mpembedze nonse Mlungutu;
1. NDI lokoma m’Mwambamo, Mugadamire m’mwambamo.
Mbuye, Bwalo lanulo; Mtamande Mbuye wanutu.
Ndi mwabwino muli ’Nu 3. Yehova adalitse ’nu,
Dziko losachimwali; Ndiye wachifundocho,
Mtima wana wonsewu Asunge moyo wanuwu;
Umakhumba m’Mwambamo Amtame anthu onsewo.
Nkhope ya Mbuyathuyu, 222
Mlungu wa chisomoyo.
1. KWEZANI mitu yanuyo,
2. Zimbalame zonsezi
Zipata zamuyaya,
Zimayamikira ’Nu;
Ikaloŵemo Mfumu ya
Anthu amakondwanso
Ulemereroyo!
Okhumbira m’Mwambamo;
Amfumu awa ndaniko?
Njiŵa yosapumayo
Ambuye ndiyeyo,
Inafika m’chombocho;
Mulungu wogonjetsa onse,
Okhulupirira ’Nu
Wolimba mphamvu njo!
Amapuma kwanuno.
Mulungu wogonjetsa onse,
3. Anthu opembedzawo
Wolimba mphamvu njo!
Amakondwa m’mtimamo;
2. Tatsegukani inutu,
Munapatsa madzitu,
Zitseko zosathera,
Munagwetsa manawo;
Amfumu akumwambako
Mumakoma mtimatu
Aloŵe mwanumo.
Tidzayamikiratu,
Amfumu awa ndaniko
Pachimpando chanucho
Wolemereroyo?
Mkhale Mfumu yathudi.
Mulungu wa makamu ndiye,
220 Wolemereroyo.
1. YESU mkhale nafe Mulungu wa makamu ndiye,
Nthaŵi yomweyi, Wolemereroyo.
Kuti mphamvu zanu Aleluya, aleluya, aleluya, aleluya,
Tilandirezi. aleluya.
2. Mzimu Wakuyera Amen, amen, amen.
Mutipatsetu, 223
Mtima wathu wonse
1. MLUNGU ali muno,
Usakhale duu.
Tonse timgwadire,
3. Moyo watsopano
Mantha omwe timchitire;
Ulimbitse ’fe,
Ali mukachitsi,
Mlungu wathu yemwe
Tonse tili chete,
Ndi ulemu timpembedze; Alonjezetsa lero
Ndiye yekha Mlungu wathu Kutsata Mbuye onse
Atipulumutsa, M’ŵathangatire iwo
Tidzamlemekeza. Asabwerere konse.
2. Mwini madalitso, 2. Tsopano alandira
Mndikonzere m’mtima, Chizindikiro chanu
Mbuye, ndingokhulupira. Munachiika ndinu
M’Mwambamo angelo Cha Ubatizo wanu
Agwadira inu, Mulembe dzina lanu
Ife tigonjanso kuno; M’mitima mwa onsewa;
Mpingo wonse uchiitse M’ŵabatizenso Mbuye,
Chifuniro chanu. Ndi Mzimu Wakuyera.
Ponse pansi pano. 3. Muŵalimbitse onse
3. Yesu Mbuye wanga, Akhazikike m’mtima,
M’khale m’mtima mwanga, Akhale chikhalire
Ndiwotu kachisi wanu. Oyera ndi olimba;
Ikafika imfa, Mutithandize tonse
Mundisunge kwanu A Mpingo wa Mulungu
Kuli inu ndi angelo. Tikhale oyenera
Moyo wanga ulimbike Ndi okondana ndithu.
Kufikira ine
Ndidzakupenyani.
226
1. MONGA zomera zonsezo
224 Zikula ponsepo,
1. MTSINJE woyerawo Mulungu mumeretsazo,
Wotuluka m’nyumbayo Momwemo anawo.
Ya Mlungu wathuyo 2. Munali mwana, Yesu ’Nu
Uyeretse tonsefe. Wamng’ono kalelo,
Ife tifikeko Ndi munakula m’msinkhu ndi
Tibatizidweko, Kutama ’Tatewo.
Tiyeretsedwedi 3. Ndi ife tinga, mbewuzo
Ndi Ambuye leroli. Zomera m’mundawo;
2. Mwa anthu onsewo Mumtima mutidyetsedi,
Umayenda mtsinjewu, Tikule bwinomo;
Nuŵachiritsadi 4. Ndi kutsukidwa m’mwazimo
Okhulupirirawo. Mumtima mwathu mbee,
3. Tikondwereratu Tionetsedwe konseko
Pakumvera Yesuyo, A Mlungu ana ’ke.
Abwere onsewo
Ndi kuloŵa m’mtsinjewu.
227
1. USIKU uja kalelo
225 Anampereka Yesuyo,
1. ATATE, muwapenya Usiku womwe m’manja mbuu
Anzathu ali pano, ’Natenga mkate Iyeyo.
Abvomereza Inu 2. Natamandira Mlunguyo
Ambuye Mfumu yawo; Wolamulira pansipa,
Natema mkate, natitu
Kwa omwe anatsatawo; Ndi nkhope yanu dwii,
3. “Ndi thupi lopatsidwali Thukuta la pamphumilo
La Ine, mtenge, mudye, ndi La myazi yanuyi.
Muchite ichi nonsenu, 4. Ndi mtanda uli m’maso mbuu,
Ndi chikumbutso changatu.” Ndiona m’menemo,
4. Ndiponso m’manja chikhocho A Yesu kufa kwanuko,
’Nakweza, natamandamo Kuthetsa imfazo.
Mulungu, mtima wake mya, 5. Pamene padzakhalapo
Nanena mawu omwewa: Milomo yanga phee,
5. “Chikho cha mwazi wangachi Mukadza ndi Ufumunso,
Chitsuka mtima woda bii, Mukumbukire ’ne.
Cha mapangano omwewo 230
Chisomo cha Kumwambako.
1. MUDZE, anthuni, talaŵani ’nu
6. “Chikho cha mwazi wangachi
Mkate ndi chikhocho cha Mbuyathu.
Chitsuka mtima woda bii,
2. Khristu ndi mwini moyo wathuwu,
Cha mapangano omwewo
Pamtanda anafera ifetu.
Chisomo cha Kumwambako.
3. Anatifera nsembe Iyeyo,
228 Ndiye Wansembe wake Iyenso.
1. SINDILI woyenera ’ne, 4. Imfa ndi mdima zinathaŵa zii!
Ambuye, kudzamo; Ndipo chisomo chikuŵala mbuu.
Munene mawu, ndimvebe 5. Tadzanitu, okhulupiradi,
Okondweretsawo. Talandirani zachinsinsizi.
2. Sindili woyenera ’ne, 6. Ndiye wa moyo wonse Mwiniyo,
Mumtima mwanga zi; Moyo wosatha atipatsa ’fe.
Munene, ndikachiradi, 7. Ndiye wodyetsa anthu omwewo,
Ndilibe moyo ’yi. Napatsa mwazi, moyo wakewo.
3. Sindili woyenera ’ne; 8. Yesu Mbuyathu, Inu nomwe ’Nu,
Pamtanda panupo Tsopano mkhalebe ndi ifetu.
Munamaliza mlandu phe 231
Ndi mwazi wanuwo.
1. MOMMUNO, Mbuye tionanetu,
4. Ndilaŵako tsopanoli
Mommuno ndizikhudza zanu phee,
Zakudya zanuzo;
Mommuno zachinsinsi zanu mbuu,
Mudzaze mtima wanga ndi
Mwa Inu mtima ndipumirabe.
Kukonda kwanuko.
2. Mommuno, Mbuye, mkate wanuwu,
229 Mommuno vinyo wakumwambako,
1. MONGATU mawu anuwo, Mommuno zolemera zanga du,
Ndi Mtima chete phee, Chisomo chanu ndidzalaŵanso.
Mbuyanga kufa kwanuko 3. Ndilibe wondithangata ‘ne ’yi,
Ndikumbukire ’ne. Ndilibe wina wondisunga ’ne;
2. Chakudya chakumwambachi Zikwaniratu mphamvu zanuzi,
Ndi thupi lanudi; Ine, Ambuye, mphamvu nzanudi.
Chikho cha chipanganochi 4. Tsopano nthaŵi yake phwandoli,
Ncha mwazi wanuwo. Loyala ili m’gome mwanumu;
3. Getsemane ndionako Ndidye ndimwere zakukomazi,
Ndiyanjanabe nanu, Mbuyathu.
5. Chakudya ichi chidzapita du, Mukhaletu pafupi,
Chizindikitsa za Kumwambazo; Mundithangate ’Nu.
Zosapitazo tidzalaŵatu, 3. A! Yesu mwapangana
Za Yesu mwini wakukondako. Ndi anthu anuwo
6. Tikadya phwando zaka zonsezi, Adzakhala ndinu
Ndipo zakudya zimalozatu Ku Dziko lanulo;
Kuphwando lija la Kumwambako, Inenso ndapangana
Komwe tidzadya kwa Mulungutu. Ndisabwerere ’yi;
232 Mndipatse mphamvu yanu
Ambuye ndinudi.
1. NDIMAMVA njala, Yesu,
4. Mundionetse, Yesu,
Ya mtima wakusoŵa;
Mapazi anuwo,
Mdidyetse ngati mana
Ndidzapondera awa
Anagwa m’chipululu.
Munjira monsemo;
2. Ndimamva ludzu, Yesu,
Ndithangateni ine
Muloŵe mwanga lero;
Ndisalefuke ’yi;
Mndimwetse ngati madzi
Mundilandire m’Mwamba
Anatuluka m’mwala.
Ndikamwaliradi.
3. Ndi mkate wanu, Yesu,
Ndi thupi lobvulala, 234
Mndilimbikitse, Mbuye 1. MUNDIMVERE, Mbuye wanga
Mundikhutitse mtima. Nkana ine ndimalakwa,
4. Mwa chikho chokumbutsa Koma ndinu moyo wanga;
Chikondi chopambana, Mbuye, mkhale ndine.
Mndipatse moyo wanu, 2. Ndine mlendo pansi pano,
Ndikayanjane nanu. Msanditaye m’dzanja lanu,
5. Mndidyetse m’chipululu Mundisunge mwana wanu;
M’ulendo wanga wonse; Mbuye, mkhale ndine.
Mdimwetse, ndipirire 3. Munafera ine kale
Osalefuka konse. Kuti mukandimasule,
233 Lero lino mndinyamule;
Mbuye, mkhale ndine.
1. A!YESU, ndapangana
4. Mundidzaze ndi chikondi,
Kutumikira ’Nu
Mndiyeretse m’mtima monse,
Ndi moyo wanga wonse,
Chifuniro changa mthyole;
Mbuyanga ndinutu;
Mbuye, mkhale ndine.
Mukhaletu pafupi
5. Imfa ikandifikira,
Masiku onsewo,
Inu ndidzakangamira
Sindidzaopa konse,
Ndikaloŵa ine m’mdima,
Mutsogolereko.
Mbuye, mkhale ndine.
2. Ndikufuna kumva Inu,
E, Mawu anuwo, 235
Ndisamve za satana 1. ANU Mbuye ndifetu!
Zonyenga zakezo; Mutimvere kwanuko;
Adani anga onse Anu tikhalirebe
Andizingiratu; Kuno ndi Kumwambako.
2. Anu Mbuye ndifetu!
Mwanu tipumiredi; Njira yakuunika.
Ndinu Mbale wathu ’fe, 2. Mbiri ya Hananiyayo
Mutusunge nthaŵizi. Inali yodabwizatu;
3. Anu Mbuye ndifetu! Ananyengatu Peturo;
‘Dikireni tonsefe; “Zopereka ndinapereka.”
Moyo ndinu, n’choona, 3. Ife tonse tichenjere
M’njiramo tiyendebe. Tingadzachite zomwezo:
4. Anu Mbuye ndifetu! Tisaname ndi kunena:
Ndife nkhosa zanuzi; “Zopereka ndinapereka.”
Mwanu tibisalemu, 4. Mulungu akondadi leroli
Mwanu mosungikadi. Wopereka mokondwera;
5. Anu Mbuye ndifetu! Tikapereka motero
Tsogolani nthaŵizo; Tidzalandira dalitso.
Mtiyendetse m’moyomu
Kunkabe Kumwambako.
238
1. MBUYE wathu, mutipatsa
236 Zonse tili nazozo,
1. AMBUYE, Mwini zonsezi, Mutikomeratu mtima
Ulemu tiperekadi; Osaleka konseko,
Chikondi tionetsanji? Mutikonda, mutisunga,
Mwapatsatu. Mutisamalira ’fe.
2. Dzuŵa ndi mvula yonseyo 2. Dzuŵa, madzi, kudya, mpweya,
Ndi mame mwatipatsanso, Moyo, zonse nzanuzi,
Masika ’dzera kwanuko; Si za ife, nzaulere,
Mwapatsatu. Tingozilandiradi;
3. Mwapatsa Mwana wanu, ndi Zifumira kwa Aate
Mwapulumutsa dzikoli; Wotikondakondatu.
E, zaulere zonsezi 3. Monga tilandira, Mbuye,
Mwapatsatu. Mtiphunzitse tonsefe
4. Tibwezeretu bwanjiko Tipere chuma chathu
Ziperewera zathuzi; Ndi kusangalalatu;
Ndi moyo tili nawowo Zakukhala m’manja mwathu
Mwapatsatu. Tiziyese nzanudi.
5. Ambuye zathu zonsezi 4. Tikhaletu nawo, Mbuye,
Kwa Inu tibwezeredi; Mtima wosauma ’yi
Tingopereka zanuzi, Ndi wofatsa ndi wabwino
Mwapatsatu. Ndi woyerayeradi,
237 Kuti tiyenere Dzina
La Mbuyathu Yesuyo.
1. PETURO ’nafunsa Hananiya:
5. Tisaiwalire ’bale
“Zopereka zili kuti?”
Athu osadziŵa ’Nu,
Hananiya ananena:
Akulira ndi odwala
“Zopereka ndinapereka.”
Tiŵapemphereratu;
Munthu aganize
Titsanzenso Mbuye Yesu
Zimene anachita Hananiya
Ndi k’ŵathangatira ’wo.
Munthu aganize
6. Dalitseni, Mbuye, zonse
Zomwe taperekazi, Yake ya Wokondayo,
Mzilandire, nsembe yathu, Ang’ono akwezanso mawu
Mziyeretse Inudi Poimba nyimbo zawozo.
63 4. Ufumu wake udalitsa
Ndi mitima yathu yonse Osauka onsewo;
Tikuyamikirani. Otopa amapuma chete,
Magoli amathyoka thyo!
239 5. Zolengedwa zonse zidze
1. POLENGA dzikoli Kugwadira Mfumu yathu,
Pakumva Inudi, Amlemekeze akumwamba,
Kwayeratu; Tiimbe pansipa; Amen.
Mumve pempheroli,
Ndipo pamenepo 241
Palibe mawuwo, 1. ANTHU akum’maŵa
Muŵaletu. Nanka msangako,
2. Inu wakudzatu Nzeru ’nali nazo,
Kuŵachiritsadi Nafatsansowo;
Anthendawo, Nanka kuli Mwana
Kupatsa moyowo, Anabadwayo;
Kuona m’masomo, Anatsogozedwa
Pa anthu onsewo Ndi nyenyeziyo.
Muŵaletu. 2. Anapeza Mwana
3. Mzimu woonadi Ali m’kholamo,
Ndi wachikondicho, Nagwadira Iwo
Idzanitu; Mbuye wawoyo;
Muunikirepo Anthu onse omwe
Pali zamdimazo, Ali pansipa,
Pa dziko ponsepo Azitsata Mbuye
Muŵaletu. Ndi nyenyeziyo.
4. Inu atatuwo, 3. Mu ulemerero,
Wodala Mlunguyo, Yesu m’Mwambamo
Timveretu; Muli eni ake;
Pa dziko ponsepo Anthu onsewo
Muchotse mdimawo, Osadziŵa konse,
Mutume Mawuwo, Akutalinso,
Muŵaletu. Akokedwe iwo
Ndi nyenyeziyo.
240 4. Akukhala kunja,
1. ADZAPAMBANA Yesu ponse Osokeranso,
Pakuyenda dzuŵalo; M’ŵaŵalire Mbuye,
Adzamverabe namgwadira Asagone’wo;
Pa dziko lonse pansipa. Amumdima omwe,
2. Sadzalekeza kuyamika Olemedwanso,
Ndi kuimbaimbabe; Mtsogoleri wawo
Adzapemphera nsiku zonse Ndi nyenyeziyo.
Natchula Dzina lakelo. 5. Paulendo wathu
3. Pomveka konsekonse mbiri
Tili pansipa, Mitima yanu yonseyo iyeretsedwe
Muŵalire tonse mbuu!
Tili m’njiramo; 4. Tsatani Mbuye Yesuyo ndi
Mutitsogolere mtanda wakewo;
Anthu tonsefe, Mlaliketu Uthenga kwa anthu
Mutifitse tonse onsewo.
Ndi nyenyeziyo. 5. Musamaopa kanthu ’yi tamani
Yesuyo;
242 Kaimbireni nyimboyi ndi
mphamvu zonse.
1. Timva mawu omwewo
6. Zipata zatsegudwa mbee! za
Atitu: Yesuyo
m’dziko monsemo;
Mpulumutsi ndiyedi,
Ambuye wapambanatu ndi
Yesuyo, Yesuyo.
mtanda wakewo.
Pita m’midzi monsemo,
Dziko lonse limvetu, 244
Pita iwe konseko, 1. PAMAIKO pali mdima,
Mveratu mbuyeyo. Penya mtima chetetu,
2. IMbadi za iyeyo, Leroli malonjezano
Amvetu anthuwo Angokwaniridwatu.
Kuti Yesu ‘nafadi Kondwerani, kondwerani,
Kalelo, kalelo. Yesu mulitsetu.
Atikonda ifetu, 2. Adze amitundu yonse,
Natifera indedi Adze akutaliwo;
Kuchotsera chimoli, Ayang’ane mtanda uja
Yesuyo, Yesuyo. Woti nji paphiripo
3. Bukitsani mawunso Mbiri yanu, mbiri yanu
Konseko, konseko! Ibukitse ponsepo.
Kaitane anthuwo 3. Ponse padakhala mdima
Ponsepo, ponsepo. Pakaŵale dzuŵali;
Kodi wina samvatu? Kumalire konsekonse
Pitako, pitako ‘we; Muthaŵitse mdima bii!
Angofuna onsewo Mpulumutsi, Mpulumutsi,
Yesuyo, yesuyo. Muyeretse zonsezi.
4. Ibukitse mbiri yanu,
243 Ifikire konseko,
1. ZIPATA zachitsulo zitseguke
Iŵagwire anthu mtima,
zonse mbee!
Iŵathyole m’katimo
Ambuye wa Kumwambako aloŵe
Mphamvu yanu, mphamvu yanu,
momwemo.
Idziŵike konseko.
2. Mbendera yake ikupiza
m’mlengalengamo, 245
Kufana ndi nyenyezi younika 1. MBWERE Mlungu Mbuye
m’mdimamo. wathu,
3. Ankondo a Mulungu ’nu, Msunge zakuonazo,
Yendani m’njiramo, Mudalitse anthu onse
Ndi chifumu chanucho.
2. MMbwere Yesu Mwini moyo, Nagonjera konseko.
Ukuletu ’lemuwo; 247
Gonjetsani anthu onse,
1. Anthu ali m’mdima akuitanitsa
Mpatsenso mtenderewo.
Unikani! Unikani!
3. Mbwere Mzimu Wakuyera,
Alikumwazika mungawalanditse,
Mutitsitsimutseko;
Unikani! Unikani!
Muthaŵitse mdima wonse,
Muŵalitse m’mtimamo.
Tumizani kuunikako
4. Anthu onse taukani,
Kuoneketu kwa onsewo;
Imbirani Mlunguyo;
Tumizani kuunikako,
Zichuluke zomtamanda
Nthawi zonsedi kuwaletu.
Pansi ndi Kumwambako.
246 2. Tamva aku makedonyako atero,
1. ANYAMATA a Mulungu, Unikani! Unikani!
Muzigwira nkhondoyo, Tititu, Mbuye tizinka komweko,
Mumenyane ndi Satana Unikani! Unikani!
Mzimu wakunyengayo. 3. Tisaleme pakuchita zabwinozi,
2. Komwe asauka anthu Unikani! Unikani!
Akukhala m’mdimamo Tidziunjikire ngale
Osadziŵa Mpulumutsi, zakumwamba,
Phunzitsani konseko. Unikani! Unikani!
3. Pomangidwa anthu nayo
M’yambo yoipitsayo,
248
1. MUNENE Mbuye, ’nenetu,
Pomwe amaopa chabe,
Nditsanze mawu anuwo;
Masulani golilo.
Munandifuna Inetu,
4. Walitsani nyali yanu
Ine ndifune zanuzo.
Ikachotse mdima bii!
2. Nditsogolere m’njirayi
Mpaka ikainga zonse
Nkhosazo zisokerazo;
Zosautsa m’dzikoli
Ndidyetse Mbuye, zanuzi
5. Akutopa ndi ofoka
Zimene zifa njalayo.
M’ŵatonthoze mtima phee!
3. Ndilimbikitse, Mbuye, nji!
Osokera, onyozeka
Pamwalapo ndiimebe;
Muŵafunefunebe.
Onse alibe mphamvu ’yi
6. Achisoni obvutidwa,
Omwe ndithangate ’ne.
M’ŵathandize msangatu;
4. Ndiphunzitseni, Mbuyetu,
Zosautsa zawo zonse
Ndidziŵitse nzeru zanuzo;
Yesu azichotsadi.
Munole mibvi yangayi,
7. Anyamata limbikani,
Ipyole yonse m’mtimamo.
Gwiranitu nkhondoyi;
5. Ndipumulire panupo,
Yes salephera mwini,
Ndinene motonthoza phe!
Sitiiŵalira ’yi.
Ndi mawu opumitsawo
8. Isaleke ntchito yake
Olema ndikanenebe.
Mpaka anthu onsewo
6. Ambuye, ndi chikondi tho!
Alambira Mfumu yathu,
Mudzaze mtima wangawu;
Ndinene zachikondicho,
Ndiyamikire monsemu. Odza kuphunzira ’mu,
7. Ndichitireni, Mbuye ’ne, Ndi antchito anu omwe
Monse mufuna mwanumo; Odza k’ŵaphunzitsa ’mu.
Kumwamba tionane mbee, 3. Tiyamike Mlungu ’Tate,
Maso ndi maso kwanuko. Tiyamike Mwanayo,
249 Tiyamike Mzimu wake;
Onse omwe Mmodzitu,
1. MULUNGU wa Kumwamba
Waulemerero wonse
bwera kunoku
Ndi wamphamvu ponsepo.
Ndi mtima wokondwera kuloŵa
m’nyumbayi; 251
Chifukwa cha zabwino 1. ANAKWATIRA kale
mwatichitirazi Pa Eden pajapo;
Tikukuyamikirani leroli. Ulipo lero lino
Inde, tikuyamikani, Atate, leroli, Mdalitso womwewo.
Mwatimangira ’fe kuno kachisi 2. Aŵiri aimamu,
wanuyu! Mwamuna ndi mkaziyu;
Ndi ulemerero wanu mudzaze O! Mzimu Wakuyera,
m’nyumbayi; Mdalitso mpatsetu.
Muyeretse, mudalitse munomu. 3. Mulunzanitse awa,
2. Tikondwa tonse ndi Atate, leroli;
kukuthokozani ’Nu Munakwatits’ Adamu
Poyamba kupemphera ndi Ndi Hava kalelo.
kuimbiramu; 4. Mukhale nawo, Yesu,
Mommuno nsiku zonse mukhale Mongatu kalelo
nafetu, Ukwati mnadalitsa
Monga ndi angelo anu Pa Kana pajapo.
m’Mwambamo. 5. M’ŵasunge, m’ŵayendetse
3. Ikhale ngati nyali yoŵala Munjira yanuyo,
nyumbayi, Akhale ndi kudala
Yakutsogoza onse ophunthwa Pabanja pawopo.
m’mdima bii; 252
Akunja ndi Akristu
1. YEHOVA Mlungu wathu,
m’ŵapulumutse ndi
Amene mumapatsa
Kuunika kotuluka munomu.
Zipatso za chikondi
250 Polenga anthu anu,
1. KRISTU ndiye Mwala wathu, Mupatse awa ‘ŵiri
Kristu timangirapo; Mitima yokondwetsa,
Wosankhidwa ndi Mulungu, Yofana m’munda muja
Atimange tonsefe; Munayendamo kale.
Iye ndi Mthandizi wathu, 3. Mbuyathu wokondedwa,
Timkhulupirira ’Ye Pokhala m’dziko muno
2. Mudalitse nyumba yathu; Munadza ku ukwati,
Mbuye, nthaŵi zonsetu Naŵadalitsa onse;
Muthandize anthu onse Ukwatiwu mukonze,
Mukhale nafe pano;
Iwowa m’ŵadalitse Mtsogoleri wathu ndinu
M’chifundo chanu chonse. Paulendo pomwepo
4. Ndi Mzimutu Woyera Tingakutameni bwanji
Mufike nayo mphamvu, Kaamba zonse zanuzo?
Mukatsangane nawo 2. E! Chisomo chosaleka
Akupangana omwe; Tachiona kalelo;
Mupatse ’wo chisomo Masungidwe ndi chikondi
Chokometsetsa mtima; Zikalimo momwemo;
Chikuletu chikondi Pausana, pausiku,
Chitsazo nchanu chomwe. Muli nafe ponsepo;
5. Mulungu mwa Atatu, Madalitso anu omwe
Atate, Mwana, Mzimu, Tiri ndi ambiriwo.
Tikhaletu wokondwa 3. Tinayenda muli mdima
Ndi Inu m’chiyanjano; Wotidetsa nkhaŵawo,
Titama Inu Mlungu, Pena tinangosauka
Wokonda ife ndinu; Ndi zobvuta zathuzo;
M’ulendo wathu wonse Koma Inu munalimo
Tiyende m’chikondano. Mumitambo yomweyo,
253 Nafe tinathandizana
Ndi mdalitso wanuwo.
1. MULUNGU wa Yakobo Inu,
4. Ena atsagana nafe
mdyetsa anthu anu,
Natsiriza njirayo,
Kalelo munatsogolera makolo
Nafikira kuli Inu,
athuwo.
Natilindirirako;
2. Tsopano tipereka mapemphero
Tithadi ulendo wathu
athu ano.
Ndi kupita komweko,
Mulungu wawo mukhalenso
Mutitsogolere ’Tate
Mlungu wa anawo.
Kukuŵala kosatha.
3. Tikasokera m’njira mutilondolere
ndithu, 255
67 1. MBUYE, tikuthokozani,
Chakudya ndi chobvala mutipatse Ndinu mwatitsogolera;
tsiku n’tsiku. Zaka zonse mwatisunga;
4. Mtifungatire ndi mapiko Tiyamika mokondwera,
paulendo pathu, Zotibveka, zotidyetsa,
E, tikafike okondwera kwa Atate Mphamvu, moyo, zonsezi;
wathu. ’Tate tikuthokozani
5. Tipempha madalitso ano mpatse Chaka chatsopanochi.
ife tonse; 2. Ndinu mwatithangatira
Tisankha Inu ndinu Mlungu wathu Pakuona zosautsa;
nthaŵi zonse. Polefuka ndi podwala
Ndinu mwatitsitsimutsa.
254 Munatiteteza bwino
1. MLUNGU wathu mwatifitsa Tili ana kalelo,
Kufikira leroli; Ndipo zomwe mwazichita
Moyo wathu munasunga Chaka chotitheracho.
M’njira yonse yathuyi;
3. Chaka chino mutipatse Mitima yoyamika.
Mphamvu zosachimwa konse, 257
Zoipitsa ndi zodetsa
1. YAMIKANI nonse ’nu,
Mtima mtichotsere zonse.
Pomwimbira nyimbozi Za
Mtithandize tizimvera
masika athuwa;
Kuyambira leroli,
Potumiza mvulayi,
Ndi kugwira ntchito zanu.
Mlungu wathu yemwedi
Chaka chatsopanochi.
Atipatsa zonsezi;
4. Inde,’Tate, mtiyendetse
Timwimbire m’nyumbayi
M’njira yolungama yanu,
Za masika athuwa.
M’mtima mwathu mtiyeretse
2. Dziko lathu lonseli
Kuti tikondane nanu.
Nla Mulungu yemweyu;
Zaka zonse muli nafe,
Atumiza mphatsozi
Sitiopa konse ’yi
Zakutilimbitsadi,
’Tate tikuthokozani
Mmera wathu wonsewu,
Chaka chatsopanochi.
Mbewu zathu zonsezi;
256 Timtamande Mbuyeyu
1. TILIMALIMA m’minda, Wotipatsa zonsezi.
Tibzala mbewu zathu, 3. Nthaŵi yina Mbuyeyu
Komatu zibvumbidwa Adzafika pansipa,
Ndi Mlunguyo wamphamvu. Nadzakonza zonsetu;
Dzuŵalo aŵalitsa Zosakondweretsazi
Namatumiza mphepo, Naziponya m’motowo,
Mbewuzo nameretsa Koma m’nkhokwe mwakemo
Mulunguyo wabwino. Mudzadzala mbewu tho!
Mphatso zonse zathu Zokomera bwinotu.
Zifuma kwa Mulungu, 4. ’Dzani Mbuye msangatu,
Tilemekeze Mbuye wathu, Msonkhanitse zonse phe;
Atikondadi. Anthu anu onsewa
2. Wolenga ndi Yemweyo Muŵapulumutse ’wo;
Wa zinthu zonse zathu; Zopweteka zawozo
Maudzu ameretsa, Ziŵathere zonse phe;
Nayatsanso nyenyezi. ’Dzani mu Ufumu ndi
Mphepo zonse zimva, K’ŵasonkhetsa onsewo.
Nyamazo aziŵeta; 258
Sadzaiŵala konse
1. OYAMIKA Mlungu mbwere,
Anake kuŵadyetsa.
Za masika mudzaimbe;
3. Tiyamikira ’Tate,
Dzinthu zathu takolola,
Zabwino zonse zino,
Sizionongeka m’minda.
Kubzala ndi kukunkha
Mlungu Mlengi asamala,
Ndi moyo tili nawo.
Zotisoŵa akonzera;
Kuninkha Inu Mbuye
Mloŵe m’nyumba ya Chauta,
Tilibe mtulo wina,
Mkweze nyimbo zamasika.
Komatu tipereka
2. Dziko lonse nla Mulungu
Kuti limbalire dzinthu;
M’munda zonse zimamera Timgwadiretu.
Zakukoma ndi zoipa; 6. Nafenso tidzadzuka kwa ’kufa
Mmera udza, bwino ngala, ngati maluŵawo,
Maso omwe amakhwima; Timlambire Mbuye;
Mutilole, Mwini dzinthu, Oyera mtima adzabvala mbuu! pakudza
Tikakhale dzinthu zanu. Kristuyo,
3. Adzabwera Mbuye wathu Timgwadiretu.
Kukolola dzinthu zawo; 7. Tidzakhala naye nthaŵi zonse ndi
M’munda mwawo akachotse kuimbako,
Minga ndi zoipa zonse. Timlambire Mbuye;
Adzatumanso angelo Kumene moyo wa anthu
Minga akaponye m’moto, okhululukidwa uli wokomatu,
Koma tirigu amsunge Timgwadiretu.
M’nkhokwe yake nthaŵi zonse. Aleluya, Amen!
259 260
1. CHIFUKWA cha zokoma mtima 1. MLENGI wathuWakuyera,
zonse za ulerezo, Mutimvere ’fe,
Timlambire Mbuye; M’ŵasungire akutali,
Tikweze nyimbo yathu Bwinodi.
yakukondwa kuli ’Ye, 2. Mbuye Yesu, myandikire
Tigwadiretu. M’ŵakondwetsebe;
2. Dzinja lokondweretsa lafikanso, Mulimbitse mphamvu zawo
litapumatu, Zonsezo.
Timlambire Mbuye; 3. Akaona masautso
Mvula igundanso, Mulungu Mkhale nawodi;
wotikonda ’fe, Akondwere mwa chikondi
Tigwadiretu. Chanucho.
3. Dziko lonse lilikukondwa, 4. Mpulumutsi wakukoma,
mlengalenga mpheponso, Muŵagwirize;
Timlambire Mbuye; Nsiku zonse akulemekezeni,
Zapansi pano zonse zimtamandire (Akuleme-keze.)
Mlungu wathuyo, 5. Mzimu wanu Wakuyera,
Timgwadiretu. Aŵayeretse;
4. Maluŵa abwino aphuka m’mapiri Agonjetse ndi chisomo
ndi m’madambomo, M’nkhondoyi.
Timlambire Mbuye; 6. ’Tate, Mwana, Mzimu ,ndinu
Masamba aŵisi ang’ono Mlungu mmodzitu,
agwedezekanso, Muŵasunge m’fupi mwanu
Timgwadiretu. Ponsepo.
5. Zanu zapansi nzokoma Mbuye; 261
Tikondwera ’fe,
1. YESU, munditsogoza
Timlambire Mbuye;
M’njira yanga yonseyo;
Koma kwanu Kumwamba komwe
Wakunditsogozatu
Kwapambanatu,
Ndinu, mundisungetu;
Inde, paulendowo
Mundisunge kolimba. Ndikatamandetu
2. Monga may’asusunza Wondisamalabe,
Mwana wake polira, Mbuyangayu.
Wakunditonthozatu 264
Ndinu, munditonthoze,
1. A! MULUNGU
Ine, m’njira yanuyi
A! Mulungu
Munditsogoleretu.
Anatuma mwana wake
3. Mbuye, ndinu wamphamvu,
Uja, ndiye Yesu
Mumatola ananu.
2. Anabadwa,
Anthu onse pansipa
Anabadwa
Ali otaikatu;
Ndi Maria Mbeta ija
Muchitire chifundo,
M’Betlehem muja.
Muŵatole onsewo.
3. Ndi angelo,
262 Ndi angelo
1. MLUNGU alinane; Anaimba: “Ndiye Yesu
Amadziŵazi Mpulumutsi wanu.”
Ndizinena, penanso 4. Alanditsa,
Za mumtimamo. Alanditsa
2. Mlungu alinane Ife anthu muzoipa
Ndi usikuwo, Zonse tazichita.
Nandiona momwemo 5. Yesu Mfumu
Mu usanamo. Yesu Mfumu,
3. Mlungu alinane; Timagonja, mutisunge
Zachinsinsizo Moyo wathu wonse.
Zosaonekerako 6. Mutisuke,
Azidziŵatu. Mutisuke
263 M’mwazi wanu, tikakhale
Ana anu tonse.
1. MLUNGU, Inutu,
Mwalenga dzuŵali,
Nyenyezi, mwezi mbee, 265
Ndi dzikoli. 1. Taonani m’kholamo
2. Koma ineyu Mwabadwira Mfumuyo
Simuiŵala ’yi; Yakulonjezedwadi,
Mundisamala ’ne Nsembe yathu ndiyeyu.
Ndisagwe ’yi.
3. Mbuye, Msungi ’Nu, Kondwerani nonsenu
Mutuma indedi Pomvetsedwa mbiriyi
Za moyo wangawu Yakumveka m’msindomo;
Zokomazi. “Wabadwira m’betelehemu.”
4. Yesu Mwanatu
Anafa imfayo 2. Adagona m’ndyeromo
Achotsa zoti bii; Wachokera m’mwambayo,
Nadzukanso; Adasiya mpandowo
5. Kuti m’Mwambamo Yesu Kristu Mfumuyo.
3. Falitsani mbiriyi,
Inudi abusa ‘nu; Munagona m’kholamo;
Nkhosa zanu zonsezo Mudzikonzere leronso
Mwasiy’ranji mphirimo? Mogona m’mtima mwangamu.
4. Pochezera m’dambomo, 6. Ulemerero m’Mwambamwamba
Tinaona ‘ngelotu Ndi mtendere pansipa;
Oimbira mawuwo Tiimbe nafe nyimboyi,
A mtendere pansipa. Timyamikire Mbuyathu
5. Mwana wakuyera ‘Nu, (Yesu ndiye Mfumu,
Munakonda ifedi; Yesu ndiye Mfumu!
Munasiya kwanuko Ndikhulupirira Yesu wobadwira
Ndi kufika pansipa. m’kholamo.)
6. Mtiphunzitse bwinotu,
Mwana wakuyera ‘Nu,
267
1. ANA inu, ana inu,
Tifanane nanudi
Taukani ndi kumvera
M’makhalidwe anuwo.
Amithenga akumwamba;
7. Tamverani, aitana;
Anafika kalelo,
“Ana, munditsatetu.”
Natiuza Mpulumutsi
Yesu, tisapite kwina,
Anabadwa pansipa.
Tizikutsatani ‘Nu.
Zaka zonse, tsiku lomwe
8. Posachedwa tilekana
Umamveka mthengawu.
Osalankhulananso,
2. M’nyumba zonse ponseponse
Koma tidzaona tonse
Zimamveka nyimbo izi,
Wina mzake m’mwambamo.
Kuti Yesu anabadwa,
266 Anagona m’kholamo,
1. TIIMBE ndi kulalikira Anafika Mpulumutsi
Mthenga wa chikondicho Wotikondweretsadi,
Anamva Mlungu m’Mwambamo Kondwerani, kondwerani
Kulira kwathu pansipa. Inu nonse ana ’nu.
(Ndikhulupirira Yesu 3. Taukani, taonani
Wobadwira m’kholamo; M’mwamba monse mwakuyera;
Iye ndiye Mfumu yathu, Amithenga a Mulungu
Timtame nthaŵi zonse.) Aimbabe nyimboyo.
2. Kwa ife lero anabadwa Yesu Kristu anatsika,
Mwana wa Mariyayo, Anachoka kwawoko;
Pamsinkhu, ine mng’ono koma Lero lonse tiimbenso
Mwini dziko lonseli. Nyimbo yathu yomweyo.
3. Anadza nazo mphatso zake 268
Anatikonzeratu;
1. KALE m’mzinda wachifumu
Anatitseguliradi
Munalimo m’kholamo,
Pakhome pa Ufumuwo.
Momwe mkazi anaika
4. Ambuye takutamandani
Mwana wake m’ndyeromo.
Tsiku lakubadwali,
Ndiye mkaziyo Mariya,
Mwa Inu tonse tikondwera,
Yesu Kristu Mwanayo.
Tiseke tonsefe.
2. Uyu ’natsikira kuno,
5. A! Yesu Mbuye wakuyera,
Mlungu Mbuye wathuyo; Ife tonse anthuwo
Anabadwa uyu m’khola Attenga Mlunguyo.
Anagona m’ndyeromo. Mlemekeze “Tate,
Mwa osoŵa ndi oipa Mwana, Mzimunso.”
Yesu anakhalamo.
3. Mwa ubwana wake wonse 270
Anakula m’mtima phee!
1. Kale anthu m’kholamo
Anakonda, anafatsa,
‘Napembedza mwanayo.
Amay’ wake namvabe;
Ndipo ana nonsenu,
Ndiye Mbuye, Mfumu yanga,
Mukamtsate bwinotu.
Ndiye Mbuye wa kumwamba,
4. Ndipo Mwana uyu Yesu
Amgwadira anthuwo,
Anakulakulabe;
Timtamande Mfumuyo.
Ndi wamng’ono ndi wofoka,
Anagona enawo.
2. Wosauka iyedi
Nsoni zathu anazimva
Anagwira ntchotozi
Ndi chimwemwe chathunso.
3. Ndani kodi mbuyathuyo
5. Ndi chifukwa atikonda,
Woyesedwa m’bwinjamo?
Tidzampenya masowa,
4. Analira ndaniyo
Kuti Mwanayo wofatsa
Pomwalira Bwenzilo?
Ndiye Mwini m’Mwambamo;
Atengera ana ake
Aleluya! Aleluya!
Komwe adapitako.
Timwimbire Yesuyo.
6. Koma sitimpenya m’khola
Aleluya! Aleluya!
Muli ng’ombe momwemo;
Timwimbire Yesuyo.
Ayi, tidzamwona m’Mwamba
Muli Mlungu ’Tatewo.
5. Iye anachoka kwawo,
Ana akuyera mbuu
Anakhala pansipa.
Adzamzunguliratu.
Kale ana ‘namwimbira
Namukondweretsadi.
269 6. Anafika ‘kazi omwe
1. Usikuwo oyerawo! Ndi tiana tawoto;
Mwana adamlerayo Yesu anatiyangata,
Akakhale Mfumuyo. Anatidalitsatu.
Anabadwa mkholamo, 7. Amithenga akumwamba
Mfumu ya mamfumu Amamuyamikiratu;
Ndi ya anthuwo. Zikwi zosawerengeka
2. Mwanayo wa Mulunguyo Zimtamanda Mfumuyo.
Andikonda inetu, 8. Ana inu yamikani
Nan’tayira chumacho Bwenzi lanu lomweli;
Nadzagona m’udzumo. M’mwamba momwe
Ndiyamika mbuye mudzampenya
Wanga Yesuyo. Ndi kumtamandirabe.
3. Usikuwo woyerawo! 271
Wadzatu mtendere
1. KULI kaphiri m’talimo
Kunja kwa mzindawo, 5. Ana inu, yamikani
Kwapachikidwa Yesuyo Bwenzi lanu lomweli;
Nafera ifetu. M’Mwamba momwe
(Kuli kaphiri m’talimo Mudzampenya
Kunja kwa mzindawo, Ndi kumtamandirabe.
Kwapachikidwa Yesuyo 273
Nafera ifetu.)
1. ANANU, ziimbani,
2. Zoopsya sitidziŵapo
Aleluya, Amen.
Anazitengazo,
Ambuye tamandani,
Komatu tidziŵitsa ’fe
Aleluya, Amen.
Anatiferapo.
Kwezani mawu anu,
3. Anatifera tonsefe
Patsani mtima wanu,
Tiwomboledweko,
Afuna kumva inu,
Tifike momwe m’Mwambamo
Aleluya Amen.
Ndi mwazi wakewo.
2. Bwerani, kondwerani,
4. Kulibe wokwanira ’yi
Aleluya, Amen.
Kulipa mlanduwo,
Ambuye akumvani,
Wina wakutsegula ’yi
Aleluya, Amen.
Pakhomo pakepo.
Amatitsogolera,
72 Kalelo natifera,
5. Anatikondakonda ’Ye, Kukonda salekera,
Timkonde ifenso; Aleluya, Amen.
Tizimtsatira, tithetu 3. Mbuye timlemekeze,
Zintchito zakezo. Aleluya, Amen.
272 Kwawo tikabwereze,
1. ANA inu, myamikeni Aleluya, Amen.
Mpulumutsi Yesuyo, Kumwamba timtamire,
Kaamba ka chikondi chake Tikamgwadire ife,
Ndi chipulumutsocho Tikhale chikhalire,
Aleluya! Aleluya! Aleluya, Amen.
Timwimbire Yesuyo. 274
Aleluya! Aleluya! 1. MNANDIDZERA, Ambuye,
Timwimbire Yesuyo. Kumwambako,
2. Iye anachoka kwawo, Munasiya akuluwo;
Anakhala pansipa. Koma m’mudziwotu
Kale ana ’namwimbira Munabadwamo
Namukondweretsadi. Munasoŵa pogonapo.
3. Anafika ’kazi omwe Idzani mumtima mwanga,
Ndi tiana taoto; Muli malo a Inu ’mo.
Yesu anatiyangata, 2. Amithenga ’naimba pamlengapo,
Anatidalitsatu. Nalalika ulemuwo;
4. Amithenga akumwamba Koma Inu munadza mofatsatu,
Amamyamikiratu Munabadwa mukholamo.
Zikwi zosaŵerengeka 3. Zili nazotu nkhwimba zirombozo,
Zimtamanda Mfumuyo. Ndi mbalamenso zisatu;
Koma Inu Ambuye mwapandadi Kopani anthu abwere kwa Inu.
Potsamira mutu duu! 276
4. Munanenatu mawu a moyonso
1. ANA a Yerusalemu
Omasula ochimwawo;
Anatama Mbuye wawo;
Koma omwe ochimwa
Lero lomwe ife ana
’Nanyozatu,
Timwimbira nyimbo yawo.
Nakuphani pamtandapo.
Mverani, aimba anawo,
5. Pakubweranso Inu m’Ufumuwo
Mverani aimba anawo
Ndi zamphamvuzo zanunso,
Zakutama, zakutama,
Mundimvetse za kwanu
Zakutama Mbuyeyo.
Kumwambako
2. Tamva tikondane naye,
Kuli malo a ine ’ko.
Tiŵerenge Mawu ake,
Ukondwere mtima wanga
M’njira mwake tiyendemo,
Pakumvera zokomazo.
Tiziimba nyimbo zake.
275 3. Aphunzitsi, ana omwe,
1. AKAZI anadza kwa Yesu Ndi akulu, t’imbe tonse;
ndi anawo, Nyimbo zathu zidzakwera
Anaŵaletsa anyamata nawakana Zikamveke m’Mwamba monse.
ndithu; 277
Ambuye naŵapezadi,
1. OSANATU, osana,
Anati: “Musatero ’yi
’Naimba anawo;
Lolani ana abwere kwa Ine,
M’kachisi wa Mulungu
Lolani ana abwere kwa Ine.
Mwamveka nyimboyo.
2. “Ndidzaŵalandira, k’ŵasunga
’Nalemekeza Yesuyo
M’manja mwanga;
Wak’ŵadalitsayo;
Ndi Mbusa wao Inetu, msachotse
Anamuyamikira
ana anga;
M’ubwana wawowo.
Akandipatsa mtimawo,
2. Kuphiri la ’Zitona,
Adzanka ndine Kwathuko;
Mumpingo wa ’nthuwo,
Lolani ana abwere kwa Ine,
’namkupizira mnjedza
Lolani ana abwere kwa Ine.”
Naimba nyimboyo,
3. Wokoma Mbuyathu kwitana ana
Angelo akumwambako
onse;
Napokerezanso:
Atsalanso ambiri ena sanamvera
“Osana m’Mwambamwamba
zake;
Kwa Mlungu wathuyo.”
Sanamva mawu akewo,
3. Zitsamba zakuyera
Sadziŵa kuti ’natinso:
’Naponya pansipo;
“Lolani ana abwere kwa Ine,
Kukondwa kunamveka
Lolani ana abwere kwa Ine.”
Paphiri ponsepo.
4. Afike masiku akuti anthu onse
Ambuye yemwe Mfumutu
Adzamva mawu anu ndi kutsata
Nakwera cheteko;
Inu nokha;
Tiana toyamika
Muwale m’mtima mwawomo,
Sanatinyozato.
Adziŵe muŵakondanso;
4. “Osana m’Mwambamwamba!”
Nyimboyi t’imbenso
Pokhala Kristu Mfumu Ine ntachimwa amandikumbusta:
Ndi Mpulumutsiyo. “Lapa mwana ‘we, akukonda Yesu.”
Timtamandire Iyeyu 4. Ndikadzaona Ambuye Kumwamba,
Ndi mtima wonsewo; Sindidzaopa pokhala akonda;
Tipite kwawo komwe Anandikonzera kalelo nyumba,
Tikaimbirenso. Ndidzakhalamo wokondwa, wokoma.
278 280
1. NGOLIZO zilira 1. NDIKONDA mbiri yomwe Ya
Za ’mithengawo, amithengawo
Ndi zipata zonse Ya Mbuye, Mfumu yathu Pofika
Zatsegudwa mbee! pansipa;
74 Zochimwa zindizinga, Koma ndidziŵatu
Kristu, Mfumu yathu, Anawombola ine
Mbuye wathudi, Pakundikondadi.
Wapambana monse, 2. Ndikondwa kuti Yesu
Alamulabe. ’Nakhala mwanatu,
Ntchito zake zatha, Chitsanzo atipatsa
Timwimbiretu; Cha moyo wakewo;
Yesuyo wakwera, Ndikati ndimtsatire
Timtamandetu. Zochita zakezo,
2. ’Natipulumutsa Sadzandinyoza konse
Natiferako, Pakundikondadi.
Ali mfumu ndithu 3. Pakumyamika Iye
Kwa Atatewo; Ndidzamwimbiratu;
Osasautsidwa, Ngakhale sindimwona
Osafanso ’yi Amandimveradi;
Yesu, Mfumu yathu Pakuti walonjeza
Adakweradi. Adzalandira ’ne
3. Atipempherera Ndiimbe ndi angelo,
M’malo ’dalawo, Pakundikondadi.
Tinke kwathu komwe
Ndi chisomocho; 281
Akonzera malo 1. YESU andikonda ine,
Ana akewo; Amatero m’Buku Iye;
Akafoka mwana wake
Yesu alipobe,
Atikondanso. Adzamlimbikitsa Mbuye.
Yesu akonda,
279 Yesu akonda
1. NDIKONDWA kuti atate wa Yeu akonda,
m’Mwamba Atero m’Bukumo.
Atidziwitsa chikondicho chake: 2. Anandifera Mbuye wanga
Ndimawerenga m’Uthenga Wabwino Anditsegulire m’Mwamba,
kuti Ambuye akonda anake Ndi machimo anga onse
Ndikondwa kuti yesu akonda, Adzandichotsera konse.
yesu akonda, andikondabe,
Ndikondwa kuti yesu akonda,
3. Mbuye Yesu andisunga
yesu akonda, Andikondabe. M’njira ya Kumwamba kuja;
2. Yesu ndimkonda,, akondanso ine, Andigwira m’dzanja langa
Anandifera pamtanda woopsa. Ndingagweremo m’makwaŵa.
wosayera, woipa ndi ine; 4. Yesu andikonda ine;
Tsoka langlo Ambuye ‘nachosta. Ndikadzafa tsiku lina
3. Mzimu woyera akala mwa ine, Atengera ine kuno,
Atsimikiza chikondi cha Yesu; Ndikakhale naye Kwawo.
282 1. YESU Mbuye ’Nu wofatsa Muyang’anedi
kamwana,Mndichitire chifundo;
Mfumu yakumveka;
Mundilole kwanutu. Ife sit’yenera,
2. Ndimalira kwa Inutu, Koma mutimvere.
Mpatse mtimawo wabwino; 3. Ndife akuchoka,
M’Dziko lanu loŵalalo Mwina tisokera;
Mulandire mwana wanu. M’njira ya Kumwamba
3. Yesu, E, ndikufunani, Mutitsogolere
Ndinu chuma change chonse; 4. Mutiletse, Mbuye,
Mtima wanu ngwofatsadi; Lero tisachimwe;
Kale munali kamwana. Tikondane ndinu
4. Wonga Inu ndikhaledi, Mutitsuke m’mtima.
Mtima wanu mundipatse; 5. Mukatiitana
Yesu ndinu wokomatu, Tikakhale kwanu,
Mndiphunzitse kukonda ’Nu. Tidzayankha, “Mbuye,
5. Yesu Mbuye ’Nu wabwino, Tsopano tili pano.”
M’manja mwanu ndikhalemo; (Yesu, Yesu,
Mzimu wanu mundipatse, Tikugwadirani
M’mtima mwangatu mukhale. Mwana wa Mulungu!)
283 285
1. YESU, ndikabwera 1. MPULUMUTSI, Mbusa wathu,
Mundikondweretsa, Mutitsogolere ife;
Nsoni zanga mun’chotsera Mutiŵete, mutisunge,
Zonsezo. M’khola mwanu mtilandire
Ndikabwera, Mbuye; Yesu wathu, Yesu wathu,
Ndidzakondwera ine; Mnatigula ana anu.
Muitana ana onse 2. Ndife ana, mutikonda,
Onga ‘ne M’njira mutiperekeze;
2. Yesu, ndikabwera, Mchotse nsoni ndi zoipa,
Mumva mapemphero Osokera muŵabweze:
Mundikonda, mnandifera Yesu wathu, Yesu wathu,
Inetu. Mumve mapemphero athu.
3. Yesu, ndikabwera 3. Munanena mulandira
Dzanja mdzandigwira Osauka ndi oipa;
Nokha mdzandilongolera Inu ndinu wachifundo
Njirayo. Ndi wamphamvu yolanditsa
4. N’takafika kwanu Yesu wathu, Yesu wathu,
Ndidzakhala bwino, Tidzatu tiana tanu.
N’dzaonana ndi ananu, 4. Tifunitsa Inu tere,
Ndi Yesu. Chifuniro chanu ndicho;
284 Mbuye wathu, Mpulumutsi,
1. YESU wa Kumwamba, Mutikonzetu m’katimo;
Mutimvere ife; Yesu wathu, Yesu wathu,
Tikugwadirani, Mutikondebe ana anu.
Mwana wa Mulungu. 286
2. Ndinu wakuyera 1. MZINDA woyerawo
Konse nkotsekako; Mutimvere, Yesu.
Kanthu koipa, 3. Ife tikondana nanu,
Kanthu koipa, Tiimbira nyimbo zanu,
Sikangaloŵemo. Tiyamika mphamvu yanu;
2. Yesu ndafikatu, Mbuyanga kwanuku; Mutimvere, Yesu.
Mundiyeretse, 4. Lero mkhale nafe ndithu,
Mundiyeretse, Poseŵera ndi pantchito,
Popemphera ndi poimba;
Mnditsuke m’mtimamu.
Mutimvere, Yesu.
3. Mbuye, ndikhaletu
Mbuye wokonda ’Nu, 5. Mutiletse tisaname
Ndi wosungidwa, Ndikunena zotukwana,
Ndi wosungidwa, Mtiphunzitse kukondana;
Ndi mphamvu zanuzo. Mutimvere, Yesu.
4. Mpaka ndabvala mbuu! 289
Wowomboledwatu, 1. YESU atiuza tiŵale ’fe.
Woyera mtima, Monga nyali m’mdima
Woyera mtima, tiunike mbee!
Kwanu Kumwambako Pansi pali mdima ŵalanitu,
287 Inu m’malo mwanu ndi ine ’mu.
1. MBUYE, tili ana anu, 2. Yesu atiuza tiyambemo,
Tiyamike Inutu; Ationa bwino ndi kuŵalako;
Zinthu zonse zili zanu, Ayang’ana pansi poŵala ’fe,
Tingadike m’mtimamo. Inu m’malo mwanu ndi ine ’mu.
Tiganize zake Yesu, 3. Yesu atiuza tiŵale pa
Za Kumwamba kuli ’Ye; Anthu ali m’mdima osaukawa;
Tisachite zomsautsa, Tiŵalire onse, tonsefetu,
Aziona zonsezo. Inu m’malo mwanu ndi ine ’mu.
2. Amakumbukira zonse 290
Tizichita zomwezo. 1. ANYAMATA inutu,
Tidzamukomana tonse, Anamwali inunso,
Sitinyazitsidwako. Muti: “Tingachitenji,
Mukhululukire ife Ang’ono ndifetu,
Tchimo lathu lonselo. Kuthandiza Ufumu
Mutitsogolere ife Wa Yesu?”
M’njira ya Kumwambako. 2. Aphunzitse anthuwo,
288 Aŵalalikiredi,
1. YESU, muli pa chimpando Akukhala moipa
Chakuŵala mbee! Kumwamba; Mumdima wakunja,
Mutipenye ife ana; Aloŵetu m’Ufumu
Mutimvere, Yesu. Wa Yesu.
2. Ife ana sitiopa, 3. E! ang’ono ndifetu,
Nzeru sizimafika
Mukabwera mutiona,
Tamva kale mutikonda; Kuti tingaphunzitse;
Titani tonsefe
Kuthandiza ufumu
Wa Yesu? Yesu ndi woyera;
4. Inu nonse anzanga, Ana ake omwe
Tiziganiza bwino, Aziyera m’mtima
Tinganene mofatsa, 3. Mzimu wakuipa
Timverenso Mbuye Ukusuzumira,
Kuthandiza Ufumu Umakuyesera
Wa Yesu. Kuti ukachimwe.
5. Pothandiza amathu, 4. Koma usalole
Pak’ŵakonda anzathu, Mawu a Satana;
Pakusiya zoipa, Bweza tchimo lake,
Pokhaladi bwino, Chita zolungama.
Tithandiza Ufumu 5. Yesu ndi Mbuyako,
Wa Yesu. Mbuyeyo ngwabwino;
291 Ana ake omwe
Aziyera m’mtima.
1. TIANA ife tingofoka,
Sitikhala ’mphamvu ’yi; 293
Tikhoza kukachitiranji 1. TCHIMO musalole,
Yesu kumkondwetsadi? musadziipitse,
2. Tiana ta Ambuye tili Myese kudzikana, muzilimbikadi;
N’ntchito yaikuludi, Mwamphamvu mpirire, mgonjetse
Kudzichepetsa ndi kusiya zabiizi;
Tchimo lili lonseli. Mpenye kuti Yesu adzakusungani.
3. Kapena m’mtima ndimakwiya, Mpemphe Mbuye asunge,
Nditukwana mnzangayo, Atonthoze m’mtimamu,
Kapena ndidzitama - izi Alikukufunani,
Ndilekere Mbuyeyo. Akasunge inutu.
4. Ndileke kulimbana ndi 2. Mleŵe oipawo, ayi musatukwane,
Kuŵanamiza enawo; Dzina la Mbuyathu
Ndinene zakufatsa, muzilikwezadi;
Zakukondweretsa Yesuyo. Khalani achangu, oona, abwino;
5. Tizikondana, tisekere Mpenye kuli Yesu,
Tsiku lonse kwathuko, adzakusungani.
Muyere m’mtima popeza 3. Yesu alandira akupirirawo;
Yesu ndi Woyerayo. Chikhulupiriro chiŵathandizadi
6. Palibe mwana wakuchepa Mbuye athangata onse akumvera;
Kunyamula mtandawu; Mpenye kuli Yesu,
Ambuye Yesu mutipatse adzakusungani.
Mtima wokondanatu.
294
292 1. NTHAŴI yaubwana yatha,
1. USACHIMWE konse, Sukulu yathu yathanso;
Lekatu kukwiya; Nkhaŵa ndi zoŵaŵa zomwe
Uli mwana wake, Zitibisaliranso.
Mwana wa Mbuyathu. 2. Yesu wakufatsa mtima
2. Yesu ndi wofatsa, Mlendo pansi pano ’Ye,
’Natifera, natisunga, Poyendayenda ’ne;
Atitsogolere ’fe. Paŵala mosekera
3. Tamverani, aitana; Ndi dzuŵa loti mbee!
“Ana, munditsatetu,” Ndikondwa nsiku zonse
Yesu, tisapite kwina, Ndikali m’dzikoli,
Tizikutsatani ’Nu. Potsata Yesu m’njira yake
4. Posachedwa tilekana Yonseyi.
Osalankhulananso, 2. Ulendo ungoyamba
Koma tidzaona tonse Wakunka kwathuko;
Wina mnzake m’Mwambamo. Amati: “Udzapeza
295 Zakusautsa ’mo”
Zobvuta ndi chisoni
1. YESU ndiye Mbusa,
Sindiziopa ’yi;
Mbusa wakukoma,
Ndidzangomtsata Yesu m’njira
Anyamula ana
Yonseyi.
Ake akuopa;
3. Zoipa ndi zabwino
Tizitsata Yesu,
Zakundigwerazo,
Atitsogolera,
Ndingonka nazo zonse
Kwina kuli mdima,
Ndimuze Yesuyo;
Kwinanso koyera.
Zoŵaŵa adzachotsa
2. Yesu ndiye Mbusa
Zondiliritsazi;
Atipenyetsetsa,
Ndikangomtsata Yesu m’njira
Mawu ake onse
4. Zondipingitsa zonse
Atikondweretsa.
Zoloŵa m’mtimamo
Mwina alangiza
Achotsa, nandisunga
Mwana wakulakwa;
M’ulendo wonsewu.
Atsogola bwino,
Sindidzaopa kanthu,
Ife tizimtsata.
Ngakhale imfayo,
3. Yesu ndiye Mbusa,
Pomtsata Yesu yekha kunka
Anafera kale
Kwathuko.
Kuyeretsa ana
Nawo mwazi wake, 297
Tsono awalemba 1. MPULUMUTSI Yesu,
Ndi chizindikiro; Mumve nyimbo yathu;
“Ana anga onse Tikuyamikani
Andikhulupira.” Mumitima mwathu
4. Yesu ndiye Mbusa Zonse tili nazo;
Wakutisunga ife, Thupi, mzimu womwe,
Ali wachifundo Inde, moyo wonse,
Chachikulu ndithu; Tipereka zonse.
Sitiopa imfa Komwe ndi Chimwemwe
Akakhala nafe, Tidzaimba tonse,
Yesu Mbuye wathu Tidzatama Mbuye
Alandira ife. Osalema konse.
296 2. Tiyandika, Mbuye,
1. POMPANO pandikonda
M’fupifupi ndinu, 1. M’MANJA a Yesu wanga
Tikugwadirani, Ndilikugonamo,
Mutilandire bwino. Mommo aphimba ine
Inu munatsika Nacho chikondicho.
Kutifera ife; Mvera! Mudzera m’Mwamba
Inu munakwera Mawu a Yesu wanga:
Kuti titsatire. “Mwana, ndidzakusunga
3. Haya! Tipitenso Pano pamtima panga,”
M’njira yomwe ija M’manja a Yesu wanga
Ana a Mulungu Ndilikugonamo,
Onse adaponda. Mommo aphimba ine
Tizisiya zonse, Nacho chikondicho.
Tiziyenda msanga, 2. M’manja a Yesu wanga
Tisamachewuka Nkhaŵa zonsezo zi!
Mpaka tipambana. Momwe zoipa zanga
4. Tero tidzakwera Sizindibvuta ’yi
Kwawo kwa Mulungu, Mmomo mulibe nsoni,
Tidzaziiŵala Mommo mokoma monse
Zotibvuta ife. Sindiliramo msozi,
Komwe ndi Chimwemwe Ndikondwa m’mtima monse.
Tidzaimba tonse, 3. Mtima umabisala
Tidzatama Mbuye M’manja mwa Yesumu;
Osalema konse. Mbuye, musunge ine,
298 Munandifera ’ne.
Ndilinda mopirira
1. Ine ndine mlendo
Mpaka wochoka mdima.
Wa Kumwambako;
Ndikaonana naye
Pansi pandikonda,
Yesu Ambuye wanga.
Koma mpoipa.
2. Kwathu nkopambana, 300
Nkosachimwako; 1. YESU ndiye Bwenzi lathu,
Zosautsa zonse Kumwamba kuli kwao;
Sizikhalamo. Amatikonda tonse,
3. Koma azibvala Akulu ndi tiana;
Mwana zoti mbuu! Anzathu sapirira
Wosachimwa konse Amalekana nafe,
M’mtima mwakemu. Komabe kutiyanja
4. Yesu, mndiyeretse, Saleka Yesuyo.
Mndimveretsedi; 2. Ana ake adzapuma
Mzimu, mndiyendetse Kumwamba mokondwera,
Mn’jira yanuyi. Amene anamkonda
5. Ine ndine mlendo Namtsata Yesu yekha;
Wa Kumwambako; Sauko ndi zobvuta
Kundiyandikira Zotitopetsa kuno,
Kwathu komweko. Sitiziona konse
299
Kumwamba kwathuko. Ndi amithenga omwewo
3. Tidzalandirabe komwe Akondwerera kokhako.
Zobvala za mitima Nkoti mbee! Nkoti mbee!
Yoyera, ndi kubvula 2. Zochimwa siziloŵako,
Zakale za kuchimwa; Mwayitu! Mwayitu!
Chimwemwe ndi chikondi Misozi m’maso mwawo yi.
Tidzangokhala nazo, Mwayitu! Mwayitu!
Za ndewu ndi chisoni Chisomo chili m’mtimamo,
Sitizipeza ’yi. Aona nkhope yakeyo
4. Woyenera ndani kunka Ya Yesu adalitsawo.
Kukhala ndi Atate, Mwayitu! Mwayitu!
Kuimba nyimbo zake, 3. Oipa tili tonsefe;
Za Mpulumutsi wathu? Mwaziwo, mwaziwo,
Tidzamka ife tonse Wa Yesu watigulatu;
Tamtsata pansi pano; Mwaziwo! Mwaziwo!
Tiyeni ana onse, Tiyeretsedwa nawowo,
Yambani leroli. Mtendere wa Mbuyathuyo
301 Ukhala nafe komweko.
Mwaziwo! Mwaziwo!
1. yesu adza kuwerenga
Ana ake abwino. 303
1. DZIKO lilipolo
Ndikuvala zachifumu Lokondwatu
Zakuwlazo ake. Oyera ’khalamo,
Ana ake angonga Abvala mbuu!
Nyenyezi zamwamba, Tamvani nyimboyo:
“Mfumu tiyamikeyo,
Adzawala m’ufumu Mkwezeni Dzinalo
Wa ambuye yesu. Mwimbenibe.”
2. yesu adza kukundika 2. Tiye kudzikolo,
Tiyeni ’nu;
Ana ake ankhosa.
Musakayikebe,
Ndiye mbusa wakufatsa Muchedwatu.
Namalizatu lero. Tikondwekondwedi,
3. kudzachera tsiku lijalo Tchimo ndi zoipa zii!
Mbuye timwona ndi
Msangatu msanga,
Kukondwabe.
Kudzawala m’mawa wake 3. Maso a m’dzikomo
Pompano Onse nga mbuu!
Mkono wa ’Tatewo
302 Ngwosungatu.
1. KWA Yesu ndi kwabwinoko, Tiye ku dzikolo,
Nkoti mbee! Nkoti mbee! Mgwire ’nu ufumuwo.
Kulibe zoipitsako, M’mwamba mwa dzuŵamo
Nkoti mbee! Nkoti mbee! Tikhalebe.
Kuimba amaimbako, 304
1. DZUŴA liŵala, m’tulotu 307
’Tate chikondi chanucho
1. AMBUYE, mtidalitsetu,
Chindidalitsapo.
Musunge Mawu m’mtimamu;
2. Dzuŵa la lero lonseli
Muyatse moto wanuyo,
Mundisungire ’ne;
Chikuletu chikondicho.
Mchotse zoipa zangazi,
Pokhala moyo imfanso,
Nanu ndikhalebe.
Ambuye mtiŵalirepo.
3. M’mtima mwangamu mloŵemo,
2. Laloŵa dzuŵa, kwada bii!
Mwini chifundocho,
Mwapenya ntchito zathuzi;
Kuti ndikafananetu
Taletsa mwini tchimolo,
Ndinu Mbuyangayo.
Mwinanso tangolakwapo.
305 3. Mufafanize m’bukumo
1. Yesu Mbusa, mutimvere, Zolakwa zanu zonsezo,
Dalitsani ifetu, Ndi kutipatsa ifetu
Ndi usiku mutisunge, Mtendere wanu m’katimu.
Tidzukenso bwinotu. 4. Chimwemwe chomwe mpatseko
2. Lero lino mwatipatsa Ndikukondana ndinunso
Zonse tili nazotu, Tifuna kufananadi
Moyo womwe; miyamiko Ndi Yesu Bwenzi lathuli.
Landireni Mbuye ’Nu. 308
3. Tchimo lathu lonse, Yesu,
1. TIKUTHA kupemphera,
Mukhululukire ’lo;
Tipita kwathu tonse;
Mtitengere kwanu komwe
Mtiperekeze Mbuye,
Kumpumulo wanuwo.
Panjira zathu zonse;
306 Titamva Mawu anu,
1. TILIKUIMBA nyimbo yomweyi, Mawuwo ndi amoyo,
Yakuyamika Mbuye wathuyo; Aloŵe m’mtima mwathu,
Mtendere wake tiufunadi, Akhazikikemo.
Titapemphera tinke kwathuko. 2. Ambuye, Mzimu wanu
2. Titanka kwathu mkhale nafeko, Atikumbutse tonse,
Tikufunani Yesu Mbuyathu; Atithandize lero
Musunge ife nthaŵi zonsezo, Kumvera Mawu onse.
Mutiyeretse m’mtima mwathu Kumudzi mkhale nafe,
mbuu! Musatisiye konse;
3. Usiku uno mutisungedi, Machimo onse mletse,
Khalani m’fupi m’nyumba Tiyere m’mtimamo.
mwathumo;
Mamaŵanso mudzatidzutse nji!
309
3. TIMYAMIKIRE Mlunguyo,
Kuti tigwire ntchito zathuzo.
Anthu ndi zinthu zonsezi,
4. Mtitsogolere nthaŵi zonsezo;
Ndi onse a Kumwambako
Kuyenda tokha sitikhoza ’yi,
Mlungu amyamikiredi.
Ngati mukhala Mbuye m’fupimo,
Sitidzaopa kanthu kena ’yi. 310
1. MULUNGU akhale nawo
ulemerero ndi dalitso,
Ndiye Atate, Mwana, 3. Ayamikire ’Nu
Mzimu Woyera, Mlungu mmodzi; Padziko ponsepa,
2. Tsopano, poyamba paja, Mitundu yonse ipfuule
Masiku onse alinkudza Mokondweratu.
Mphamvu, ulemerero, 4. Pakuti mfumuyo
dalitso, chipambano. Ndi Inu nokha ’Nu;
311 Mudzalangiza bwinotu
Mafuko onsewo.
1. YEHOVA, Mbusa wangadi,
5. Zipatso zakezi
Ndilibe kusoŵa;
Labala dzikolo;
Andigonetsa bwinoli
Adzadalitsa ifetu
Mumsipu wokoma.
Mulungu wathuyu.
2. Ku madzi ake odikha
6. Adzadalitsa ’fe
Anditsogolera;
Mulungu mwiniyo;
Ndi moyo wanga wofoka
Padziko ponse anthuwo
Aulimbikitsa.
Adzamuopatu.
3. Anditsogolera m’njira
Zakulungamazo; 313
Chifukwa changa ay’, koma 1. NONSE okhala pansipa,
Cha dzina lakelo. Muyamikire Mlunguyo;
4. Ndipyola kodi chikhwaŵa Ndi nyimbo mtumikire ’Ye;
Cha mthunzi wa imfa? Mubwere mokondweratu.
Ndilibe mantha ngati ’Nu 2. Yehova ndiye Mlungudi,
Mundiperekeza. Anatilenga yekhayo;
5. Chakudya changa chabwino Amatidyetsa ake ’fe,
Mwandikonzera pha! Ndi nkhosa zake ifetu.
Pamaso pa adaniwo 3. Loŵani m’Nyumba mwakemu
Mudyetsa mtimanga. Ndi nyimbo zokondweretsatu;
6. Mwadzoza mutu wanga ndi Mumyamikire Mlunguyo.
Mafuta okoma; Mulemekeze Dzinali.
Mwadzadza chikho changadi, 4. Pakuti Mbuye Mlunguyo
Inde, chisefuka. Wokoma mtima ndiyedi,
7. Zokoma ndi zakuyanja Woona adzakhalabe
Zidzanditsatako; Kunthaŵi nthaŵi zonsetu.
Ndikhala m’nyumba ya Mlungu 314
Ku nthaŵi zonsezo.
1. MULI ndi ludzu, idzani
312 Kumadzi amoyo
1. MULUNGU, anthu ’fe Imwani monse kolere
Mutidalitsetu; Kuchitsime konko.
Chisomo chiŵalire ’fe 2. Munka kangati kulaŵa
Cha nkhope yanuyo. Madzi onyengera?
2. Potero onsewo Musataye mphamvu yanu,
Okhala pansipa Musataye chuma.
Adzamva bwino msangatu 3. Imvani, Yesu akuti;
Za njira yanuyi. “Chuma ndili nacho,
Landirani, yemwe amva Lidzakhala nthaŵi zonse
Akhale ndi moyo.” (Nthaŵi zonse).
4. Funani Mlungu tsopano. 8. Tonse timyamiketu,
Akulindirani; Tonse timyamiketu,
Iye ndiye wachifundo, Mpulumutsi wamuyaya
Akulandirani. (Wamuyaya).
5. Ali wokhululukira; 316
Imvani ananu:
1. AITANA, aitana dziko lonse,
Mtima wake usiyana
Imvani mukhaliranji chete?
Ndi mitima yathu.
Aitana,
6. Monga m’Mwamba mupambana
Aitana aitana dziko lonse.
Zonse pansi pano;
2. Mfumu iyi, Mfumu iyi ya
Choncho maganizo ake
Kumwamba
Apitira athu.
Ndi Yesu, ndi Mpulumutsiyo wa
7. Anthu onse a padziko
anthu onse.
Adzamvera Mlungu:
Anthu onse, anthu onse, tinke
Adzakhala ndi chimwemwe,
kwawo.
Nadzamtama ndithu.
3. Aitana,aitana inu mayi,
315 Ndi Yesu, amene anakhetsa
1. TIYAMIKE Mlunguyo, mwazi wake;
Tiyamike Mlunguyo, Mwazi wake unagwera inu mayi.
Watidzera ndi mtendere 4. Aitana, aitana inu ’tate,
(Ndi mtendere). Ndi Yesu amene anakhetsa mwazi
2. Anatuma, Mtetezi, wake;
Anatuma Mtetezi, Mwazi wake unagwera inu ’tate.
Ndiye Mfumu Yesu Kristu 5. Yesu ati, Yesu ati; “Muzisiye
(Yesu Kristu). Zoipa zimene muzichita,
3. Tifunafunatu, muzisiye,
Tifunafunatu, Muzisiye, muzisiye inu nonse.”
Osapeza Mpulumutsi 6. Titi bwanji? Titi bwanji ife anthu?
(Mpulumutsi). Ndi Yesu anatifera ife
4. Tifunafuna m’phirimo, akuchimwa;
Tinafuna m’phirimo, Akuchimwa, akuchimwa tinke
Koma osampeza mommo kwawo.
(Osampeza).
5. Tinafuna m’nyanjamo,
317
1. ’TATE, ’Nu.
Tinafuna m’nyanjamo,
’Tate ’Nu, mtione ’fe
Koma osampeza mommo
Tadza kupemphera kwa Inu.
(Osampeza).
2. Imvani,
6. Yesu ndiye Mtetezi,
Imvani Amfumu ’Nu
Yesu ndiye Mtetezi,
Mawu athu tinena lero.
Wina saoneka ayi
3. Tipempha,
(Saoneka).
Tipempha mdalitsetu
7. Dzina lake Yesuyo,
Mpingo wanu woyera uno.
Dzina lake Yesuyo,
4. Imvani, Aleluya Bwenzilo!
Imvani akunjawo Amakonda, amasunga;
Akulira opanda Yesu . Ndimufuna Yesuyo.
5. Ayenda, 2. Yesu ndiye mphamvu yanga,
Ayenda munjirazo Andilimbikitsatu;
Zakupita kuchitayiko. Poyesedwa ndi adani
6. Ambiri, Andipambanitsadi.
Ambiri akufadi 3. Yesu atonthoza mtima
Osadziŵa za Kristu Yesu. Ndikadera nkhaŵa ’ne
7. Auke, Pakukhala ndi chisoni
Auke akristuwo, Andisangalatsabe.
Akakhale antchito anu. 4. Yesu ndiye Mtsogoleri
8. M’ŵatume, Pakuyenda m’njiramo,
M’ŵatume antchitowo Ndipo ndikafuna kugwa
Alalike Uthenga wanu. Andigwira dzanjalo.
9. Ubwere, 5. Yesu ndimafuna Inu,
Ubwere Ufumuwo, Mwapambana zonsezo;
Uoneke padziko ponse. Mlamulire mtima wanga,
318 Mndikhalitse wanutu.
1. PEREKANI mtima wanu, 320
Yesu aitana nonsenu; 1. ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,
Osauka, amasiye, Ŵalira Yesu m’ntchito zakozi,
Yesu anakuferani ’nu. Ŵalira Yesu pofanana ndi
Perekani, perekani Ambuyathu Yesu Kristu.
Mtima wanu nonsenu; Tiŵaliretu, tiŵaliretu
Yesu akulindirani, Ambuye Yesu wotikonda ’fe;
Perekani mtimawo. Mlemekeze ’Ye tsiku lonseli,
2. Tsegulani mtima wanu Ine tiŵalire Yesu.
Nonse, Yesu akaloŵemo; 2. Ŵalira Yesu pazobvutazo,
Akuchimwa, Iye adzaloŵa nazo Ŵalira Yesu pakukondwanso,
zakukomatu. Ŵalira Yesu, imbirani ’nu
3. Mtembenuke mtima wanu, Ambuyathu Yesu Kristu.
Inu osamvera Mlunguyo; 3. Ŵalira Yesu wolimbitsayo,
Yesu aitana ife Ŵalira Yesu m’moyo monsemo
Tikamtsate m’njira yakeyo Ŵalira Yesu; tidzaonatu
4. Perekani mtima wanu Ambuyathu Yesu Kristu.
Kwa Mbuyathu Mpulumutsiyo, 321
Ndiye wakudziŵa kuchiritsa
1. ZAMBIRI zogona m’kholamo,
Anthu akuchimwatu.
Zosungika bwino ’mo;
319 Koma imodzi inasokeradi,
1. YESU, Bwenzi la ochimwa, Nitayika m’thengomo
Yesu wondikondable, Kutali kuphiri loopsalo,
Ena samandikwanira, Kutali ndi mbusa wakeyo.
Yesu salephera ’yi. 2. Ambuye, muli nazo zambirizi,
Aleluya Mpulumutsi!
Kodi sizifikirazi? Maumtima muli mwai;
Koma Mbusa nanena, “Yangayo Ndi Yesu ndikondanetu,
Yatayika naneyo; Si kanthu kena ’yi,
Ngakhale njira njoopsadi, Si kanthu kena ’yi.
Ndilinga kuphiri kuipezanso.” 323
3. Koma zina sizinadziŵa ayi,
1. ATATE Wamkulu ndi
Makwaŵa ’napyola ’ye,
Wamphamvu zonse,
Ndi mdima woopsa WA usikuwo
Atate Wamkulu ndi wamphamvu
Ambuye nailonda yake.
Zonse,
Anamva kulira kutaliko,
Khalani ndi chifundo ndi ife lero.
Naipeza yofoka, yakufayo.
2. Ifetu kuchimwa timachimwa,
4. Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
Mbuye,
Panjira ponsepo?
Ifetu kuchimwa timachimwa,
“Ndaukhetsa potsata iwetu,
Mbuye,
Kukubweza ku kholalo.”
Mutume Mzimu wanu
Ndi m’manja mwalaswa
Atiphunzitse.
Bwanjimo?
3. Mwa Mzimu muloŵe mumitima
“Ndalaswa ndi minga pofuna
Yathu,
Iwe.”
Mwa Mzimu muloŵe mumitima
5. Ndi ponse paphiri ndi padambopo
Yathu,
Ndi makwaŵa, indetu,
Zoipa zathu zonse mtiululire.
Kunakwera kupfuula
4. Tafika Kwa inu mutiunikire,
Kumwambako,
Tafika kwa inu mutiunikire,
“Kondwani, ndaipeza yanga!”
Chifundo chanu chonse taleka
Nd’ angelo a Mlungu
lero.
nabwezanso,
5. Tifuna kuchita chifuniro chanu,
“Kondwani, Ambuye ’napeza
Tifuna kuchita chifuniro chanu,
yawo.”
Chifundo cha Mulungu
322 nchabwino chokha.
1. MUTHIRE, Yesu, m’mtimanga 6. Atate, mupatse zomwe
Kukonda kwanuko: tapemphazi,
Mwa Mlungu ndidzalimbika, Atate, mumpatse zomwe
Ndisasokerenso, tapemphazi,
Ndisasokerenso. Tapempha m’Dzina lake la
2. E, moto wanu woyera Mpulumutsi.
Uyake mwa ine; 324
Utenthe zonse zoti bii,
1. ONA Mwanawankhosayo
Undiyeretsedi,
Wakuseza zakuipa zathu zonse.
Undiyeretsedi.
Mwanawankhosa
3. Munagwa pa Atumwiwo;
Watisenzera
Dzazani mwa ine;
Zakuipa zathu zonse.
Mzimu wamoto Woyera,
2. Anazenza m’thupi mwake;
Ndipempha mudzetu,
Pakukhomedwa pa mtanda anali
Ndipempha mudzetu.
duu.
4. Ndikhazikike inetu,
3. Ona pamtanda Yesuyo Ithamange m’ntchito yanu
Anabvutika chifukwa cha anthu Yokhayo.
’fe. 6. Ndi milomo yathu iyinso njanu,
4. Imva kulira kwa Yesu Ilalike Mawu anu kwa onse.
Pamene anasiyidwa muimfayo. 7. Ndi makutu athu awanso nganu,
5. M’mwazi wake tisambamo; Muŵamvetse Mawu anu okhawo.
Zichotsedwa zakuipa zathu zonse. 8. Tidziperekadi konse Kwa Inu
(Ona Mwanawankhosayo Tikakhale anthu anu okhawo.
Wakusenza zakuipa 327
Zathu zonse.)
1. ATATE, ndipempha
325 Tsopano mundimvere,
1. YESU analikhanda Ndipempha kuti mundithandize.
M’Betlehemumo; 2. Ine ndili munthu
M’ngelo anasimba za Wochimwa pansi pano,
Kubadwa kwake. Munditsuke Mbuye, ndiyeretu.
Kubadwa kwa Yesu 3. Ndalema ndathodwa
M’Betlehemumo; Ndi zinthu zapadziko,
Khandalo linagona Zakhalatu goli londimanga.
M’khola la ng’ombe. 4. Yesu Mfumu Inu
2. Mngelo anatumidwa Mumandiuza kuti:
Kuŵasimbira “Pemphera, ndipo udzalandira.”
Abusa a nkhosa za 5. Ndipempha, Ambuye,
Kubadwa kwake. Mundidzaze n’chikondi,
3. Anapita nasiya Mtima wangawu ukukondeni.
Nkhosa zawozo;
Anapita kumudzi
328
1. DZIKO lonse mlambire
Kukamlambira.
Yesu Mbuye wathuyo,
4. “Tadodoma, abusa,
Muimbire ndi chimwemwe
Kwachitikanji?
Dzinalo.
Mwazisiyira yani
2. Mbwere nonse muone
Nkhosa zanuzo?”
Zomwe achita Yesu:
5. “Posunga nkhosa ife
Nzozizwitsa, nzodabwitsa
Kubusa kwathu
Ntchitozo.
Mngelo anasimba za
3. Aweruza ndi mphamvu
Kubadwa kwake.”
Ku nthaŵi yamuyaya;
326 Dizo Lake Lisamala
1. ATATE, tifika pamaso panu; Am’dziko.
Mukomane ndi ife, Mbuye wathu. 4. Mbwere mudzamve nonse
2. Mitima yathu iyi nayo njanu, Zamphamvu za Yehova;
Muiyeretse, muikonze Mbuye. Mumwibire, mumyamike
3. Ndi maso athu awa nawo nganu, Yehova.
Muŵapenyetse zinthu zanu zokha. 5. Tisonkhane tonsefe,
4. Ndi manja athu awa nawo nganu, Tigwadire Ambuye;
Agwiretu ntchito yanu yokhayo. Timlambire, timlambire
5. Ndi miyendo yathu iyinso njanu,
Yehova. Naitana atate
329 Kupereka mzimu wake:
“Mlungu wanga, Mlungu wanga.
1. Mlungu akuyanganiradi
Mwandisiy’ranjitu Ine,
Kufikira tionana. Mundikweze m’Mwambamo,
Azasunga nkhosa zake; Landirani mzimu wanga.”
Mlungu akuyang’aniredi 4. Ankhondowo Poona
Zinachitika pamtanda,
E! Tidzakomanansotu Anabaya m’nthitimo,
Pamapazi a yesu, Munatuluka magazi.
E! Tidzakomanansotu Paphirilo la Golgota
Anaferapo Mbuyeyo
2. Mulungu akuyan’ganiredi. Nasauka koopsya
Mulungu akuyan’ganirenidi Ndi zoipa zathu izi.
M’dzanja mwake akulere, 331
Ndi mapiko akubise; 1. TUMPHATUMPHA moyo wanga,
Mulungu akuyan’ganirenidi. Sangalala ndi Mtetezi;
Kuwombola Kwa Yehova
Kwatuluka m’dziko lako.
Mulungu wakwezekatu,
Mpulumutsi m’dziko lako,
Wakwezekatu Chitetezo.
330 Wabvundikira iwedi
1. POTULUKA m’mudzimo Mzimu wanga’we wafunda,
Yesu anasenza mtanda, Lulutiratu moyo wanga.
Pokwera ku Gologota 2. Bvinabvina moyo wanga,
Kukampachikatu Mbuye. Lulutira mtima wanga;
Pilatoyo, mfumu yawo, Wa mawuwo a Yehova
Inampereka kwa ’Yuda, Watuluka m’dziko lako.
Kuti ampachiketu 3. Imbirira moyo wanga,
Kufera zoipa zathu. Mtendere wako wafika;
(Atate ’nu amayi ’nu, nonsenu, Mbendera ya Chitetezo
Onani Yesu wasenza mtanda; Waikwezetsa ndi Yesu.
Atate ’nu, amayi ’nu, nonsenu, 4. Ukondwere moyo wanga,
Onani Yesu wasenza mtanda.) Kuunika kuoneka,
2. Zoopsya zopambana Ndi mdimawo uthaŵatu;
Zinachtika pamtanda Lulutira moyo wanga.
Kuti mdima unadza, 5. Usekere moyo wanga,
Dzuŵa linabisikanso. Ndi Yehova akufuna;
Chinsalucho cha m’kachisi Wakwezatu mbenderayo
Chinang’ambika pakati, Ya Chitetezo, sekera.
Myala inaswekanso,
Dziko linagwedezeka. 332
3. Pomwalira Mbuyeyo 1. PAKUONA imfayo
Anapfuula kokweza Chisonicho chikula
Ndilira misozi. AMEN, Amen, Amen.
Ndilira, ndilira, 335
Ndilira Mbuye Yesu wangadi.
1. NDIDZE pafupi pa
Ndaimba ndi kulira ndi kusisima,
Mlungu wanga,
Ndaimba ndi kulira ndi kusisima,
Ngakhale pamtanda
Ha! Ha! Aleluya!
Mundikweza;
Ha! Ha! Aleluya!
Koma ndiimbabe
Mwasiyiranji Ambuye Yesu?
Mbuye mndikhalitse,
2. Ndinasiya amayi,
Mbuye mndikhalitse,
Ndinasiya atate,
M’fupi Ndinu.
Abale komweko.
2. Ngakhale kuthengo
3. Kazembe wanga m’matenda,
Ndasokera,
Ndili m’manja mwa Mbuye.
M’mdima ndigonapa
Abale tsalani.
E, pamwala;
4. Zoipa zakanikadi,
Koma m’kulotako
Sizikhoza kuchotseka,
Ndiyandikizanso,
Ndilira misozi.
Ndiyandikizanso
5. Angelo aitana,
M’fupi Ndinu.
Aitana Kumwambako,
3. Pajapo ndipenya
Tiyeni, tikwere!
Pokwerapo,
6. Munafera pa mtanda
Angelo atsika
Chifukwa cha inedi, Si
Kumwambako,
cha wina ayi.
Ndiwo akodola
333 Kuti ndikabwere,
1. LIDZE msanga dzuŵa lanu Kuti ndikabwere
Lolonjezedwa, Ambuye. M’fupi Ndinu.
Mnalinena polaŵira 4. Tsopano poukanso
Kwa anyamata, Ambuye. Wokondwatu,
Kuli chimwemwe m’dzuŵalo Ndipeza pomwepo
Lakufika Ambuye. Pali Mlungu;
Ha! Ambuye bwerani. Ndipo masautso
Ha! Ha! Ambuye bwerani. Andisendezanso,
2. M’dziko lino chimwemwecho Andisendezanso,
Chakudza ndi Yesu Mbuye. M’fupi Ndinu.
Mfumu yathu ya Kumwamba 5. Pena pakufadi,
Ndi dziko lonse lapansi. N’kwera m’Mwamba,
3. Adzakhala pampando Dzuŵa ndi nyenyezi
Wakuweruza makamu; Zitsalira;
Amitundu adzaima Pomwe ndiimbanso,
Pamaso pa Mbuye Yesu. Ndidza pafupi pa,
4. Adzanena kwa anthuwo Ndidza pafupi pa
Akudzanjatu lamanja, Mlungu wanga.
“Loŵani ’nu m’chikondwero
Cha Atate nthaŵi zonse.”
336
1. Munasiyatu
334
Dziko lanulo, Ataya zoipa;
E! Chifukwa cha tse; Omwe asamba mwa uyu
Ndi ku betlemuko Ataya zoipa.
Pakubandwa inu. 2. Woba wakufa ’napenya
Nyumba zao nakukanani. Kasupe, nakondwa,
Ndimo inenso mwa uyu
Ndisamba ndiyera.
Mbuye yesu lowani m’mtima,
Ndisamba ndiyera,
Nyumba yanu ndimtimanga
Ndisamba ndiyera;
. Mbuye yesu lowani m’mtima, Ndimo inenso mwa uyu
Nyumba yanu ndimtimanga. Ndisamba ndiyera.
3. Mwazi wa Yesu wokondwa
2. Akumwambawo Ukhala wamphamvu
naimbitsatu, Kwa ana onse a Mlungu,
kukulemekezani Uchita kwombola.
koma monga mwana, Uchita kwombola
mziko munabadwa, Uchita kwombola;
munadzichepesadi. Kwa ana onse a Mlungu
3. nyama za mthengo Uchita kwombola.
Ndi mbalamezo, 4. M’mene ndapenya mwazi wa
Mabala anuwo,
Zili nazo zogonamo.
Kukonda kwathu nditama
Koma mwana wa mulungu Kwa kutha kwa moyo.
Analibe nyumba, Kwa kutha kwa moyo,
M’mapululu nagonatu. Kwa kutha kwa moyo;
4. munadzera ndi Kukonda kwanu nditama
mau amoyo, Kwa kutha kwa moyo.
Akupulumutsa anthu; 5. Kumwamba ndikaimbanso
anakanidza, Zimphamvu za Mlungu,
anatsautsa, Zopulumutsa onsewa
anapichika inu. Omvana ndi Yesu.
5. M’mene mubwera Omvana ndi Yesu,
Kutiweruza Omvana ndi Yesu;
Zopulumutsa onsewa
Ndi angolo oimbira,
Omvana ndi Yesu.
Mundiitane,
Muti “idza’wo, 338
Khala nane kumwamba. 1. Yesu and’itana
Adzandiyeretsa,
337 Ndi mwazi wake wkhetsa,
1. KASUPE ali wodzaza Paphiri gologota.
Ndi mwazi WA Yesu;
Omwe asamba mwa uyu
Ataya zoipa. Ndlikudzatu,
Ataya zoipa, Ndidza Kwa inu;
Munditsuke m’mtimamo
Ndi mwazi wanuwo 4. Kalekale ndinathawa,
Ndinakana kumvera inu;
Koma lero ndamva kuti
2. Ndafoka, ndaipa, Muli mwini wake wa moyo.
Mundilimbikitsetu;
Mundiyeletse konseko,
340
1. MALO alimo m’nyumba ya Yesu,
Ndiyereyere mbuu. Ndi nyimbo zake zakuitana:
3. Atero ndaniyo? “Loŵa, loŵa,
Ndi yesu wabwino; Tsopano loŵatu.”
2. Mdima ufika, dzuŵa laloŵa,
Apatsa mvanu mtendere Nthunzi zilipo, wadza usiku.
Ndimphamvu m’mtimamo. 3. Nyumba yodyera ilikudzaza;
4. Yesu akhzika, Idza nuloŵe, Mkwati anena:
Zonse za m’katimo; 4. Chakudya ichi ndi cha iwenso,
Madzi amoyo umwe kolere.
Nalonga mzimu woyera 5. Onse am’Mwamba Ali momwemo,
Munafoipamo. Ndipo Angelo akuitana:
5. Nditam mwaziwo! 6. Mawu a Yesu ati: “Msangatu
Nditama chifundo! Idza, wochedwa, loŵa
Nditam yesu ambuye, m’nyumbamo.”
Nditenga mphamvu “ko. 7. Msanga adzachitseka chitseko,
Adzakuuza: “Choka, chokatu.”
Choka, choka,
Anena chokatu.
339 341
1. Ndi misozi ndi chisoni 1. PAMTANDAPO, pamtanda,
Ndiliratu Kwa inu yesu. Yesu ’nafera;
Ndichifundo chandi gwira Pamutupo chilemba,
Chisoni ine.
Ndirila kuti ndine wanu.
Analira, “Eloi, Mlungu wanga!
Lama Sabakatani,
E! kwa inu, E! kwa inu,
Mwandisiyiranji?”
Ndirila kuti ndine wanu. 2. Kumandako, kumanda
Yesu nauka;
2. Mbuye yesu ndi atate, Anaposa imfayo,
Mundiona ndili wosowa Watha zonsezi.
Ndikondwera, Mbuyanga
Ndimasowa mzimu wanu
’Naukadi;
Kuyinga zonse za mumtima. Sekerani nonsenu,
3. Mtendererewo wosanyenga Yesu ngwamoyo.
Ndirila ine m’mtima mwanga. 3. Pakukwera Kumwamba
Kondimvets chimwemwetu Yesu anati,
Ndirila ine m’mtima mwanga.
“Musachoke m’mudzimu, Tikomana mwadzikolija.
Pempheranitu;
Mzimu Wakuyeradi adzabwera,
Kuthangata nonsenu, 2. Tidzaimba komwekonyimbo
Kuti msafoke.” Za abwino omvero yesu.
4. Uzanitu abale, Sitizamva chisoni Ife.
Onse alongo, Tidzakondwe masiko onse.
Ndi amitundu yonse
Adzakondwera. 3. Tidzatama atate wathu
Musaope ntchitoyo yokomadi, Kuti iye napatsa yesu
Mphotho yake Kumwamba, Kuchotsera zochimwa zonse
Moyo wosatha. Ndikutidalitsira Ife
342 344
1. M’DZIKO lino tikhalamo APITA anzathu dzuŵa lino
Utibvuta moyo, Kosaoneka,
Koma dziko la mtendere Apita anzathu dzuŵa lino,
Lili kwa Mulungu. Apita anzathu dzuŵa lino
2. Watitsogolera Mbuye, Kosaoneka.
Komwe Kwa Atate, A! Kumwamba
Ndimo tidzatsata naye A! kuli a Yesu.
Moyo wathu wonse.
3. Ndi tsopano tilindira
345
1. INE ndili ndi manyazi
M`dziko lathu lino;
Kuti kale lomwelo
Ntchito atipatsa Mlungu,
Ndinanyoza kudza komwe
Tizigwira bwino.
Kwa Mtetezi wanga Yesu,
4. Ngati zakuipa zathu
Ndati, Sindimfuna `yi.
Zikatisautsa,
2. Koma Iye wandipeza;
Tithaŵire kwa Mbuyathu,
Atipulumutsa. Ndamuona m`mtandamo,
5. Timpemphere kutipatsa Mwa kufera ine momwe;
Mtima watsopano, Ndipo ndati m`mtima mwanga:
Mbuye, ndikufunani.
Kutithandizira kunka
Paulendo uno. 3. Nsiku zonse kwanja kwake
Kunandithandizatu,
343 Kunandichiritsa mtima;
1. kuli dziko la bwino mwamba Ndipo ndati: Mpulumutsi,
Lakuwala kopotsa dzuwa; Ndinu Mbuye wangatu.
4. Sindifuna Mbuye wina,
Yesu atikonzera malo Koma Yesu yekhayo;
Pokarila Ife komweko. Ine ndili munthu wake,
Iye anandigonjetsa
Ndi kukonda kwakeko.
Bwinoli tipita
Tikomana mwadzikolija, 346
Bwinoli tipita 1. KONDWANI nonsenu,
Mpulumutsi anadza; 1. MEMA nkhondoyo, wadza
Onani kukhola, Mdaniyo,
Ndi mtanda ndi manda Kweza mbendera ya Mbuye.
Mlemekeze, bukitsani, Bvala zidazo, imba nyimboyo,
Naferatu kale; Khazikikatu pa Mulungu.
Kondwerani, mlemekeze Haya, anzathu, itilinda nkhondo;
Akhaladi moyo. Limbanitu, nkhondo nja Yesu.
2. Kondwani nonsenu, Musafoke, m’thyole linga lawo;
Anakhetsatu mwazi, Mbuye ndiye Wopambanayo.
Natiwombola nawo, 2. Mlungu mverani, mphamvu
Tikhale ana ’ke. Patseni,
3. Kondwani nonsenu, Tithandizeni, tipempha.
Atikhululukira, Nkhondo itatha, titapambana,
Wosachimwa nafera Tidzalandiratu korona.
Anthu ’fe oipa. 3. Mlake mdaniyo, mwimbe
4. Kondwani nonsenu, m'njiramo
Mfumu yathu yakwera; Mpaka nkhondoyo ileka.
Kwa Atate Kumwamba Zida konzani, mantha tayani,
Atipempherera. Pitikitsani adaniwo.
5. Kondwani nonsenu, 349
Adzabweranso Yesu,
1. M'MANDA, nagonamo
Waulemu, wamphamvu,
Yesu Ambuye,
Kuweruza dziko.
Anadikiratu
347 Tsiku lija.
1. TATE ndili mwana wanu, M'manda naukamo
Nkana ndinachimwa, Napambana ’'dani akewo;
Ndingolirira kwa Inu; Anauka kupambana imfayo,
Khululukireni. Ali moyo ndi oyeramtimawo.
Machimo anga ngambiri Wauka, wauka!
Osaŵerengeka, Aleluya wauka!
Ndingoyang’ana kwa Inu; 2. M'manda munalibe
Khululukireni. Yesu Ambuye,
2. Ndinachimwa poganiza Nadikira chabe
Ndi polankhulanso, Alondawo.
M'ntchito zanga ndachimwanso; 3. Imfa yalephera
Khululukireni. Kumutsekera,
3. Ndinachita mphulupulu, Anachotsa zonse
Ndinakunyozani, Zomzingazo.
M'ntchito zanga ndalephera; 350
Khululukireni.
1. YENDANI, Mfumu yamtendere
4. Zonse ndinakonda kale
Anthu akuimbirani;
Ndi zopanda pake,
Apfuuletu Hosana,
Sindinakhuta nazotu;
Agonjeranso anthuwo.
Khululukireni.
Yendanitu m'ulemudi,
348
Pulumutsani anthuwo. Zinthu zonse pansi pano
2. Yendani, Munthu Wachisoni, Sizikondweretsa ife.
M’mudzi wa Yerusalemu; 3. Mzimu, mlonge m’mtimamo
Angelo amapenya ’Nu Maphunziro achifundo;
M’mene mwafera anthuwo. Timve lero ndi maŵa
3. Yendanitu, Wansembe wathu, Ndi masiku onse Yesu.
Mtanda wanu mwanyamula Ndimo m’Mwamba tidzaona
Watisandukira dalo, Tidazimva pansi pano.
Watitengera moyowo. 353
4. Yendani mwaulemerero,
1. PEMPHERO ndiko kufuna,
Akulindirani mphotho,
Kulakalakatu;
Moyo wanu wosatha
Ndi monga moto liyaka
Watilonjezera moyo.
Mumtima wa munthu.
351 2. Pemphero ndiko kulira,
1. KAMWANA Yesu ’nabadwa, Ngakhale misozi,
Ndi Iye Mlungu Wamphamvu; Kupenyetsetsa Kumwamba,
Angelo anapembedza Mulungu mpafupi.
Mwana wakhanda Iyeyu. 2. Pemphero ndiko kufuna
2. Kamwana kaja ’nayamba Kwa mwana wamng’ono;
Kuonetsera Atate, Ndiponso mawu amphamvu
Lero anena Kumwamba: A munthu wamvanu.
“Tiana tidze Kwa Ine.” 3. Pemphero ndiwo mweyawo
3. Tibwera ndi tianato Apuma akristu;
Kukabatiza ’menewa; Ndi mapemphero tiloŵa
Muŵachitire chifundo. Dziko la imfalo.
M’ŵapatse Mzimu Woyera. 4. Mutiphunzitse, Mbuyathu,
4. Angelo anu asunga Kupempha kotero,
Tiana tathu tofoka; Kuyandikira kwa Mlungu
Pa njira yanu tiyenda, Ndi mtima wabwino.
Mulembe m’Mwamba maina. 354
5. Mukonda nyimbo za ana,
1. Ndisauka, ndinachimwa,
Kokoma amaimbatu;
Ndi ana athu atama Koma inu mnandifera,
Ndimo ndamva mnd’itana
Atate, Mwana ndi Mzimu.
Mwana mlungu ndingubwera.
352 2. Ndisauka, ndimasowa
1. YESU Mbuye, onani Mpamvu ya kuyera m’mtima
Tadza poitana Inu;
Mwazi wanu wanditsuka;
M’dzina lanu tifika
Mwana mlungu ndingubwera
Osekera Kwa Atate;
Mkhale nafe Inu nokha 3. Ndisauka, sindikhoza
Tikaimba nkupemphera. Kuiletsa nkhondo m’mtima,
2. Mbuye, Mzimu Woyera Ndichisoni, mantha, nkhawa
Munapatsa ana anu Mwana mlungu ndingubwera
Kukalonga mumtima 4. Ndisauka, sindiona
Mawu ndimo mvanu womwe:
Ndingudwale, ndilefuka, Kuti anthu ena
Zonse ndizitaya Kwa ‘nu, Amuone iye.
Mwana mlungu ndingubwera Yenda iwe, yenda.
5. Inde yesu mulandira. Yenda iwe, yenda,
Muchilitsa, mpulumutsa Siliva ndilibe;
Mwa Yesuyo, yenda!
Mau anu ndivomera
2. Kukondwa kwa wodwalayo
Mwana mlungu ndingubwera. Kunali kopambana;
6. Inde, yesu, mundikonda Iye anatumphatumpha,
Zonse zina ndizitaya; Kuzungulira
Tsono kukakhala wanu, Sunagoge yense.
Mwana mlungu ndingubwera. 3. Lero lino Mbuye Yesu
355 Aitana nonsenu;
Mukamvera ndi kumtsata,
1. YESU, ndipemphera Mudzakondwera
Mndithangate
Ndi mdalitso wake.
Kukonda Inutu,
E, kwambiri. 357
Koposa zonsezo 1. YESU watidzera, watidzera,
Za pansi panopo, Way’tana anthu onse.
Ndikondane Udzimvere wekha.
Ndinu Mbuye. Aleluya, Aleluya!
2. Kale ndinafuna Aleluya, Aleluya!
Za pansipa, Udzimvere wekha.
Tsopano ndilira 2. Kudziŵa ukudziŵa, ukudziŵa,
Inu nokha. Kulibe zachisoni.
Ndifuna kukonda Udzimvere wekha.
Inu kopambana 3. Atumwi atumika, atumika,
Zinthu zonse Akulalika Yesu.
Za pansipa. Udzimvere wekha.
3. Inu ndidzatama 4. Yesu Mpulumutsi, Mpulumutsi
Nthaŵi zonse, WA dziko lili lonse.
Imfa ikafika Udzimvere wekha.
Ndidzanena: 5. Kumva ulikumva, ulikumva,
“Ndifuna kukonda Ungonyalanyaza.
Inu, Mbuye wanga, Udzimvere wekha.
Kopambana 6. Bwerani inu nonse, inu nonse,
Zonse zanga.” Mudzalandire moyo.
356 Mudzimvere nokha.
1. PANALITU wakudwala 358
Amene akakhala 1. MUDZE Kwa Yesu, musachedwe.
Pakhomo la sunagoge: Kalata ilozera njira;
Amaitanatu tonsefe,
Bvomerani Iye.
Tidzakondweradi m’Mwambamo
Posonkhana komwe kuli ’Ye; 4. Aliponso adani am’kati ndi
Tidzakhala naye komweko Ku Akunja;
Dziko losafa. Yesu watisekera, tidzakuimbirani.
2. Lolani ana, mumve Mlungu, 5. Aliponse mabvuto, ena ndi oipa;
Tsegulani mitima yanu, Yesu mutimasule Kwa adani athu.
Sankhani Iye, Bwenzi lanu; 361
Musachedwe, mudze.
3. Ganizansoni, ali pano, 1. Ndine mbusayo wabwino
Ndinafera nkhosazo;
Mthenga wake mverani lero;
Mawu okoma ati lero, Yotaika ndaifuna,
Musachedwe, mudze. Mpaka ndataya moyo.
359 Mbulu wandi’gamba nthiti
1. MWA ine, moyo wanga ndi Yesu Wandin’gambanso m’manja,
(Yesu) Yemwe anafera ine, Wandin’gambira zbvala,
Ndiye anandiwombola; Ndasala waumphawi.
Yesu, Yesu.
2. Mwazi wake ndi chitsime changa,
(Yesu) Pamene ndikasambamo 2. Nkhosa zanga zimandimva,
Zochimwa zanga zidzatha; Ndikaziitanazo;
Yesu, Yesu. Ndimazipatsa moyowo,
3. Yesu Mfumu, ine ndingadzafe Atate nazisunga.
(Yesu) ngati mundisiya ndekha, 3. Atate wondipatsazo
Kukhala ndekha sinditha; Ali nayo mphamvutu,
Yesu, Yesu. Kuzidyetas, kuzisunga
4. Yesu Mfumu, ine ndisekere Palibe wolandazo.
(Yesu) Inu Mpulumutsi wanga 4. Mudzaona zovalazo
Pamene mukhala nane; M’kati ali fisiyo;
Yesu, Yesu. Mananyengedwa anthuni,
Ine ndine mbusayo.
360 5. Tamverani anthu inu,
1. LEKANI kubvutika ndi zinthu za Ine ndine mbusayo;
Padziko, Ndine njira, ndine khomo
Musekerere kuti tidzaimbira Yesu. Thawani mimbuluyo.
Imbira!
Timwimbire Yesu, 362
Mpulumutsi wathu! 1. CHIYEMBEKEZO changacho
Imbira! Chamangidwa pa mwaziwo;
Timwimbire Yesu, Sindikhulupira pena,
Tonse tidzakondwera. Ndigotsamira pa yesu.
2. Musadziunjikire chuma cha
Padziko Ndaima nji pa Kristuyo,
Dzimbiri ndi njenjete Ndiye chitanthwe cholimba,
Zimachiononga. Maziko ena mpa mchenga.
3. Koma mudziunjikire chuma cha Ndaima nji pa Kristuyo,
Kumwamba Ndiye chitanthwe cholimba,
Kumene anapita Mtsogoleri wanu. Maziko ena mpa mchenga

2. Nkhope yake ‘kabisika,


Ndipuma m’chisomo chake;
M’namondwe ndi m’mphepo zonse,
Nangula wanga ali nji!
3. Pangano lake m’mwaziwo 363
Lindisunga m’chigumula; 1. TIYAMIKE mbuye Yesu
Zondizinga zikachoka. Yemwe anatifera
Yesu ndiye thanthwe langa. Imfa ija yoopsetsa
Kuwombola tonsefe.
4. Likalira lipengalo, Ife
Ndipezeke mwa yesuyo Tapulumukadi,
Wobvekedwa, wolungama, Ife
Wopanda banga konseko. Tapulumukadi,
Imfa,
Imfa yoopsa ija yapamtanda, M’ulemerero wake!
Imfa, 2. Tsopano ndimwona Iye
Imfa yoopsa ija yapamtanda. Mwa chizimezimetu;
2. Panalibe mwa abale Tsiku lija ndidzaona
Yemwe akadakhoza Ulemerero wake.
Kupereka moyo wake 3. M’mene masautso onse,
Kuwombola tonsefe. Nthenda, imfa, zidzatha,
3. Tikondwera ife tonse Dziko likadzakonzedwa,
Pakuona ntchitoyo Ndidzakondwa koposa.
Anachita Mbuye Yesu 4. Lodala tsiku lomwelo
Kuwombola tonsefe. Ndidzamwona Yesuyo,
364 Mpulumutsi wanga yemwe
Anandikonda ine.
1. MZIMU ndi mtogoleri
M’njira yachikristuyo, 366
Atitsogoleratu 1. MVERANI mbiri yozizwitsa
Paulendo wathuwu. Ya Yesuyo kalelo;
M’yoyo ikondweratu Iyeyo ’nadza pansi pano
Pomva mawu akewo, Kutipulumutsa ’fe.
Pakunena Mzimuyo, Ndani anatiwombola?
“Osokera, bwerani.” Mwana wa Mlungu pa mtanda.
2. Bwenzi lathu ndinutu, Anatani?
Mkhale m’fupi nafetu; Anafera.
Msatisiye tokha ’fe Ali kuti?
Pakuyenda m’mdimamu; Akhaladi m’Mwamba
Pakuwomba mphepozo Kutipempherera.
Timaopa m’mtimamo, 2. Palibe m’modzi akanatha
Tsono timve mawuwo: Kuloŵa m’malo mwake;
“Amantha ‘nu, bwerani.” Ngakhale anali wamkulu
3. M’mene ntchito yathatu, ’Nasiyidwa namnyoza.
M’mene tidikira ’Nu, 3. Kodi mudzampembedza Mbuye
Pakukhumba m’Mwambamo, Mpulumutsi wathuyo?
Tsono tipempherabe. Kodi inu mudzaloŵamo
Nthaŵi ya mabvutowo Mu Ufumu wakewo?
Tikhulupirira ’Nu, 367
Tsono timve mawuwo,
1. Ufuna kowomboledwa kodi?
“Okondedwa, bwerani.”
Ilipo mphamvu m’mwazi wake,
365 Ufuna kugonjetsa zoipa?
1. MASO ndi maso ndi Kristu, Muli mphamvu m’mwazi wake.
Kodi ndidzachitanji
M’mene ndidzaona Yesu,
Muli mphamvu yodabwitsatu
Yemwe anandifera?
M’mwazi WA yesuyo
Ndidzamwona maso ndi maso
Muli mphamvu yodabwitsatu,
Kuseri kwa mitambo;
Posachedwa ndidzamwona M’mwazi wamwana WA nkhosa.
2. ufuna kuleka kunyadako?
Ilipo mphamvu m’mwazi wake, (mloŵetsenitu).
3. idzatu pa mtanda nutsukidwe. 2. Utsegule mtimawo,
Muli mphamvu m’mwazi wake. Mloŵetseni
3. ufuna kuyera kopambana? (mloŵetsenitu),
Ilipo mphamvu m’mwazi wake,
Ukachedwa achoka,
Zoipa zonse azayeretsa Mloŵetseni
Muli mphamvu m’mwazi wake. (mloŵetsenitu):
4. ufuna kugwera ntchito yake?, Ndiye Bwenzi lakolo,
Ilipo mphamvu m’mwazi wake, ’Dzapulumutsa ’we;
Ufuna kumuimbira iye? ’Dzakusamaliranso,
Muli mphamvu m’mwazi wake. Mloŵetseni
(mloŵetsenitu).
368 3. Imva mawu akewo,
1. MPULUMUTSI Wokondedwa, Mloŵetseni
Mwandipulumutsa ine; (mloŵetsenitu),
Ndine wanu, wanu nokha, Sankha Iye leroli,
Wotsukidwa m’mwaziwo. Mloŵetseni
Aleluya, Aleluya, (mloŵetsenitu);
Mwanawankhosa ndinutu: Wangoima pa khomo,
Mwazi wanu wanditsuka, ’Dzakusangalatsa ’we,
Aleluya kwa Yesu. Udzamlemekezatu,
2. Mtima wanga wabvutika, Mloŵetseni
Zaka zonse ndingochimwa; (mloŵetsenitu).
Tsono sindikangalika, 4. Mlendo wa Kumwambayo,
Ndingopuma mwa Yesu. Mloŵetseni
3. Mwandipatulira ine, (mloŵetsenitu),
Kwa Inu ndidzipereka, ’Dzakupatsa zonsezo,
M’moyo, m’imfa mboni yanu Mloŵetseni
Ya chipulumutsocho. (mloŵetsenitu);
4. Aleluya, mwandigula, ’Dzakhululukira ’we,
Ndipo mudzandisungabe; Ndipo potsirizapo
Mwazi wanu ndi wamphamvu ’Dzakutenga m’Mwambamo,
Kuyeretsa konseko. Mloŵetseni
369 (Mloŵetsenitu).
1. MLENDO ali pakhomo, 370
Mloŵetseni 1. NDIPEREKA zanga zonse
(Mloŵetsenitu), Mwaufulu Kwa Yesu;
Wadza kalekalelo, Ndidzamkonda kopambana,
Mloŵetseni Tsiku lili lonsetu.
(Mloŵetsenitu); Ndiperekatu
96 Zonse Kwa Yesu;
Mtsegulire msangatu, Ndipereka zonse Kwa ’Nu,
Wakuyerayerayo, Dalitsenitu.
Mwana wa Mulunguyo, 2. Ndipereka zanga zonse
Mloŵetseni Pamapazi a Yesu;
Zapadziko ndazikana, Ambuye yesu.
Nditengeni Yesu ’Nu. 3. Chiso chandisungadi,
3. Ndipereka zanga zonse, Panjira yangayo,
Ndipo n’khale wanutu; Chisomo chidzasunga ne’
Mzimu wanu ’ndidziŵitse Mpakatu kwathuko.
Kuti ndine wanudi. 4. Kwathu tizaimba nyimbo
4. Ndipereka zanga zonse, Ya chisomo chake,
Ndili wanu ndense ’ne; Yolemekeza mlunguyo
Nditamanda Dzina lanu, Munthawi zosatha.
Aleluya, Ambuye.
373
371 1. CHITETEZO chachikulu
1. Kwathu sipaziko, ndingopitilira Chotuluka m’mwaziwo
Ndazikundikira chuma kumwambako WA Ambuye Yesu Kristu,
Mungelo akodola pakhomo la mwamba Mpulumutsi wathuyo.
Ndipo dziko la pansi sindiyetsa kwathu. Mpulumutsi, chitetezo
Chipezeka m’mwaziwo.
Muye, ndinu bwenzi langa ndithu 2. Ndi chimwemwe ndimaona
Ndichitenji ngati kumwamba sikwathu Mtsinjewo wa mphamvutu;
Zonditsutsa zachotsedwa,
Mungelo akodola pakhomo la mwamba
Yesu wanditsuka mbuu!
Ndipo dziko la pansi sindiyetsa kwathu.
Mpulumutsi, chitetezo.
Chindisangalatsatu.
2. Andiyembekeza aulithuchi ndidziwa 3. Tchimo lonse ligonjera
Mpulumusi wanga wondikhululukira Chikondicho cha Yesu,
Adzandi pyolesa pamene ndafoka. Maganizo ’yeretsedwa;
Ndipo dziko la pansi sindiyetsa kwathu. Ndingofuna zakezo.
3. Mayi watsogola ku ulemelero, Mpulumutsi, chitetezo
Ndfuna kugwira dzanja Lake Konko. Chigonjetsa mtimawu.
Andi dikhilanso pakhomo la m’mwamba 4. Ndili nawo moyo w’satha
Ndipo dziko la pansi sindiyetsa kwathu. Wochuluka mwa Yesu,
4. Mu ulemelero tidzakhala m’yaya, Mzimuyo wadzaza mtima
Ndi chimwemwe chakecho.
Oyeramtimawo alikulambira.
Mpulumutsi, chitetezo,
Ati, “aleluya kwa mlungu wa mphamvu’
Chiyanjano chomwenso.
Ndipo dziko la pansi sindiyetsa kwathu. 5. Mantha, nkhaŵa, ndi chisoni
Zachotsedwa zonsezo;
372 Mbuyeyo ndimkhulupira,
1. Chisomo chodabwitsacho, Anditsogoleratu.
Chapulumutsa ne’ Mpulumutsi, chitetezo,
Woipa wapambanatu Ndimkondadi Yesuyo.
Ndapeza moyo ne’ 374
2. Chisomocho chachotsatu 1. AMBIRI tikondwera mwa Yesu,
Mantha a infa, Nanga inu? Nanga inu?
Pakukhulupirira ye’ Tapeza chipulumutso ndithu;
Nanga inu?
Masiku onse timakondwera Mdalitse Mtsogoleri, nafe,
Pakumva Mawu ake a Yesu; Ndi Mayi Malaŵi.
Wolalikira tidzamumvera; 2. Malaŵi dziko lokongola,
Nanga inu? La chonde ndi ufulu,
2. Ife tiyembekezera YESU, Nyanja ndi mphepo ya m’mapiri,
Nanga inu? Nanga inu? Ndithudi tadala;
Chimwemwecho chili Zigwa, mapiri, nthaka, dzinthu,
Mumtimamu; Mphatso zaulere;
Nanga inu? Nkhalango, madambo abwino,
3. Titasokera tinabwerera, Ngwokoma Malaŵi.
Nanga inu? Nanga inu? 3. O! Ufulu tigwirizane
Tidziŵa kuti ndiwo uchimo; Kukweza Malaŵi;
Nanga inu? Ndi chikondi, khama, kumvera,
4. Tinachoka munjira ya imfa, Timutumikire;
Nanga inu? Nanga inu? Pankhondo nkana pa mtendere
Takopeka ndi Mawu a Yesu; Cholinga n’chimodzi,
Nanga inu? Mayi, Bambo, tidzipereke
375 Pokweza Malaŵi.
1. MBUYE dalitsani Afrika, 377
Itukulidwe nyanga yake; 1. ANTHU m’maiko onse
Mverani mapemphero athu, Akhala mitundu;
Ndipo mtidalitse ife ana anu. Kapena m’dziko lino
Mbwere Mzimu, Akhala anzathu;
Mbwere Mzimu, mbwere! Agona mwa zoipa,
Mbwere Mzimu Apulukiradi,
Mbwere Mzimu,mbwere! Ati, Mutilangize
Mbwere Mzimu Abale, bwerani.
Woyera, Woyera. 2. Ngakhale alemera
Mbuye, dalitsani Ndi chuma cha dziko,
Ife ana anu. Kodi akakondwera
2. Dalitsani mafumu athu, Opanda Mulungu?
Akumbukire Mlengi wawo; Kodi akhala mwaŵi
Aope ndi kunjenjemera, Otsata zawozo?
Ndipo m’ŵadalitse iwo ana anu. Iyai, awonongeka,
3. Dalitsani mafuko onse, Apeza tsokalo.
Aweruze bwino maiko; 3. Ndi ife akudziŵa
Adzichepetse ndi kuopa, Chikondi cha Mlungu,
Ndipo mtidalitse tonse ana anu. Kodi tidzaŵamana
376 Kuŵala kwa Kristu?
Chipulumutso! Inde,
1. MLUNGU dalitsani Malaŵi,
Tichibukitsetu,
Mumsunge m’mtendere;
Kuti mitundu yonse
Gonjetsani adani onse,
Ibwere kwa Yesu.
Njala, nthenda, nsanje;
4. Akristu nyamulani
Lunzitsani mitima yathu
Kuti tisaope,
Maneno a Mulunguyo, Ndimo mudzazizwa potsirizapo.
Ndi moyo lalikani 2. Kodi muvutidwa naye katundu?
Pa dziko lonselo; Ngwolemera mtanda muusenzatu?
Ndi Yesu Mpulumutsi Ŵerengani madalitso anuwo,
Anatiferatu; Ndimo mudzaimba dzuŵa
Adzabvomera onse; lonselo.
Ndi Mwana wa Mlungu. 3. Poyang’ana ena ndi ndalamatu,
378 Ganizani kuti Mbuye wanudi
Adzakupatsani zake zonsezo,
1. PADZIKO pano tikhalira
Chosagula chuma chanu
M’moyo wosauka;
chonsenso.
Komatu kwa Mulungu kuli
Dziko lakudala; 380
Mbuyathu Yesu wapitako, 1. YESU Mbuyetu, mwafera
Iye ’natsogola; Mphulupulutu zanga,
Tidzamtsatira ife tonse, Ndimo ndamva mund’itana,
Tsiku lomaliza. Mutitu, Msachedwa.
Tiyeni, tiyeni, 2. Zonse za m’dziko zidzatha,
Ku dziko lakudala; Koma za moyo m’Mwamba
Tidzafikira m’dziko ilo Zomwe zidzakhalitsatu,
Tsiku lomaliza. Chakatu ndi chaka.
2. Masiku tikatsala ife 3. Nyengo ifika, chenjera!
M’dziko mwathu momwe Adzakukana m’Mwamba.
Mulungu watipatsa ntchito, Lapa zoipa zakozo,
Tikazigwiritse. Kuti ukaloŵe.
Pamene zakuipa zathu 381
Zisautsa ife,
1. TAMANDANI Mbuye,
Tikapemphere Mbuye wathu,
Inu atate,
Atipulumutse.
Mpatse Yesu mitima yanu.
3. Ulendo wathu ukadzatha
2. Tamandani Mbuye,
Tidzafika kwathu,
Inu mafumu,
Adzatifitsa ife komwe
Mpatse Yesu mitima yanu.
Yesu Mbuye wathu.
3. Tamandani Mbuye,
Sitidzapeza masautso
Inu abale,
M’dziko la Mulungu,
Mpatse Yesu mitima yanu.
Tidzakondwera chikondwere
4. Tamandani Mbuye,
Nthaŵi zonse zathu.
Inu nonsetu,
379 Mpatse Yesu mitima yanu.
1. POZUNZIDWA inu ponseponse 5. Tamandani Mbuye,
Ndi kufoka m’mtima nazo Mipingo yonse;
zonsezo, Aleluya, Aleluya!
Ŵerengani madalitso anuwo 382
Ndipo mudzazizwa potsirizapo.
1. MVERA mtima wanga ’we
Ŵerengani madalitsotu,
Akufunsa Ambuye;
Anakupatsani Mlungudi.
Ŵerengani lina linanso,
“Wosauka WA’mphaŵi, Kwa ife kudzakhala mwayi,
Kodi undikondadi?” Kwa Inu ulemu.
2. “Ndakupeza womanga, 384
Ndamasula zinsinga,
CHIKHULUPIRIRO chathu
Ndakulonda kutali,
Tatchulachi pakamwapo,
Kodi undikondadi?”
Mulungu athandize ’Fe
3. “Akaleka amake
Chikhale cha mumtimamo.__
Kusungira mwanake,
Ine sin’kuleka ’yi,
Kodi undikondadi?”
4. “Ndakukonda ku imfa
Ndi chikondi chosatha,
Kwaulere, kwambiri, Reference
Kodi undikondadi?” Christian literature association of
5. “Msanga ndidzabweratu, Malawi
Udzaona ulemu,
Udzakhala ndi Ine, P.o box 503 blantire [© 1974]
Kodi undikondadi?”
6. Mbuye ndisaukadi,
Chimachepa chikondi,
Mtima wanga mudziŵa,
M’ndipunzitse kukonda.
383
1. MBUYE mtsitsimutse
Ntchito zonse zanu!
Utsani anthu akufa
Ndi mawu a mphamvu.
2. Mbuye mtsitsimutse EDITED BY: ELIAS MUTEYA
Ntchito zonse zanu!
Tauzirani pa ife RCZ LILANDA CONGREGATION
Ndi mweya wa Mzimu
3. Mbuye mtsitsimutse NO: 0972580751
Ntchito m’mitimamo!
Mumvetse njala kwa Inu—
Mutikhutitsenso.
4. Mbuye mtsitsimutse
Ntchito m’kati mwa anthu!
Chikondi chawo chikule
Muchikolezetu.
5. Mbuye mtsitsimutse!
Mawu alimbike,
Pamene aphunzitsidwa
Onsewa amvere!
6. Mbuye mtsitsimutse!
Mzimu adzazetu!

You might also like